President wontani osakonda anthu ake pamene akulira, mmmmmm this is not good at all and yet tinamusankha kut azilamulira dziko koma relo tasanduka makape 😢😢😢😢
The enquiry must happen and thanks very much comrade Namiwa for the boldness... you aren't alone the Heaven is with you and will back u always coz you are standing on the truth...
God is our saviour,, koma tikufuna owinayooooo azawapase 24hrs after kulumbira abweze ndarama zathu zimene akubazi ndikumagulira oyimba ndi andale ,zilizathu kumene , what a shame, or aza wonetse nkhope ngati achisoni ,ayiiii atikwana,tifera Malawi wathu.
More fire 🔥 Namiwa azatitole chikangawa umakwana big man 👨 🔥 🙌 no matter what chikangawa waga bas will don't need this president again kkkkk chakwera anthu akukudikila ku chipiku pls 😀 👏 👍 😉 😳
He need to come and tell the nation and what I don't understand is that do we really need to pleade to him does he not know that commission of enquiry will solve or make people calm down and stand what happen.. Maybe he put his hand on this.. If they are scared of upcoming election they are going to lose anyway..
munthu uyuyo needs much support coz waima pachilunamo ..dzikoli crsly sililibwinotu...anthu akuvutika especially mamidzi umu uhm may God forgive&help us and hv mercy us👋🙏
Ndimadabwa ndi afitiwa Chikangawa akamabwera kuchokera kunja basi kumudikira KU airport. Kodi a malawi ena mitu yawo yikugwira ntchito bwino. Report la uchitsiru NDI Germany yoo
Amen inu mwasakhidwatu nfi mulungu,,chifukwa mfundo zanu zikulowa mtima mwa ina aliyese yemwe ali ndi mafuso ochuluka,,,komaso aziwe kuti ma plan okupha chilima anapanga ngati mbuli,,maso anu akuona patali
Kodi payifa ya olemekezaka mwatumidwa mwatumidwa or bwanji Ngati mkufuna za kafukufuku waku Germany simkukhula kapangeni wanu basi free koma munthu alindisiku lo badwa ndi la kufa