Ngati iwe ukuti anthu asamvere limpopo iwe amakutuma ndani kuti uzimvera ambiri timamukonda amatidziwitsa zobisika keep it up Mr. Mtanyiwa tikumvera pano pa Port Elizabeth RSA.
We don't need him, he just showed us how an settled he is, ndale za nkodzo tatopa nazo, take us seriously, we are not going to stand and look anymore, malawi up, n do right thing