Тёмный

Boma Latha - Samuel Lwara 

Nyasa VoiceBox
Подписаться 25 тыс.
Просмотров 8 тыс.
50% 1

On Nyasa VoiceBox, Samuel Lwara asserts that due to UTM's withdrawal from the Tonse Alliance, Malawi theoretically lacks a government. The Alliance has been dissolved.
Ku Nyasa VoiceBox, Samuel Lwara wanenetsa kuti chifukwa UTM idatuluka mumgwirizano wa Tonse, dziko la Malawi lilibe boma. Alliance yathetsedwa.
#malawi

Опубликовано:

 

11 июл 2024

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 37   
@KennedyPhiri-h9h
@KennedyPhiri-h9h 24 дня назад
Boma palibe and we got no president now
@alickkachepa3801
@alickkachepa3801 24 дня назад
Chakwela sakonda zikoli
@BertharrySecurity
@BertharrySecurity 25 дней назад
Boma latha, MCP yikazawina ndiyekuti Abela zisankho
@tasmania527
@tasmania527 20 дней назад
Awa a Lwara awa sazatha bwino. Ali ndi chimtima chovutika kwambiri. Kaya ndi kukhwima kaya ndi chani koma mathero awo ali pafupi.
@LoveHere-ki8ck
@LoveHere-ki8ck 24 дня назад
Yagawana zida band 😂😂😂😂
@GraceZumazuma
@GraceZumazuma 24 дня назад
Ma corner onse obela ma vote mcp mwatulukilidwa kale
@user-wd9yd1bg9n
@user-wd9yd1bg9n 19 дней назад
Thako limozi 😅😅😅
@thomasphiri7799
@thomasphiri7799 25 дней назад
😂😂😂😂
@LucianoKapepuza-sy9wx
@LucianoKapepuza-sy9wx 24 дня назад
Chakwera achoke Ku state house
@Eric-gb9ms
@Eric-gb9ms 24 дня назад
Kwambiri big azipita
@maxwellchilima5440
@maxwellchilima5440 24 дня назад
🎉 judiciary it's your role now. Apa honestly boma lathapo
@rexnyalugwe4910
@rexnyalugwe4910 24 дня назад
Law society of Malawi. UTM yachotsa vote yake, Kodi otsalawo mandate to govern Ali nayo?
@OssmanAbubaker-t3n
@OssmanAbubaker-t3n 24 дня назад
Zoonadi Mr Lwara simukunama apa palibetso chanzeru MCP athako
@user-um6yo6nc3e
@user-um6yo6nc3e 24 дня назад
Awabwezele a Dad aja basi...
@OliverNkhoma
@OliverNkhoma 25 дней назад
Boma latha palibepo
@YasinMusa-ym8lp
@YasinMusa-ym8lp 24 дня назад
Latha boma kumalawi kulibe boma 😂 achakwera agalu chimunduchopa ndamanyasi
@BertharrySecurity
@BertharrySecurity 25 дней назад
Ndipo zakhalabwino kwambiiiiiri
@grayakuzikemanda3114
@grayakuzikemanda3114 24 дня назад
Mphamvuyo ma MP 4 basi boma latha?
@user-wb9ji3oe5o
@user-wb9ji3oe5o 24 дня назад
Latha boma limenelo ndipo mcp iri mmadzi ndipo achita manyazi
@brendachiwamira
@brendachiwamira 24 дня назад
Apule atilankhule chifukwa sadalowe kunyumba ya chifumu ndi chipani,km akupezeka kumeneko chifukwa Cha tonse alliance.ndiye alliance ndiyomwe yatha.
@user-uc1pd1tc2x
@user-uc1pd1tc2x 24 дня назад
Yaaah ndiokuti a Malawi tipange action kaah Kuti tipange referendum
@PetroMatias
@PetroMatias 24 дня назад
Boma rathadi basi
@MikeChingala
@MikeChingala 24 дня назад
Silingathe Ai chifukwa utm inali just a small part of mcp
@Eric-gb9ms
@Eric-gb9ms 24 дня назад
You are a liar
@user-jc5tf8jl1m
@user-jc5tf8jl1m 24 дня назад
Mcp yabisala pa chipande in 2025
@YaqoobStandwell
@YaqoobStandwell 24 дня назад
Mcp yantha kungot yawina ndiye kut yabela palibe wina aliyese akuifuna ndipo or atabela sitizalola kutilamulila ngat akufuna kulamulila azikalamulila nyumba mwake amalawi sakumufuna or akakamile amalawi sakufuna enan or akupatsen kena kake koma nokha mukuziwa chilungamo mukuchiziwa kut palibe wina aliyese akuchifuna chipan cha mcp and achoka or atabela tizachotsa ndimakofi
@joaquegerman2250
@joaquegerman2250 25 дней назад
Vinyo watcha tibalalike
@BrightPhiri-bt6ev
@BrightPhiri-bt6ev 24 дня назад
Chakwera simbuli ngati iweyo samuel lwara.chakwela salankhula akalankhule chifukwa cha iweyo ndiwe ndati kapolo wadziko iwe kumangokhalira kuchikamwa.alliance siyinachite kutha koma utm yachita kutuluka yokha ndiye boma litha chifukwa chan? Dikila uwone ngati boma lithe.zifukwa zomwe ulinazo ndi mcp ndizaiwe wekha.mesa unkadya komweko ku state house? Siumatisokosela nthawi imene umadyayo bwanji? Panopa anakuthamangisa ndiye uzitipangila phokoso fotsek zako ndithu.
@user-qp8kh2hj9o
@user-qp8kh2hj9o 24 дня назад
Hehehe muona kuti mutani Boma latha basi mixeeeeee
@BrightPhiri-bt6ev
@BrightPhiri-bt6ev 24 дня назад
Uko ndiye timati kuzikwata ndi chala maloto a chumba.funso ndiloti kodi president ndani ku malawi? Ngati president alipo ndiye kuti boma lilipo.utm siingathese boma.ufune usafune chakwela ndi president wa boma kkkkkkk
@Eric-gb9ms
@Eric-gb9ms 24 дня назад
Ndiwe wakuba ngati chakwera wakoyo mwantha muziwona
@BrightPhiri-bt6ev
@BrightPhiri-bt6ev 24 дня назад
Ndinaba pa khomo pa pako ?? Iwe ndiwe galu eti ndiponso mbuli yamunthu anthunu mmadana ndi reality.akanakhala kuti dzulo muja watula pasi udindo ndi chakwela bwezi panopa kuli chipwilikiti.koma kutuluka kwa utm ndi kaliati sikungasinthe chilichose mufune musafune chakwela 2025 wooooooo ndiponso ndachepesa chakwela 2030 woooooo.msegula mumimba chaka chake ndichino.kulakalaka mutasamuka mmalawi muno.as long muli panthaka ya malawi president ndi chakwela.
@Eric-gb9ms
@Eric-gb9ms 24 дня назад
@@BrightPhiri-bt6ev mbuli ndiwe because you don't know what you talking about
@mzondinkosi1151
@mzondinkosi1151 21 день назад
Problem is that you think you are very intelligent. NO. Latha bwanji? Tione ngati latha.
Далее
МЕСТЬ МАЛОГО
00:52
Просмотров 75 тыс.
Mudziko Muno Mulibe Chitetezo   Phalombe Big Boy
18:31
A Michael Usi Inu Si A UTM - Lyton Mangochi
23:13
Просмотров 32 тыс.
EXCLUSIVE INTERVIEW WITH SAMUEL LWARA
51:08
Просмотров 30 тыс.