Dat's true bro, we're in a democratic society and noone lemme repeat noone can come and intimidate us in our own country!, Bakili Muluzi tv is a genuine freedom fighter and He's a Hero and watever is saying or talking is the truth!, mukuleka kusakana ndikumangana nokhanokha am'boma inu amene mukutionongela misonkho yathu, pano mwagundika kupanga hire kapena kuti hayala mbava ndizigawenga zimzanu zaku Zimbabwe ndi Ruanda kuti zithane ndi anthu olankhula chilungamo, for wat!, shame on you zikhale ng'oma and mozesi kumukuyu, shame on you!, . Bakili muluzi tv will Never ever be arrested and if u'll try to do dat, we'll fight each other!,
Kodi..uwu wa mutu ngati nkhonkhwe mmati ndani... ? Kunkuyu ..akunama kwambiri.... My brother, you are opening the minds of vulnerable Malawians. Keep it up...afa ndi mtima
Zikhale munakhala bwanji inu simumanyodza a Peter muthalika pa hot current amakusakani ndindan zamachende akakhala moses tikufuna justice nkhan ya wetika