Malo anafela chilima or kukamangapo nyumba mzabwino kwambili imeneija inapweteka kwambili and mukumbukile ndege kusowa (10:00 am) president kulengeza muma 3 kosaka kuyamba chama 6 pm within 30 minutes kuyimisa kusaka kubwelela ati kukagona kaye kuzayambilaso tsiku losatila ,, akulu akulu or athu aja kanakhala kuti ali ndi moyo muthu wavulala pangozi ya ndenge akale 27hr asanalandile thandiizo sangakhale ndi moyo zosathe ngakhale ili ngozi yagalimoto muthu akagone popo anagwelapo mpana tsiku linalo aaaaaaa mpana pano palibeso wachosedwa tchito zongowoneselatu kuti zogwilizana chifukwa chilima anali osatila kwa msogoleli kusonyeza kuti kumwalila chakwela president bwezi ali chilima so chitetezo chake chimayenela kukhala ndendende cha nsogoleli waziko😭😭😭😭😭😭😭 na yachilima yokha kampeni wakwana
Bon Kalindo is indeed an activist of Malawi. He is spending his resources for Malwians,he is using his money to help the poor and fight for their rights and freedom. Thank you DR BON KALINDO for the job welldone for the voice of the poor who can't voice out for themselves. Bon Kalindo is speaking for all bitter Malawians no wonder anytime he asks people to come out for demonstrations they do it accordingly
Kkkkkkkk tinyamuleni a Kalindo tikagona konko ku Chikangawa,campaigning yose tikachitire konko 2025 Misonzi ya auntie Mary Chilima pa Chikangawa palibe masanje.Ndale zinthu zosiyilana mpakana kuphana. Mtendere apa palibe. 🤗🤗🤗🤗🤗🤗🤗
MA DEMO AKUFUNIKA VUTO NDI SUPPORT PALIBE OPPOSITION IMAFUNIKA IZIPEREKA NDALAMA KOMA KULI ZIIII KUSATA NDONDOMEKO PENA KUMAONGA ZITHU @@WisikiBlack-gj4gu
Despite all. Wolira samuseka pakwamwa that speech ya H.E the state president inali yabwino kwambiri and kuimila pamene paja zinali bwino. Komano izizi zomathana ndikalikonse kakambidwa mukuluza direction yet Boma ndilomweli, why fear ?? Iiiiih Bwana anyamata anufe tiuzeni tiyigwire mitima...
Chakwera ndi Boma lake samayenera kufikaso next year, Malawi akanakhala kuti ndi dziko lopanda mantha. Coz akukula ndi mantha ndi Mifuti koma kunjaku anthu zikasolobana Mfuti sayionaso mwakanthu or atafa bola iwowo atamenyera ufulu bas. Koma zikufunika umodzi osati masewera, mwina Chilima akanakhala kuti ali moyo tikanati tiona zinthu, but anyway the brave person are still alive let's unite to protect our country. This is too much
Koma MCP siizatheka ndithu.Kodi anthu a chipani cha MCP muzasiya liti nkhanza zomwe mukuwachitila a Malawi??Simukuganizabe za 30 years zaku opposition?Komatu dziwani kuti zomwe mukuchitazi inu a Chimwendo,inu a Kamajekete,iwe ochepa thupiwe koma dazi lili phuliphuli yemwe unapha Witica ndi mkulu wanuyo dziwani kuti matsiku anu ndi ochepa kwambiri.Muziwona
Apolice chikuwankhuza ndi chani? Ndipo Mary Chilima walakwisa chani? Kodi mesa akufuna kudziwa Chilungamo pa ifa ya Dr Saulos Chilima Ndi Anthu 8 anafa pa ngozi ya ndege kuchikangawa akuluakulu a MCP zimene mukufuna ndi chani mdziko muno munthu akanike kulira ifa ya mamuna wake?
Ndi zomvesa chisoni kuti press conference ya dzulo yomwe anapanga hule uyu waku Salima uja ndi uyu okhota mutuyu inali yonyansa kwambiri zoona mkumanena kuti a DPP amamenyana okhaokha yet anawatuma kuti avale makaka a DPP koma anawatuma ndi anyani amenewa.Koma iwe Chimwendo Banda ndi galu wako wachikaziyo ngati nthawi yakwana ya chisembwere muzikapangila ku Salima kwa uyo wa mutu ngati galimoto yochotsa manyiyo.Mwandinyansa nayo press yanu ndipo mudziwe kuti anthu anu omwe anakawononga zinthu za anthu a DPP azagwidwa ndipo choona chenicheni adzawulula anthu amene aja.
The spirit of Kamuzu Banda is with them these MCP murderers, but this time, they will face resistance from the people which our fathers and grand fathers failed to do and resulted in their self imposed exile
Zachisoni kwambili Kodi aja adakhapa a DPP ku Lilongwe aja mpaka pano bola silikuwamanga koma uyu chikwanje wa ku machinga masiku ochepa womangidwa koma mcp? Chipani choiipa kwambili