Тёмный
No video :(

Bon Kalindo Ndi Guru lake la Malawi first ayankhura izi pamene anapangitsa press conference lero 

Makosana
Подписаться 81 тыс.
Просмотров 39 тыс.
50% 1

Опубликовано:

 

28 авг 2024

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 172   
@user-mg5yy5hk9t
@user-mg5yy5hk9t Месяц назад
Anganga Alula malawi fist member all the way from mangochi mamatiyimilira mr big man keept up mangochi yosaopayo
@Moses51
@Moses51 Месяц назад
The Dc bon kalindo keep up update 💪💪🇲🇼🇲🇼💯 osawopa
@VungaQueen
@VungaQueen Месяц назад
Boni Kalindo munthu wotiyimilira 🔥🔥🔥
@user-ez8uk7py8n
@user-ez8uk7py8n Месяц назад
That is true it needs all Malawian to vote as long as he/ she is Malawian Mr president keep continue loving your poor people abd our country Malawi proud of you thanks
@user-eh1mg3ww6d
@user-eh1mg3ww6d Месяц назад
Ndipo athu inuyo tchito mukuigwila mulungu azikusungani ndi moyo maka Mr boni kalindo simutopa mwamangidwa kambili mbili mukanakhala wina bwezi mutatisiya ife athu osauka sikuti ndinu Muthu ovutika ayi koma mumasiya pogona pabwino zakudya zabwino kukagona Malo onyasa chifukwa Cha ife aphawi kuzipeleka m,sembe pokhapo mulungu adzikudalitsani ❤❤
@RiyemaDomybusiness
@RiyemaDomybusiness Месяц назад
Exactly 💯💯 bon amatiyimirila ampwawi
@user-eh1mg3ww6d
@user-eh1mg3ww6d Месяц назад
@@RiyemaDomybusiness sure tidziwapephelela ndithu athu amenewa
@esaMoha-dm4kj
@esaMoha-dm4kj Месяц назад
I respect your Mr nkalindo together with Malawian fest and the cautrry everyone DC is so powerful as well and you are always welcome to our team of Malawi wholld my Allah bless you always about the what happened with Malawian
@esaMoha-dm4kj
@esaMoha-dm4kj Месяц назад
I am a Malawi but now I'm in the sauth Africa estan about working on
@WysonJalamu
@WysonJalamu Месяц назад
Big up the DC osatopa, osafowoka, osawopa malawi ndi wathu uyu, tili limodzi pa nsewu basi.
@user-ml4bl2ll2g
@user-ml4bl2ll2g Месяц назад
Please please ife TIKUFUNA ufulu wathu wovota a MCP asauchotse ponamizira ma id, aliyense akuyenera kukavota popanda id
@Franklifo2217
@Franklifo2217 Месяц назад
Nzelu mulibe enanu! Anthu omwe mumalephelesa malawi kutukuka🙌
@hudycorex1893
@hudycorex1893 Месяц назад
Inu amzeru kwambiri?​@@Franklifo2217
@SamKaposa-i5c
@SamKaposa-i5c Месяц назад
Anzeru ndinuyo? ​@@Franklifo2217
@MussaHassani-zg1hm
@MussaHassani-zg1hm Месяц назад
This is our president kalindo thanks so much for your help Malawias
@DavieBinzih
@DavieBinzih Месяц назад
More fire mr kalindo we proudly of you keept up we love you
@WezzieChimuzi-ek7bk
@WezzieChimuzi-ek7bk Месяц назад
Good job my people Ambuye azikutetezelani ndi mwanzi wawo nthawi zonse ..
@chippakaribafox2865
@chippakaribafox2865 Месяц назад
Lets presure dem evo!....aluta continua!
@YousufMpunga
@YousufMpunga Месяц назад
Ndine Yusuf wakumangochi kmnso amalawi amene Ali kumaiko akunja apasidwe mwai wovota kuchokera kunja konko kumene ali
@patrickmacheso5062
@patrickmacheso5062 Месяц назад
That's true, we need to vote and choose the President that we want not this Manyaka Government, but the problem is Akazembe athu sathandiza or kuwapempha kuti atipatse mwayi ovota.
@FrankSpison-o7o
@FrankSpison-o7o Месяц назад
The Dccccccc Booooooooon kalindo inu nde anthu oti mzika zamalawi tizikupemphererani kwambili 🙏
@AnussaAlli
@AnussaAlli Месяц назад
Big up the DC Bon kalindo continue timakunyadlan❤❤❤❤❤❤🎉🎉
@ChristopherMadulira
@ChristopherMadulira Месяц назад
Congugulations Mr DC ntchito mukugwila anthu inu only God bless you ❤❤❤❤❤
@user-uf4db7im7d
@user-uf4db7im7d Месяц назад
Every malawian should be in a possession of ID, If the NRB is failing to reach all malawians for ID registration, you should expect Malawi to be on fire, because voting results will not be accepted, People have rights to vote for who they want not rigging.
@jogechawa6192
@jogechawa6192 Месяц назад
Bon Kalindo and malawi first our hope basi
@harrisonlowheat6569
@harrisonlowheat6569 Месяц назад
My president
@esaMoha-dm4kj
@esaMoha-dm4kj Месяц назад
I respect your nkalindo bisid ashankwela and everyone else has been in the path of mcp I don't respect anyone anymore because the people who keep and keeling Malawian people 2025 mashall Allah bless you nkalindo 😮😮😮
@user-uf4db7im7d
@user-uf4db7im7d Месяц назад
This government must go
@user-wi9pe2hz7e
@user-wi9pe2hz7e Месяц назад
Good move Malawi First ❤
@NellieKabvina
@NellieKabvina Месяц назад
Pa ziphatsopo ndie zikudabwitsa zikupezeka kuti anthu ambiri akumadziwa tsiku lokuti akumaliza kupanga ma ID,,,sakulengeza tsiku loyamba anthu ambiri akudandaula
@user-gs7wc3nx3q
@user-gs7wc3nx3q Месяц назад
yaa wa mcp ngati akunyasidwa ni boni karindo asavere khani zake ayi chonde ife anthu osauka tiyeni tizimuvera boni koma uzayime iwe boni tizakuvotere
@RemaniNkhoma
@RemaniNkhoma Месяц назад
boni karindo tingopita mawa bwanji pa sewu kuti agaru awa tiwakhawurise
@SamKaposa-i5c
@SamKaposa-i5c Месяц назад
Viva malawi first Richard mphepo umadziwa kuyankhula more fire dc
@FatimanickisJaffer
@FatimanickisJaffer Месяц назад
Wa mcp ngt born kalindo amakunyasa usamaver nkhan Zak iwey ndy opanda zelu ife tikufuna dziko libwerer ngt kal osat mukumakambo shem on you 😢😢😢😢
@KhalidwePentani-c6q
@KhalidwePentani-c6q Месяц назад
Iwe ndamene ukava ngat ine mbuz izi za duuu
@OdettaLowrence
@OdettaLowrence Месяц назад
Ulemu wanu Mr Born 🙏🙏🙏🙏
@amoschataika7440
@amoschataika7440 Месяц назад
Well done guys kpt up
@user-uv5rf4zt5q
@user-uv5rf4zt5q Месяц назад
Malawi first all the best u are representing poor people. To be honest Malawi is the poorest country in the world our leaders are selfish we are going backwards.
@BacklinebwanaliBwanali
@BacklinebwanaliBwanali Месяц назад
Akupatsen moyo was utali
@dawsonwaya4722
@dawsonwaya4722 Месяц назад
Za ziiiiiiiii munthu unalephera kuimirira constituency ndiye ukati amalawi osauka aaaa zangokuvutani Moya, .
@robenallie6985
@robenallie6985 Месяц назад
Ndizako zimenezo dc number 1
@FatimaAyami
@FatimaAyami Месяц назад
Vuto ndi bomalo iyeyo amangopanga imprement
@Samu-q3z
@Samu-q3z Месяц назад
Boni karido ndikatundu
@user-dq9oe8sp8k
@user-dq9oe8sp8k Месяц назад
Ifetu though tilibe ma ID kma tikazavota Angoona kuzinamidza agwapewa Fireeee the DC❤
@YohaneChitapini
@YohaneChitapini Месяц назад
Mumakwana ndipo ndinu nokha boss ndagwada ndikumvesela
@AndrewNyondo-ut3gk
@AndrewNyondo-ut3gk Месяц назад
King David bon kalindo the DC❤
@AlidWidon
@AlidWidon Месяц назад
Wosawopa bon kalindo tili limodxi 💪💪💪🔥🔥🔥👆👆
@Okalekale
@Okalekale 26 дней назад
Tikufuna tidziwe kuti ndi ndani amapanga sponsor gulu lanuli Mr.Kalindo?.The nation should know if you claim to advocate for transparence.
@MercyJohnsonkanchure
@MercyJohnsonkanchure Месяц назад
Mr Kalindo Mulungu azikupansani zeru zakuya ngati Solomon ❤
@MikeKoloko
@MikeKoloko Месяц назад
Mumatiimilira, big up
@RanaQari-py4bd
@RanaQari-py4bd Месяц назад
Mumakwana guys we love you all the time 🙏🙏🙏🔥🔥🔥🔥
@ShariffAbdul-m9t
@ShariffAbdul-m9t Месяц назад
I salute you
@usherjamson174
@usherjamson174 Месяц назад
Mulungu azikhala namu guy's 💪💪
@HusseinAdamLidezo
@HusseinAdamLidezo Месяц назад
Never give up guys let's see what happens
@lastonkandiyado4526
@lastonkandiyado4526 Месяц назад
Respect 🎉🎉🎉
@isabelmartin7567
@isabelmartin7567 Месяц назад
The DC ❤
@MuhammedNtaba
@MuhammedNtaba Месяц назад
❤❤❤ The DC
@ImanRashidi-so4oo
@ImanRashidi-so4oo Месяц назад
Congratulations mr DC
@KeftonChimaliro
@KeftonChimaliro Месяц назад
Iyayi zonsezitu akupangazi akufuna ndalama mtambo samachitaso chocho anango kuwapatsa zochita ndikungokhala duuu osayakhulaso amalawi anthuwo ndi amodzi Lucia's. Anayimba kale
@Lazarus-qo1sl
@Lazarus-qo1sl Месяц назад
Pick up guys chilungamo ndimwano
@patrickmacheso5062
@patrickmacheso5062 Месяц назад
Ndimayesa ngati mukhala kumbuyo kwa a name anu kkkkkkkk let's fight together, this country is belongs to all Malawians not MCP only.
@RanaQari-py4bd
@RanaQari-py4bd Месяц назад
🙏🙏🙏🙏🙏 Thnx good work
@GodisoneNoel
@GodisoneNoel Месяц назад
Asirikali achirendo muzikorathu zichepe mr DC
@user-bd5kw8oq1r
@user-bd5kw8oq1r Месяц назад
Akumangeni ngati mwaphwanya malamulo dala mbuli
@kenmasta
@kenmasta Месяц назад
Ndiye mmene akumamumangamo ndiye akumamupeza ndi milandu yanji,,,,..ndaletu zisakusokonezeni mchimwene andale amabwera amapita koma Malawi adzakhala yemweyu ndiye let's love Malawi.
@user-bd5kw8oq1r
@user-bd5kw8oq1r Месяц назад
@@kenmasta mwanena nokha awa asiyeni koma akanalankhula zinthu zambili ndi za against popeza ine ndinapanga nawo compain ndiye sanandipatse udindo awona, zimenezo ndi zabodza,chikuwawe sichimanga dziko amwe awa ndi a ndale musokonekera sayamika ndi ankhwidzi amafuna zawo ziwayendere kalindo akudya makobidi inu mukudya nawo 🤗🤗 ayi so bola yesu
@user-dy5bj9ck5e
@user-dy5bj9ck5e Месяц назад
The DCCC
@CostanceLalli
@CostanceLalli Месяц назад
Good move bafethu salute you
@GetrudeBanda-sd1yf
@GetrudeBanda-sd1yf Месяц назад
Only GOd Bless you DC
@SueWahna
@SueWahna Месяц назад
Big up Malawi first 💪💪
@TiyamikeMakande
@TiyamikeMakande 29 дней назад
Mumatiuankhulira ndinu bwana ,mutiyankhulireso za ndrama za masiye ku Capital hill Chaka chino nchachitatu ndrama sakutipatsa tikuvutika ndi ana
@HarrisonMangani
@HarrisonMangani Месяц назад
They need to address those issues other wise Mmmmm panunkha mphira
@PempheroMoleni
@PempheroMoleni Месяц назад
Firr the DC
@EliasMcray
@EliasMcray Месяц назад
Go go ahead
@frankiechasokoneza5802
@frankiechasokoneza5802 Месяц назад
Point of correction not guru lake koma Born kalindo ndi guru la Malawi 🇲🇼 first
@nelsonmhango7515
@nelsonmhango7515 Месяц назад
Inu ndi king
@gracetjomane-jj3ib
@gracetjomane-jj3ib Месяц назад
Kutundu uyu the DC❤❤❤❤❤❤
@YohaneChitapini
@YohaneChitapini Месяц назад
Guys inu musazafe mulungu azikudalisani
@user-tw2zf7bj3e
@user-tw2zf7bj3e Месяц назад
❤❤❤❤ guys
@AnockyDavidd
@AnockyDavidd Месяц назад
Congratulations to all
@Malambia
@Malambia Месяц назад
Mr kalindo ulemu wanu
@KhalidwePentani-c6q
@KhalidwePentani-c6q Месяц назад
Zopanda ntchito izo akalindo mumangofuna udindo ngat mungakwanitse kutumikila dziko aaaa zawumbuli
@Mervic-vm8eo
@Mervic-vm8eo Месяц назад
Wa MCP pamtu...
@InnocentKavalo
@InnocentKavalo Месяц назад
Zoona big umakwana dc
@ambeweburton
@ambeweburton Месяц назад
Timenyeleni nkhondo please mulungu imvani kulira kwathu
@PetroMatias
@PetroMatias Месяц назад
Amarawig fct muri nbi mfunbo zabwini timakuyamikirani
@Fridayasani
@Fridayasani Месяц назад
Osawopha Bon kalindo tikukupembela kwamulungu Kuti anzikala nawe kwina kulikonse komwe udziyenda
@ntandokazindzwana3083
@ntandokazindzwana3083 Месяц назад
Fire fire tili pa mbuso pa malawi oyambirira
@ritchardchakuma5725
@ritchardchakuma5725 Месяц назад
Apomwayikwanisa maiko enasaziwa Chichewa pakufunika ayaluke mbavazi 💯🔥🔥🔥🔥🔥
@Samu-q3z
@Samu-q3z Месяц назад
Zikomo boni karindo umatiyimilila big Kom amalawi sitimayamika
@chikoko-uj2tt
@chikoko-uj2tt Месяц назад
Salute 🫡 The DC
@user-dy4gc2hr5e
@user-dy4gc2hr5e Месяц назад
Good move
@HajaSande
@HajaSande Месяц назад
Zikomo kwambiri umawona patali
@AgnessChiwalo
@AgnessChiwalo Месяц назад
Your good man bon
@DavidJackson-ox4xm
@DavidJackson-ox4xm Месяц назад
The DC'S mwana woooopsa kwambiri chilungamo chiyende ngat madzi.
@AgnessChiwalo
@AgnessChiwalo Месяц назад
❤❤❤ good news
@JafaliAjusa-zg2xi
@JafaliAjusa-zg2xi Месяц назад
Respect Mr
@user-mh7cc8up4i
@user-mh7cc8up4i Месяц назад
❤❤❤💯💯🔥🔥🔥
@LukaJaulanchirwa
@LukaJaulanchirwa Месяц назад
You people you thinking harder that is good Diction thank chakwera is not thinking
@SolokingChimzy-yt7dj
@SolokingChimzy-yt7dj Месяц назад
Following with all my chidwi
@shephardlonex3371
@shephardlonex3371 Месяц назад
Booooooooni kalindo
@Mervic-vm8eo
@Mervic-vm8eo Месяц назад
Go konko bwana DC❤
@kurhikhoza8298
@kurhikhoza8298 Месяц назад
Tipiya pa sewu akapanda kuyakha
@sarahmphande6108
@sarahmphande6108 Месяц назад
I'm sure, the government you will grant our request
@PreciousKARINGANIZA
@PreciousKARINGANIZA Месяц назад
Tilikomweko
@shephardlonex3371
@shephardlonex3371 Месяц назад
Munene kuti ife ngati A Dpp
@MaryNgola
@MaryNgola Месяц назад
Mmene wafikira Malawi alipodi amene akumamuona uyu kt akupanga zolakwika? Iweyotu wa MCP nkana akukubowa
@JoshuaNyirongo
@JoshuaNyirongo Месяц назад
Go konko..
@PiusMpando
@PiusMpando Месяц назад
Tikukunyadilani kuno
@DaglasUseni
@DaglasUseni Месяц назад
Well
@kashmirmohakashmirmoha8659
@kashmirmohakashmirmoha8659 Месяц назад
Ulemu wanu DC😊😊
@dondamissonchdziwe3958
@dondamissonchdziwe3958 Месяц назад
Wina Aliyense amavota kumene adabwadwira Ndipo amfumu amadziwa Wanthu wao,apapa wina Ali yense azavota amene ali mbadwa ya Malawi zama I'D za chani?zopusa
@ShadreckChimaimba-l9y
@ShadreckChimaimba-l9y Месяц назад
Osatopa big
@user-ru6fc3qy5n
@user-ru6fc3qy5n Месяц назад
Zilibwino kwambili osaopa
Далее
娜美这是在浪费食物 #路飞#海贼王
00:20
Просмотров 3,9 млн
What is ChatGPT doing...and why does it work?
3:15:38
Просмотров 2,1 млн