Bon amanena pomwe pasali bwino saimira mbali munthuyu kumavuta n kumumvetsa basi Utsiru of the year unachita ochakwera uja,iye uja amayenera kuikamasi patsogolo osati kumapangaso za ndale pomwe ali patsogolo zandale akanasiira ku opposition
Koditu mcp ija imapanga ndale zau savage ndinso za chikuwawe ngati zopanga ana, president ndi president yo zoona zija zachitika dzuro zija does it make sense even kwa anuwakewo ??? Ali ndi ndale zamangawa ndinso za uchikale just to proof ena ake wrong basi!!! Kulibe maturity uku olo pang'ono pena mpaka kumasilira andale amayiko ena okwima mu nzeru !!!
bwana dc,zayambikatu mmabank zomatipasa ma k 20 kwacha pamene ku mashop ma 20 kwa akukana.takakamizika lero ku tsandard bank kukanengo.ndalandila k3000 yama 20 kwacha,apano zikuyambika zakuzimbabwe.tivutika ndithu.
Koma nkuluyudi ndiopepera eti ndimayesa ndi yemweyu ndi alomwe anzake a pa social media kupusatu yekha kuzitsutsa alomwe anzake opusaonso kumamuyamikira mmalo momufunsa kuti nanga zija mumanena zija kuti wagwa zija bwanji. Koma poti zitsiru zokha zokha siziweruzana ndi chifukwa zitsiru zambiri pamenepa zingomuyamikira. Iweweme umanena zomwezo. Shame on you.
Komanso nanu a bon kalindo apa mukungofuna kuzipanga clean mesa dzulo mumati uncle anu che mapwesera adwala kwambiri mukumunena chakwera yemweyu and munalankhula kuti anthu mu nsika wa lunzu anakondwera kwambiri and munatitsikimizira kuti wadwaladi ndiye lero mukuti chani? Aaaah penatu anthu asiya kukupangani follow muzikhala ngati wa Bakili Muluzi tv sanayankhulepo kanthu koma inuyo ndi Ntanyiwa anthu ayamba kukutulukani ngati Skeffa sure
Bon Kalindo it shows that u are now interested in talking anything baseless because u present the same issue in mockery way in name of your uncle at the estate sarcastically .What do you want to tell us wadziwa liti kuti aliyense amadwala?