Zanu za ufitizi musiye mukumupempherela ngati anakuuzani musiyeni Mary Chilima azipanga zake chonde, Mary Chilima don't allow that akupwetekani these people seems like anthu abwino then disaster chonde were ever you are musalole A Malawi kumbukilani za Chilima ananamizidwa lero Ali kuti nde these are false prophet please pass this to Mary I love her❤❤❤❤
Mfundo wakambayi ndi yofunika kuti asalore kuti yemwe wabwela kumene adzatenge mpando ayi. Eni utm tikuwaziwa patricia can be good president koma ndi obalalika okha amazizi sangalore
iremember this guy loves too much chakwera ndiye pano wasinthanso ngati Joseph phungu nkasa anthuwa they are hungry for money basi amene angawonere ma interview ake muona kuti amanena kuti chakwera ilove you my president