Тёмный

BON KALINDO 11 JULY 2024 KUNG’ALURA PA THURSDAY 

Malawi Trends TV
Подписаться 34 тыс.
Просмотров 29 тыс.
50% 1

Опубликовано:

 

9 июл 2024

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 223   
@VungaQueen
@VungaQueen 20 дней назад
Apa nde chakwela akutitola kwambiri mulungu mumve kulilira kwa amalawife mupaka kugilitsa mutchenga uli wachilengendwe ayi zikomo magamuro anu chakwera adutsa muyetso mitsozi yanthu kuvutika kwanthu dzikhare pa panja lanu achakwera 🥲🥲 inu aboni kalindo keep it up kutiuza anthu opepelawa 🔥🔥🔥🔥
@FRAVIOKUNSANJA
@FRAVIOKUNSANJA 19 дней назад
Koma boma ili lafika posauzana n'chenga umene akulesa wayamba kuvuula lero ameneyu galu kwabasi chakwera atimaliza tonse
@LysonMtalika-tb6fk
@LysonMtalika-tb6fk 19 дней назад
Powerful talking from our beloved president, president for the poor always there for poor Malawian citizens the Dddddd Cccccc!!!!, proud of you always. May the good Lord continue to guide and protect you always 🔥🔥🔥🔥
@GanizaniKamvazaana
@GanizaniKamvazaana 19 дней назад
Akuti apolice adzisilira mpunga WA Ana school koma ADC inuyo ndi wa wani long live a kalindo anya manyi achakwera achitsiru amenewo , nde bwino akalindo ineso maganizo amenewo nariwo kuti athu asavotere chauzika akalindo inuyo inuyo ambuye akudaritseni ife kwakwataine sitikupanga nawo zopusazo tikulira ife ku Ntcheu😢😢😢 koma God knows chakwera adzafa imfa yowawa
@INNOCENTMOFOLO-io8tg
@INNOCENTMOFOLO-io8tg 19 дней назад
😂😂😂😂😂 DC ndiyakatundu zoona
@user-hk3hg1to4e
@user-hk3hg1to4e 19 дней назад
Anatiloza ndi malemu chilima aise pomuchita follow achinyamata ife😢😢
@StevieChikaonda
@StevieChikaonda 19 дней назад
Uku nde kung'alulatu 10,000% ayi zikomo ndithu💪💪💪💪💪💪💪
@FisherAction
@FisherAction 19 дней назад
Big mulungu akudaliseni ndipo pitirizani kutiombola kuwachosa amalawi mw agaluwa a mcp
@EllenPhiri-xt8pt
@EllenPhiri-xt8pt 19 дней назад
God bless you Mr DC you always stand for the poor this government of chakwala is useless ever
@GoodsonDiwadiwa
@GoodsonDiwadiwa 19 дней назад
The Dc Bon Kalindo anthileni fire anthu osowa umunthuwa osanyengelera ayi
@GospelSoldiers-sr7np
@GospelSoldiers-sr7np 20 дней назад
This two much guyz..koma kuli Mulungu amatha kumuchitsa munthu pa mpando ndikuthamangitsa kukamusiya ku ntchire..koma mmawelenga baibulo????? Inalipo mfumu ina imachita zimenezi koma ngati simusamala Mr president ndi nduna zanu mupalanura mkwiyo wa Yehova....take my note
@EmmanuelMpalagule
@EmmanuelMpalagule 19 дней назад
Mr kalindo u are a hero, the opposition the very week, the opposition is in deep slumber,
@vitumbikokamanga5869
@vitumbikokamanga5869 19 дней назад
❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤go deeper mr kalindo you are the best ❤❤❤❤❤❤
@raytavares2256
@raytavares2256 19 дней назад
Mr president the DC we love you and greetings from North London UK
@GamaGama-z8p
@GamaGama-z8p 19 дней назад
Tell dem the dccccc!!! Never stop fighting for the poor innocent people we vote for purposes Mr born we are on ur side
@DalitsoMatope
@DalitsoMatope 19 дней назад
Kalindo we are failing to thank you but only God will thank you
@DeliaKaduya
@DeliaKaduya 19 дней назад
Koma Mulungu ngati kunali kufuna kwanu kuti munthu uyu awulawe u president ayi pafikapa ife anthu anu timveni kulira kwathu 😢, Ife anthu akumuzi kuti tigule sopo timadalira kuvuwula mchenga omwewo kuti tichape, onani pomwe zinthu zafikapa Yehova, ingobwerani muzaweruzepo dziko lanuli Ambuye
@RidwanAdam-nq6lz
@RidwanAdam-nq6lz 20 дней назад
Booooon kalindooooo 🔥🔥
@user-or7ng3fj8f
@user-or7ng3fj8f 19 дней назад
Mr Bonnnnnnnnnnn kalindo DC big up kodi bwanji osayambisa madem bwanji kumalawiko galu ameneyo ife kuno atikwana kwambiri ndithu tiye nazo Mr bonnnnnn kalindo the DC
@GRACIOUSKENAN
@GRACIOUSKENAN 19 дней назад
Timanva nanu kukoma nsaname🎉🎉 ndipo mau anu amatitothoza ifeo,ndiposo pa mpando wa upresident inuo mwafika kale bwana,zolembalemba zangosala tsiku loyikika bas
@kelvinmphande3754
@kelvinmphande3754 20 дней назад
It's the sikusinja Gwenembe song for me
@HawardStainly
@HawardStainly 19 дней назад
Akubwila fodya wamagogo wakuzino uja,(maganga).
@InnocentEdasi
@InnocentEdasi 20 дней назад
The DC 🔥🔥💕 Chakwera atule pansi udindo..., Palibe zoti asintheso ai.., tikumunyengelela uyuh.. _
@limbanimtitima9170
@limbanimtitima9170 19 дней назад
Kung'alula big man,ife Angoni kuntcheu ndife oganiza kkkkk😂
@chimwemwemasamba2880
@chimwemwemasamba2880 19 дней назад
Allowance ya manebbtatenga koma ndiyochepa kobasi....polingalira ndi mmene zinthu zakweleramu
@gwatandingo9502
@gwatandingo9502 19 дней назад
Muli bwino koma Anthu Ena sakukhulupilira inuyo boss munatitenga kutisiya ku sewo inuyo munapita kunja nokha mukadya ndalama zatha lero mwabwera 😂😂😂😂😂😂
@user-vh9uk1jy7w
@user-vh9uk1jy7w 19 дней назад
Our president more fire 🔥 Booooon kalindoooo 🔥 🙌
@MartinsKhumalo
@MartinsKhumalo 20 дней назад
❤❤❤ ndimakunyadilani 👏👏
@user-xd1cm7tm7t
@user-xd1cm7tm7t 20 дней назад
The dc our poor president in Malawi
@ChimwemweBottomani-hc5ju
@ChimwemweBottomani-hc5ju 19 дней назад
Make mbuuu mwana mbuuuuu long live the DC
@pacharokoloviko1694
@pacharokoloviko1694 15 дней назад
😂😂😂😂 ati kufuna kumangidwa!! Komadi ndiwe DC
@JabesAlfaiate-t4v
@JabesAlfaiate-t4v 19 дней назад
A kalindo tiyankhulileni ife tili nanu mcp ndi yoipadi ifeyo a malawi amenetili kuno ku Mozambique tili o khuzika ndi zomwe likuchita boma la a chakwela , ku vuula mchenga mpaka laicence zinachitikako kuti ? Keep it up a kalindo.
@AudettaYohanie-fl3oc
@AudettaYohanie-fl3oc 19 дней назад
Aaaah koma izizi ndiye chakwera wationjedza zedi ,koma chifukwa chani kweni kweni?
@user-wu4tl2yn9e
@user-wu4tl2yn9e 19 дней назад
Khaaaaaa wafika the DC
@loycemmadi9303
@loycemmadi9303 19 дней назад
And it's the song for me😂😂😂😂Winiko Ayi ndithu
@MosesKalenge
@MosesKalenge 19 дней назад
ULEMU WANU MR, THE DC..... BON KALINDO 💪✊✊✊📡🔥🔥🔥🔥🔥🔥
@mbewemisoyaanenenji1908
@mbewemisoyaanenenji1908 19 дней назад
Boooon Kalindo , Pangolin mwana womvuta kwambiri
@PempheroKasimongwa
@PempheroKasimongwa 19 дней назад
Kalindo 🎉🎉 iweyo ndi 1,,,ku Egypt kuja timadya kwabasi ❤❤
@JaxyKumwenda
@JaxyKumwenda 19 дней назад
Tikufuna mademo bwana osamunyengerera Chakwera
@gwatandingo9502
@gwatandingo9502 19 дней назад
Koma mpaka chenga mmmm mawonjeza
@user-ko1lk3br4r
@user-ko1lk3br4r 20 дней назад
Mafuta ayamba kuchoka ku Mozambique kukafika ku area 50 ku Lilongwe kudzela pa njanje ai zikomo
@user-lp8wj3vq4x
@user-lp8wj3vq4x 19 дней назад
Ife dzuro timadikira mademo, agalu amenewa atitopesa
@OwamiSimeon
@OwamiSimeon 19 дней назад
Born kalindo more 🔥
@LuundoJohnkabage
@LuundoJohnkabage 20 дней назад
😅😂ayi ziliko mpaka boma kugulitsa ntchenga😂😂😂😂
@MarkinaJohn
@MarkinaJohn 19 дней назад
Kkkkkkk koma DC kkkkk gwenembe
@BatsonKadzuwa-tl3rp
@BatsonKadzuwa-tl3rp 19 дней назад
Zoonadi mboni ndineyo nditachita ngoz ku Queens ndinalipira kut andithandize
@HannockMesiwni
@HannockMesiwni 19 дней назад
Njira ya ld pokavota sitikavota nkhondo ichitike ichitike
@MariamJaffali
@MariamJaffali 20 дней назад
The DC boooooon kalindoooooooo
@KnowledgecGodwin-xo4pw
@KnowledgecGodwin-xo4pw 19 дней назад
Chakwera nkongo wamako ,mboli Yako ,machende ako ,alipwisi alitongo.
@MouriceChimkondo
@MouriceChimkondo 19 дней назад
Kkkkkk
@RashidSaid-lk6bb
@RashidSaid-lk6bb 19 дней назад
Uchitsilu ndiye umeneo Sizidachitikepo
@annamazingashaibuh6276
@annamazingashaibuh6276 19 дней назад
Kkkkk koma ndipo akavoteraa nda amawooo hiyaa mau Mr Bon
@IvieMwabile
@IvieMwabile 19 дней назад
Akufuna kutimpha agalu amenewa.go deeper
@JohnAsendi
@JohnAsendi 19 дней назад
Kkkk Boma amalawi kutifinya tiwona zinthu shop chaine chasala ndi maepute katoni okhaokha ndatawira kunnjenga ndiyemukulesa mukufuna kundipha chani mukandiphera kuzenje komweko 😮😮😮😮
@annamazingashaibuh6276
@annamazingashaibuh6276 19 дней назад
Uyu ndi nyoooo kwa nyooo ulemu wanu aaaa mchenga athu anayambira kale za mchenga athu amadyera momo abale eishh sambi
@RashidSaid-lk6bb
@RashidSaid-lk6bb 19 дней назад
MCP ikufuna kuzabela ma vote chifukwa sizidachitikepo ku voter without ID ngakhale kuno ku South Africa
@RafickRaj
@RafickRaj 19 дней назад
Mmatha madhala madhala inu mungoyimila koma zikhala bwino
@LovelyJapaneseMaples-xc2bc
@LovelyJapaneseMaples-xc2bc 19 дней назад
Kuswakuswa big osaopa😊
@user-kw7wr4kq9w
@user-kw7wr4kq9w 19 дней назад
We only need solutions not only kulalika
@OmegaNjati
@OmegaNjati 19 дней назад
Ambuye nditengeni
@user-je8jm5uy1q
@user-je8jm5uy1q 19 дней назад
Mafumu aku ntcheu mtima wawo ukuwawa alibe dyera ndi mafumu odziwa kulira moyo wa munthu sizocheza
@MouriceChimkondo
@MouriceChimkondo 19 дней назад
Following boss
@duncainjimmy
@duncainjimmy 19 дней назад
Mulungu adalenda dothi osati Chakwera ai
@OsmanBakali-s5x
@OsmanBakali-s5x 20 дней назад
Where are we going to make our hustle now😭😭😭 mpakana nchenga omweu tkatenge chilolezo? 🔥🔥🔥🔥🔥
@babranzima8120
@babranzima8120 19 дней назад
Ndizisilu zaathu zathu ananyerapo chenga iyewo chakwera
@user-gd6zb2bv8f
@user-gd6zb2bv8f 18 дней назад
Koma funso nkumati kuti, Kodi Chakwela ndi Zikhale wacheyo, samachita manyazi konse akamamva izi? kapena umunthu wanu unatha?? The DC tell them shit
@densonchiwaya8439
@densonchiwaya8439 19 дней назад
Mau awaa sikalindoo
@ChondezVick
@ChondezVick 19 дней назад
The DC himself 🔥🔥🔥🔥🔥🔥
@happychimwemwe-1805
@happychimwemwe-1805 19 дней назад
Umakwana booooon kalindo
@user-qc7qg4cy6k
@user-qc7qg4cy6k 19 дней назад
Totally agree the dc
@dinahmunthali5324
@dinahmunthali5324 19 дней назад
Ine nyimbo ndi zomwe zimandi waza koophya ati Sikusinja ndi Gwenembe amkaimba agogo awake DC popita ku Mzuzu akudutsa mu chikangawa 😂😂😂😂😂 DC makina 😂😂
@LinoMatchado
@LinoMatchado 19 дней назад
Iyayi na ya mchenga yokhayo boma likunena zoona chifukwa mchenga is in the group of minerals and any mineral is a government property which is minored through the government permission. Everywhere in the world illegal mining is prohibited citizens are allowed to collect sand ndi wilibala basi not with a thipa truck then you have to go face the law which is in the constitution every country.
@JamesKambale-s2c
@JamesKambale-s2c 19 дней назад
Koditu uku mcp kwangokula mbuzi za anthu
@user-nf3ik3ff6y
@user-nf3ik3ff6y 20 дней назад
The Dc bon kalindo good Messnge
@texonkautera
@texonkautera 19 дней назад
Anthu amene amabweresa Mbatata Ku nsika wa Limbe Ku chokers Ku Mulanje akuzunzidwa kwambiri akafika kuti asise a Police akuchosa misonkho akuti alakwa akalipire. K20 Pamene anthu akupangira mavuto mafuta anadula Palibe chomwe akupindula
@user-hb1ll8lj3v
@user-hb1ll8lj3v 19 дней назад
Gwenembe ND sikisinje yemweyo 😂😂😂😂
@MynessChirwa
@MynessChirwa 19 дней назад
😂😂😂 book la gwenembe kodi kkk
@user-je8jm5uy1q
@user-je8jm5uy1q 19 дней назад
Ndipo zoonadi chonsecho sanapangile anthuwo chochita
@LoveBanda-sw1nu
@LoveBanda-sw1nu 19 дней назад
😅😅😅😅kumalawi mkokoma ndithu bwanawa akutiposa zochita
@KunyengaMoyo
@KunyengaMoyo 19 дней назад
Ng'alula DC
@ChimwemweBottomani-hc5ju
@ChimwemweBottomani-hc5ju 19 дней назад
Sikusinja ndi Gwenembe😅😅😅😅😅😅😅 Nyengo yokhadxula kukhazula
@SimonMtonga-kf5ht
@SimonMtonga-kf5ht 19 дней назад
Born kalindo more fire
@jameskamanga628
@jameskamanga628 18 дней назад
Koma mkulu uyu kkkkkkkk sikusinja sikusinja kkk
@loycemmadi9303
@loycemmadi9303 19 дней назад
Mr kalindo munafika aaaah kukanapezeka ambiri ngati inu bwezi dzikoli titaona zina aaaah
@TutuAlfred-y2l
@TutuAlfred-y2l 19 дней назад
😂😂😂😂😂. Zosatheka sizidzatheka nanga chenga ndichani uyo wasala pang'no kt amfe ameneyo chisilu chamunthuyo muuze ambere Ku muloza border kuno aone kt angatile ife kuvuula chenga.
@EsnartGirivin
@EsnartGirivin 19 дней назад
Osakhala presdent bwanji abon kalindo Tayambitsani chipani cha amphawi
@INNOCENTMOFOLO-io8tg
@INNOCENTMOFOLO-io8tg 19 дней назад
😂😂😂😂 azingomwadi ambuye mtengeni 😂😂😂😂😂
@LonnieGrem
@LonnieGrem 19 дней назад
🙌🙌🙌ay zikomo
@user-wu8kp7ui5j
@user-wu8kp7ui5j 19 дней назад
The DC 🔥🔥🔥🔥🔥
@user-nn4bf1kw9h
@user-nn4bf1kw9h 19 дней назад
Ing'alureni 🔥🔥
@azunguauskay4903
@azunguauskay4903 19 дней назад
😂😂 Akalindo nyimboyo ndayikonda
@user-no2mx4go8p
@user-no2mx4go8p 19 дней назад
Mpakana licence 😂😂😂😂😂🙌🙌🙌🙌 zili kumalawi nzatose akatenge licence ndi driver 😂😂😂😂
@Sugerman-tw4do
@Sugerman-tw4do 18 дней назад
Big Bos DC mumakwa
@ChikumbutsoTsalangu
@ChikumbutsoTsalangu 20 дней назад
Ati pedza madzi mu tikuvula chenga tikhapanamo
@MarthaJafali
@MarthaJafali 19 дней назад
Sure
@WitnessPhiri-zr9uf
@WitnessPhiri-zr9uf 19 дней назад
Aborn kalindo nde mumatiziwisa nkhani zambili mumatiyimilira koma or mukuyankhula anthuwa palibe chomwe akuva bwanji kuti kupangike mademo poti apo akuwona ngati tikusangalala ndi ulamuliro wawoo kukufunika ma demo kuti Ave ngati mumene anapangila azathu ku Kenya lizaini sangapange popanda ma demo 😢
@stanfordnsona
@stanfordnsona 18 дней назад
Kalindo umatitsekula maso
@mlimolubanda6348
@mlimolubanda6348 19 дней назад
The DC .....
@samuelgambatula2415
@samuelgambatula2415 19 дней назад
Tiyambe mademo.... Ulemu wathapo apa
@user-fq4kv8dj4t
@user-fq4kv8dj4t 19 дней назад
Zoona aliyense akavote opanda cha unzika basi nanga izizo nchilungamo
@Vascomw
@Vascomw 19 дней назад
Ndipo live eeee a police eeee akuwo jeza
@user-sv5yi9gt4u
@user-sv5yi9gt4u 20 дней назад
Zoona Born Kalindo auzeni ife tikuvutika kwambirii pa msewu kuno ku Kasungu chamama
@ZainuluNsalule
@ZainuluNsalule 19 дней назад
Good
@user-eh1mg3ww6d
@user-eh1mg3ww6d 20 дней назад
Koma m,chenga wa mulungu abale koma chakwela ambuye mutengeni watituza mokwanila mulungu mulangeni galu ameneu
Далее
A Michael Usi Inu Si A UTM - Lyton Mangochi
23:13
Просмотров 8 тыс.
EXCLUSIVE INTERVIEW WITH BON KALINDO
59:52
Просмотров 48 тыс.
Times Exclusive featuring Bon Kalindo - 6 January 2024
1:03:20