Ulemelero wa malawi unachoka basi ....Bingu was q blessing and special gift to us malawians koma tinali mu m'dima.May forgive our country and give us someone like him😮
Good speech that people with good confidence will follow it forever, he died for body only but spirit for him still alive. Your body rest in peace almighty name of Jesus Christ Amen 🕊📖.............✍
ndine wa mcp koma pa bingu hmmm zinali nkhani zina mpaka 2009 mutu wanga unapenga bingu ngati anatumidwa ndi ambuye kudzatilamulira moti pazoipa zake zimene anthu amanena ine ndimaziika m'manja mwa mulungu coz satana anakwanitsa gawo lake kutitseka maso ndikumadana ndi utsogoleri wangilo
koma osati zinazi kungoonjezela kuipitsa mbili yake koma sindikukhulupira kudzaonaso tsogoleri ngati ameneyu ngakhale kamuzu sangafike pamzelu zake rest in piece baba