No mukulakwisa mukatelo kod mayiko enawa anthu samafa nakha anthu ena osayimba ndipo sanatchuke komwe anthu akumuzi samafa ndi infa za m'zizizi munganene kuti ndi bwana Lucia's Banda. No come on guys let's us learn to respect our favorite artist from our country because if we could no palibe Munthu yemwe angawalemekeze
My opinion Lucius sanakhalepo freedom fighter, unali chabe mukwiyo after bingu kuchoka ku UDF plus ma personal issues awo. Uyu kumapetoku atapasidwa udindo anangoti ziii kumanyambita misonkho ya amalawi
Sorry wapita mwachangu coz timadikila kt ayibe nyimbo mubo lilipoli koma ay zidko limatha bas kulimbanila nkazi kaya zichani tilibe nazo ntchito koma ife tingoti abuye wayakha bas RIP BINGU MUTHALIKA
Lucius banda dyera amafuna bazi koma anaona kuti bingu anali dolo sanamupatse 😂😂palibenso president angazafanane ndi bingu 😢😢alucius nanga lero muli kuti dziko lili pa moto ili