Тёмный

BON KALINDO NDIYE KUTI SAMAOPA? NANGA ZOMWE WAYANKHULA LERO PA 16 AUGUST ZI TIZITI ALIBE MANTHA? 

Makosana
Подписаться 89 тыс.
Просмотров 67 тыс.
50% 1

Опубликовано:

 

11 сен 2024

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 138   
@KennedyPhiri-h9h
@KennedyPhiri-h9h 26 дней назад
❤❤ the DC president wa anthu osawuka 💪✊
@ThokoMbewe-k5x
@ThokoMbewe-k5x 26 дней назад
j
@LessonBester
@LessonBester 26 дней назад
Bon Kalindoo The DCCCCCCCCCC mwana oopsa kwambriiii
@MichaelPhiri-jn7bb
@MichaelPhiri-jn7bb 24 дня назад
😊
@sylvesteralfred8355
@sylvesteralfred8355 26 дней назад
Bon Kalindo simunthu wamba this guy is hero palibe kanthu kuti fans ina imamunyoza but he's true son of the soil yemwe amalifunira zabwino dziko lake
@augustMag
@augustMag 26 дней назад
President wa phawi ku Malawi kulibenso the DC Boooon Kalindo 🔥🔥 osatopa osafooka mumatiyimilira bwana
@MosesFanuel-k3u
@MosesFanuel-k3u 26 дней назад
Get well soon the DC
@YasenYasen-q9g
@YasenYasen-q9g 23 дня назад
Dc❤❤
@DonexKatuli
@DonexKatuli 26 дней назад
Powerful speech
@KellsDesderious
@KellsDesderious 26 дней назад
Machine the Dc ❤
@user-mm3wq8qp2q
@user-mm3wq8qp2q 26 дней назад
koma chakwera olo atafa palibe angadandaule afe galu ameneyi 😢😢
@ChisomoBisani
@ChisomoBisani 26 дней назад
Ndipo live
@chrisboyce2
@chrisboyce2 26 дней назад
Bon Elias Kalindo president oyamba wa anthu Osaukafe Kuno ku Malawi🔥🔥
@MillieMalakam
@MillieMalakam 26 дней назад
Bon kalindo God ahead u
@shaibuidriss2741
@shaibuidriss2741 25 дней назад
Kalindo deserve to be called President wa anthu osauka🙏
@SungananiBalaka-z4s
@SungananiBalaka-z4s 24 дня назад
Dan Lu ameneyo akudwalayo walupha oyimba azake
@SamsonMalefula-j4b
@SamsonMalefula-j4b 26 дней назад
Mwana woophya kwambiri the Dc
@DKMWALE-ew3lp
@DKMWALE-ew3lp 26 дней назад
Get well soon
@marryphili5419
@marryphili5419 26 дней назад
Mulungu ndi wamphamvu ndithu tiyembekezera phiri limeneri Kuti ligwe mwina mapiri enawo angapume
@ndalamaandrew
@ndalamaandrew 26 дней назад
Ndipo wayankhula mosanyengelera
@Phiricostina
@Phiricostina 21 день назад
Zoona angangaa enu Ake Boma ndife ndipo tiziziwaso zose zochitika mbomamo osat zoophwyezazo ayi🤷
@WestonGawaza
@WestonGawaza 26 дней назад
Saport kalindo ndikuonaziko likulira kuli ifa zosaikana Borne kalindo amaona patali kwambiri
@jackiendlovu9564
@jackiendlovu9564 25 дней назад
Get well soon the DC Mr Bon Kalindoooooooo
@MafavukeJere
@MafavukeJere 26 дней назад
Møre fire❤❤❤
@user-ty1vq9lq6w
@user-ty1vq9lq6w 26 дней назад
Adziwe zoti wamphamvu ndi Mulungu yekha chifukwa palinyengo zina ngakhale chuma chako sichingazakupulumutseni
@ThokoLungu-tq6pw
@ThokoLungu-tq6pw 25 дней назад
Amen 😢
@TyconSululuwa
@TyconSululuwa 26 дней назад
The Dc Bon kalindoooooo. Auzeni kuti nthawi yathera
@jezalakaphuka7325
@jezalakaphuka7325 26 дней назад
Booooooon Kalindoooooooooo the DC mwana owooooopsya kwambiri
@user-ew6xr2pd5l
@user-ew6xr2pd5l 26 дней назад
Get well soon the D C
@WillmotChiuimia-vr6ou
@WillmotChiuimia-vr6ou 26 дней назад
Yaa ndizowona zakee ndithu
@cassimyusuf6683
@cassimyusuf6683 26 дней назад
Ena omwe mukuziwa tiwuzeniko kuti phiri limeneli ndindani
@BittonRashid
@BittonRashid 26 дней назад
Yes bon kalido aimilileni makolo adyeletu masiku awasalilawao.
@GladesMhango
@GladesMhango 25 дней назад
President wathu wathu wa Anthu osaukafe🔥🔥
@EmmanuelMinyanga-gm4hv
@EmmanuelMinyanga-gm4hv 26 дней назад
Loud and clear
@Yusuf-j6c
@Yusuf-j6c 26 дней назад
I love you ❤️ Mr Dc
@KinziWindassoni
@KinziWindassoni 26 дней назад
The born kalindo the dc
@Amgwagwa
@Amgwagwa 26 дней назад
@PhilbertoChaimah
@PhilbertoChaimah 26 дней назад
Inenso ndikuvomereza kuti lingwe kumene😂😂😂😂
@MuhiyeBright
@MuhiyeBright 26 дней назад
Zoona bon kalindo more fire
@MaxwellSamuelChikapa
@MaxwellSamuelChikapa 26 дней назад
Umphawi sizinthu
@charleskayamba-s7c
@charleskayamba-s7c 25 дней назад
galu iwe panyapsko kalindo
@AlickChiphwanya
@AlickChiphwanya 25 дней назад
Chifiti ukugwa ndiwe chambacho chitha
@DRIPMIND-q3n
@DRIPMIND-q3n 21 день назад
Eeeh kwavuta
@TaweniChavulaKamwendo
@TaweniChavulaKamwendo 26 дней назад
Mmm 🤔🤔🤔🤔
@yotamumahomed1313
@yotamumahomed1313 26 дней назад
Sikale ay ndipompano tiphana
@TecksonKaima-dr6er
@TecksonKaima-dr6er 25 дней назад
Fireeeeeeeee
@JamesMisoya
@JamesMisoya 25 дней назад
More. Faya, osasiya
@CatherineDesire
@CatherineDesire 26 дней назад
Phiri la Dr Chikamgawa?👉iwe Bonnie 🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤸🤸🤸🤸🤸🙋salute sir🙄🤸🤸🤸🤸🤸🤸🤝
@ThokoLungu-tq6pw
@ThokoLungu-tq6pw 25 дней назад
Mulungu wathu saodzela, ulemu wanu the dc
@user-ul1fb4yn5o
@user-ul1fb4yn5o 25 дней назад
The DC mwana woooopsa kwambiri
@mercychirwa2147
@mercychirwa2147 26 дней назад
Boring government... They must get out of power
@user-eh1mg3ww6d
@user-eh1mg3ww6d 26 дней назад
Asiyeni abe momwe angabele kaya amaliza ndrama zose koma mulungu si Lazaro chomwe tikupepha mulungu atichotsele boma limeneli chifukwa siliva ndi golide ndi zake zaye yehova akaba zose mulungu azabwezeletsa kuposa zomwe abazo chomwe tikufuna ife ndi m, tendele mudziko lathu
@omarbindula
@omarbindula 26 дней назад
Mmm koma yah ziliko
@AlickChiphwanya
@AlickChiphwanya 25 дней назад
Chifiti ukugwa ndiwe chambacho chitha😢🎉😂😂😅🎉nkhope ngati galu
@MalonzoMazombwe
@MalonzoMazombwe 26 дней назад
Phiri ligwa nthawi yanji pls!! Tikuona kuchedwa mwina enafe mkupanga party... Phili iwe tagwa amalawi tipume.
@tanishadias
@tanishadias 26 дней назад
😂😂😂 my president the DC ❤
@JamesNyalubwe
@JamesNyalubwe 25 дней назад
Uyu eee
@moureenmolesi
@moureenmolesi 26 дней назад
ife tikudikira kuti zitero ndithu
@AUTONYMOUS-YARD-SOUND-ENTITY
@AUTONYMOUS-YARD-SOUND-ENTITY 26 дней назад
Makosana munakapanga focus zanu zja izi mungopa devalue kanthu kanuka za ziii asiyeni machanel andale azipanga zandale izi mulowa nazo pasi izi zofoila izi😂
@AllanJentala-g6h
@AllanJentala-g6h 26 дней назад
Kunali Mr Mtambo nawoso anayamba chonchi koma chomwe tingadziwe ndichakut onsewa ndi andale chabe akungofuna kutiphimba mmaso.
@LINELYBISANI
@LINELYBISANI 26 дней назад
Kodi akupatsidwa ma 50
@FebbieNjewa-g3k
@FebbieNjewa-g3k 26 дней назад
One day,,,,,ena adzanong'onezadi Bondo ndithu
@ELLENZAPS
@ELLENZAPS 26 дней назад
Inuyo bwana simukuyenera kudwara oyenera kudwara komaso kufa ndi chakwera mfiti
@emmanuelpiffano259
@emmanuelpiffano259 26 дней назад
Or JOSEPH NKASA adayimba kale kuti mudziwauza anawa MBIRI yadziko lawo Adanena ndithu zankhanza 😂😂😂😂😂
@JacquelineKanjedza
@JacquelineKanjedza 26 дней назад
Mcp ikuwinatube ndithu ndipo mwanena kale kuti ikubera
@Creslevison-vj2sl
@Creslevison-vj2sl 26 дней назад
Inu tsekani chabe kuchikamwako ,awinise ndamako,iya
@yotamumahomed1313
@yotamumahomed1313 26 дней назад
Sikale enafa tinatopa kale any mistake tili ready
@ThomasMwandila-tn7cf
@ThomasMwandila-tn7cf 26 дней назад
Wayamba mantha wonkhwima amadwara,osamatumbwa kumwamba kuri murungu akukuwonani
@NizigiyimanaChantal-c2p
@NizigiyimanaChantal-c2p 26 дней назад
@@ThomasMwandila-tn7cf choka idiyonyo m,dima umadana mkuunika vaziii vilibe na salt
@ShorayChimera
@ShorayChimera 25 дней назад
🎉
@ziwani3682
@ziwani3682 26 дней назад
The DC president wathu wathu wa ife amphawi
@jonaslabisonnthyola8036
@jonaslabisonnthyola8036 25 дней назад
Machine kung'alula osaoa freedom of expression launched 1996 Chakwera stop arresting people
@ChrisyMbewe
@ChrisyMbewe 26 дней назад
Awandi.akatundu.wawa.kuchikwedza uko
@EmmanuelMpalagule
@EmmanuelMpalagule 26 дней назад
Tasunga video kudikila kut phili limeneli ligwe ndipo tizaitulutsanxo video imeney phili lo likazagwa
@FrancisNyayi
@FrancisNyayi 26 дней назад
Winnico mcp ikazachoka usazankhare ndimpando wamba wayesesa
@ReginaMulipa
@ReginaMulipa 26 дней назад
Kalindo tamasuka ukutikuluwikatu chachitikaso ndichani 😂😂
@InnockishmaelAnafi
@InnockishmaelAnafi 26 дней назад
Respect 🙏 🫡 the dc
@user-fy7qk6kk5s
@user-fy7qk6kk5s 26 дней назад
M.C.P sikubwerela palibe chichita iwo D.P.P ikubwerela boma tidzidya nsima mamawa,masana,manzulo osati M.C.P ndichipani cha satanic
@user-fy7qk6kk5s
@user-fy7qk6kk5s 26 дней назад
Mo fire winiko umatimilira osadanda tilitonse
@MartinsilverChirwa-fv9wn
@MartinsilverChirwa-fv9wn 26 дней назад
❤❤
@CharlesBanda-pm2oe
@CharlesBanda-pm2oe 25 дней назад
Ndiachitsiru ichi wotsatira chitsiru amakhalanso chitsiru
@AlexKaunda-ny2eg
@AlexKaunda-ny2eg 26 дней назад
From 1964 ku malawi sikunakhalepo president wanzelu kaya mulungu dzikoli analipanga bwanji 😢
@Creslevison-vj2sl
@Creslevison-vj2sl 26 дней назад
Suli m'Malawi iwe and suyamikai waonekeratu
@temwekamlenje4358
@temwekamlenje4358 26 дней назад
-KUBA TSANKHO, KUPHA, FAMILY YONSE M"MBOMA . ENDLESS LIST. NDALE ZONYASA ZA KUMALAWI NGATII DZINA LAKE LOMWE NYASA LAND
@fredwchipatala
@fredwchipatala 25 дней назад
Koma uyu
@PetarKenedi
@PetarKenedi 26 дней назад
Phili ligweee💔
@ChrispinEdward
@ChrispinEdward 26 дней назад
Koma thyolo yokhayo ndi mukapanga chibwana tiyambinsa khondo yomwe mukufunayo mufunse mai joice banda mwa goliat.
@LimbanMedson
@LimbanMedson 26 дней назад
DC mukutiimililadi ife pitirizani zimenezi
@PgodfreyBanderouss
@PgodfreyBanderouss 26 дней назад
Mangochi anabwera dzulo pansika wa chiponde apolice amangotiopseza mmalo odyera,omwera anamanga anthu ochuluka
@user-gs7qk6lk7z
@user-gs7qk6lk7z 25 дней назад
The dangerous and deadly Child
@mphatsogondwe1836
@mphatsogondwe1836 25 дней назад
Ayi tikudikira ife tione phiri lokugwa
@LINELYBISANI
@LINELYBISANI 26 дней назад
Akutimanga mmasambatu
@SalahKamanga
@SalahKamanga 26 дней назад
Koma kalindo .eeee mavulutso awa anayamba ndinthu.anthu ambili anenelelapo.ambuye ndemwini wazonse
@AlickChiphwanya
@AlickChiphwanya 25 дней назад
Chitsilu chambachako
@user-le9su3mt7r
@user-le9su3mt7r 26 дней назад
Chakwela mbuzi
@VictorJaphet-z5l
@VictorJaphet-z5l 25 дней назад
Kodi akalindo mumati mumaimirila athu athu akendiakuti tiuzeni teve pano
@FrancisNyayi
@FrancisNyayi 26 дней назад
😢
@AnthonySadick-u1b
@AnthonySadick-u1b 26 дней назад
zofuna amavotera dala mcp
@TamikaKaponya
@TamikaKaponya 26 дней назад
Pemphero ndi pembedzero ligweeee ndithu
@ZuzeMbalame
@ZuzeMbalame 26 дней назад
Boma ili munkati tilivotere ndi inu nomwe.Ulendo uno mukutisankhiranso okuti timusankhe?Bola musazapwereketsenso aMalawi kachikena.
@azunguauskay4903
@azunguauskay4903 26 дней назад
Afe ndithuuu
@MussaAndreQuenessi
@MussaAndreQuenessi 26 дней назад
Auze mau the dc
@YusufGafa-s3j
@YusufGafa-s3j 26 дней назад
Bola ligwe mwachangu Phiri limeneli kkkkkkk
@PatriciaMbewe-xn7ke
@PatriciaMbewe-xn7ke 26 дней назад
Bola likhale phiri limene ndikuliganiziralo Malawi apume uyu😊
@SuzgoMkandawire-ss4kh
@SuzgoMkandawire-ss4kh 26 дней назад
Ineso ndikuganizira phiri Lina lake
@ChikumbutsoDzukwa
@ChikumbutsoDzukwa 26 дней назад
The DC 😅😂
@BlessingsNkhata-q7h
@BlessingsNkhata-q7h 26 дней назад
👍👍👍👍👍💕💕💕💕💕🙏🙏
@ZuzeMbalame
@ZuzeMbalame 26 дней назад
Phiri lokugwa lidzadziwika lokha 2025
@nelsonkajawo5176
@nelsonkajawo5176 26 дней назад
Amandinyasa
@FloraBanda-w7t
@FloraBanda-w7t 26 дней назад
😂😂😂just hit the head of the nail
Далее
Bacon на громкость
00:47
Просмотров 112 тыс.