Good news zoti presdent he's active and strong and unfortunately plan yakanika cz anthu omwe anatcheledwa a apa sanakodwemo congratulations kwa zipani zonse zosutsa posatenga nawo mbali pa fake news yomwe imazungulilayi cz wina waka akanapalamulapo ndithu, koma commission of inquiry tikuifuna ndithu
Abale wa DPP wa MCP tikukhal moyo ovutika tonse tiuzen ngt mitrngo ma shop ili yosiyan kuti iyi ya DPP iyi ya olemrkezeka a MCP tikukandra limodzi guyz
Kom ayi zikomo Mulungu zonse zi akuwona ndithu, kom a chakwera ayi zikomo. Opusa ndi ife A malawi , leo akuti boma ndilomweli bas akutelotu kulibe a.silikali kuno kulibe paja tu anagulidwa kale onse, chifukwa chake, akumagowonera ngati akuwonera mpira
Africa yonse ngati kuli Anthu oputsa ndi amalawi.ndipo,zichita chakwela kukhala ku maiko ena.bwezi,ataiwalidwa,kuti kunali family ya chakwela.koma,ndiye amalawi tatoledwa.
Kkkk abwanawa kunamanamaku nchiyani a chikangawawa ? Mwinatu ndikudwala eeehh!!? Aonjeza kunamaku a chikangawawa izi akuchitazi ndi nyansi.hoo!! Koma chilima iwe ; unatipititsa ku galena. Kwa sayana..😮😮😮
Bola wadziwadi kuti Amalawi mpk kuvina pa imfa yanga enafe tinadula ma ticket kuti tidzibwera kumudziko ndye basi sitikubwera til pano mpk 30years achoke kae