Тёмный
No video :(

DALITSO KABAMBE CHIFUKWA CHANI ADATULUKA DPP. 

HOT 265
Подписаться 76 тыс.
Просмотров 11 тыс.
50% 1

Опубликовано:

 

25 авг 2024

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 38   
@LovelyGalaxy-rb7yl
@LovelyGalaxy-rb7yl Месяц назад
Ayende bwno mwana waukape Awona ngati akapeza upele ku UTM, KOMA AXIWE KUTI NDIMWANA PANDALE 😅😅😅
@esaMoha-dm4kj
@esaMoha-dm4kj Месяц назад
ngani yankulla and yakt ankufunna nkumugulla ndi m c p nkoma saneena nkandu ankabambe
@user-lw4hw9ce4w
@user-lw4hw9ce4w Месяц назад
APM akuzasosora aswiswiri onse awo achoke alibe meaning ku dpp
@ephraimphalawala4720
@ephraimphalawala4720 Месяц назад
At this stage, we need to concentrate on National Interest and not political. Mavuto akula ku Malawi. Malawi must unite first to defeat MCP. That's top on the agenda. Politics ndi maudindo later.
@ThomasChiwaya-qx9mf
@ThomasChiwaya-qx9mf Месяц назад
Ine mau ambiri ndilibe kom Peter mulungu adalise amalaw tinaphuzir bas kut chikuni chachikulu chimasunga moto bas
@user-db3mh9wr9v
@user-db3mh9wr9v Месяц назад
Kabambe wachita bwino akhale President wa UTM basi best wishes DK
@ephraimphalawala4720
@ephraimphalawala4720 Месяц назад
DPP my vote
@lungisanishezi1023
@lungisanishezi1023 4 дня назад
Pali ndale zoopsya dpp ndi a katundu,akudzaphatikizana dpp ndi utm
@OmegahThipa
@OmegahThipa Месяц назад
Ngakhale anthu ambiri angayike maganizo awo motani, Ndichisankho chawo koma sikuti DPP ingagwedezeke palibe (APM 2025 boma akutenga
@JayoneAmbitious
@JayoneAmbitious Месяц назад
Kabambe apanga phuma peter anafunika awatenge akabambe kukhala vp wao after 2or 3 years akanapanga resin kuwasiila akabambeo km paokha sangawine
@user-nj4ob8jw6y
@user-nj4ob8jw6y Месяц назад
Mbabva iyiyi sidatuluke ku DPP, koma a Peter Mutharika amutuma kuti akayimile ku UTM cholinga ndichofuna kukatenga mabvoti a UTM kukapeleka ku DPP. Chonde a Malawi chenjerani
@gifttembo2306
@gifttembo2306 Месяц назад
DPP ndiyochenjera akudziwa kuti utm ikhala pa mgwirizano ndi dpp and akufuna adzachithetse mphamvu chipani cha utm in the coming yrs. pomuika madalitso kabambe as vice president
@adamu1287
@adamu1287 Месяц назад
Komano kunena zoona kabambe simunthu wandale
@user-zo3bf3ec3g
@user-zo3bf3ec3g Месяц назад
Muyendako bwino koko
@user-dc7qq9yz3v
@user-dc7qq9yz3v Месяц назад
Akamati mfulumila ndiumeneu
@user-lu8px7td6p
@user-lu8px7td6p Месяц назад
Akufuna udindo wa uprezident
@StiveKantiki
@StiveKantiki Месяц назад
Sanalakwise Ali Malawi momuno kulikose kumene angalowele akatumikila amalawi
@actuarialscience2283
@actuarialscience2283 Месяц назад
Ameneyu ndi wandale. I don't believe he has left DPP. Why? Here is the reason: HE ENDORSED APM.
@AndrewSimakweli
@AndrewSimakweli Месяц назад
Akabambe si andale
@user-hb2hr5oc9l
@user-hb2hr5oc9l Месяц назад
vuto anthu ambili sakufuna kunthandiza Malawi Koma Kuba ndalama Za boma akakhala pa udindo
@AlfredNazombe-me2ly
@AlfredNazombe-me2ly Месяц назад
Muononga dziko ndiinu amene achinyamata simuziwa chomwe mukuchita munasonkhana mu 2020 lero ndi izi mumazitenga ngat otsogola lero mukuzinzika
@bornface4786
@bornface4786 Месяц назад
This is not a right time for the Kabambe to move we can he doesn't lo Malawi
@user-vl8uw8mc3u
@user-vl8uw8mc3u Месяц назад
Kuthamangila udindo.saphulapo kanthu awa
@AntonyEdwinMuyila-ij4sx
@AntonyEdwinMuyila-ij4sx Месяц назад
There is no future for the youth in Dpp.
@user-bp1cu2rb4f
@user-bp1cu2rb4f Месяц назад
Kape iwe:Palibe chomwe uli.Galubwakoooo.Kachipanda ka peter bwenzi ulingati ndani?
@MatthewsJohn-kv8fj
@MatthewsJohn-kv8fj Месяц назад
Kuba bas ndizimene akufuna anthu kufinya mukaka ng'ombe yakuwanda kare
@eliffagondewe8214
@eliffagondewe8214 Месяц назад
Kabambe anatuluka kalekale ku Dpp, the thing is iyeyu Ali ngati nankhumwa amafuna president komaso ndiwa phuma nde no wonder palibe move apa ndi APM koma iyeyu wafuna you can see ma meeting ambiri adpp samapitako.. Ayende bwino
@yasitafuphiri-nw2he
@yasitafuphiri-nw2he Месяц назад
This is a plot for DPP 😢, APM will make him his running mate Kutuluka DPP ,kudzagwiranso ntchito ndi DPP yomweyo😮?? Pali nzeru apa??
@user-ml2vw1dc9c
@user-ml2vw1dc9c Месяц назад
Achinyamata akutulula kamba koti APM sapeleka mpata kwachinyamata ndiye ataya chikhulupililo
@JustineAdani
@JustineAdani Месяц назад
y⁷
@ChrisEnos-to5uv
@ChrisEnos-to5uv Месяц назад
Uyu sanatuluke ku Dpp achita kumutuma
@user-bz4fs6gv8v
@user-bz4fs6gv8v Месяц назад
Uyu amutuma serious
@JaneMoyo-ws2di
@JaneMoyo-ws2di Месяц назад
MOTi ku UTM kulibe oti angaimile u president? Zikukhala bwanji? UTM say NO to Kabambe ( UTM presidency).
@user-qp8kh2hj9o
@user-qp8kh2hj9o Месяц назад
Musavutike wakuuzani ndani zomwe mukunenazo
@user-qp8kh2hj9o
@user-qp8kh2hj9o Месяц назад
Aliko kabambe akutaya nthawi uyo
@user-mw3kj4qz7b
@user-mw3kj4qz7b Месяц назад
Let just Mary chilima stand guys to heal the heart s of Malawi
@user-nj4ob8jw6y
@user-nj4ob8jw6y Месяц назад
Kabambe ndiwe mbabva wakuba. Udaba ndarama zambiri, zankhani nkhani. If u think that u r clever, Ukunama. U will never become president of UTM, never. Ndiwe mwana wa ng'ono pa ndale ku Malawi kuno.
Далее
Музыкальные пародии
00:28
Просмотров 16 тыс.
AZIMAI A UTM KU AIRPORT KOWALANDILA ACHAKWERA
17:16
Просмотров 11 тыс.
Main News || 26/08/2024
Просмотров 194
When A Gang Leader Confronted Muhammad Ali
11:43
Просмотров 7 млн
A RICHARD CHIMWENDO BANDA KUNG'ALULA DPP
25:45
Просмотров 21 тыс.