Mmmm but Born Kalindo you are really a true activist and you stand us though am a Zambian but l follow you. Please keep on updating us and never stop doing for the betterment of malawians.
Bakili muluzi tv , Limpopo tv ndi Bon Kalindo Tv tikuyamikeni chifukwa mukuyimila ife osawuka mwa jeniwini poti zipani zotsutsa zikugona kwambiri. More 🔥
Amfana nambala 1 Bon Kalindo 15:52 olimba mtima kwambiri mmalawi muno, Number 2 bakili muluzi tv, Number 3 NTANYIWA, Number 4 mutholo chikuni chautsi, Number 5 innocent banda, Anthu opusa kwambiri kumalawi ndi awa: Number 1 redson muklo, Number 2 ben longwe, Number 3 billy malata, Number 4 agape khombe, Number 5 layton mangoch, Number 6 ken msonda, Number 7 kondwani nankhumwa, Number 8 sungamoyo , Number 9.... too many to mention eish! , wina apitilize guys
Ursogoleri ndi mphatso osati sukulu kapena mpikisana. Ndimachita chidwi ndi mafumu akumudzi, samakhala anthu asukulu koma amaweruza milandu mwamzeru kuposa ma judge ama PhD koma too corrupt. Mr Kalindo you can be the president, tikusowa mtsogoleri wolimba mtima ndi wachilungamo
Mnthu wotiyankhulira ndi ameneyu the DC monga ine kapopangolo sindingayankhule koma zimandiwawa mmtima kuopa kumangidwa koma the DC alipo ndithu wotiyimirira kkkkk
Let's do something guys especially to as we are out of malawi country. Which means Malawian they don't have land. Now the land it's for goverment. What nonsense is this Mr president 😢😢