Тёмный

Hot Current Nduna Yoona Zachitetezo Cha Mdziko Wamukalipira Brian Banda 

MJ-MODAH MALAWI TV
Подписаться 13 тыс.
Просмотров 148 тыс.
50% 1

Опубликовано:

 

2 июл 2023

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 412   
@fedson2050
@fedson2050 11 месяцев назад
This Hot Current palibe chimene tatola ngat ife ma Listeners ndim'mene akuyakhira wakubayo
@bi8942
@bi8942 Год назад
A Brian tamubooleni mimbayo zikhale ng'oma mwina mimbayo iphwe kenako aziyankha . Ndichinduna cha mwano komanso Makati kwambiri. Changoseza mimba uko phwiiii kumapanga makani apa ngati ndi munthu ozindikira power ndi mbuzi ya munthu. Musazachiitanenso pa hot current kawiri , chizikhala ndi chakwera wakeyo kudikira kuchoka 2025. AIP ikuyenda bwino pakhomo pakwawo osati kwa amalawi anthu okuba Mulungu awalanga pompano anthu amenewa
@eliffagondewe8214
@eliffagondewe8214 Год назад
Kkkkkkk
@gavinpillay1253
@gavinpillay1253 7 месяцев назад
Galu wammpha dzikodi silingalongosoke ili nduna yaza chitetezo ikuyikiraso kumbuyo mbwererazi
@Extratremendouszeus
@Extratremendouszeus 14 дней назад
Chilbe nzeru chunkhumba chimenechi He uses his udindo wrongly
@zechariah265
@zechariah265 11 месяцев назад
This shows how hot current bases on issues with no tract evidence. Please Brian learn to be prepared for the program
@moseskavalo3304
@moseskavalo3304 Год назад
The nduna himself doesn't know how to argue,,too much emotions ķkkkkkkkkkk hahaha MCP is dangerous party indeed
@salimmkumakumakitombi-yc7pw
Kodi mlendo anali ndani pa Hot current imeneyi.... nduna yoonjedxera nkwiyo kwa A malawi
@user-eh1gn1nj9d
@user-eh1gn1nj9d 3 месяца назад
2025 ndi Chaka chamawa Why panic with this thing Let's go and work for our better
@MotivatedI
@MotivatedI Год назад
This is exactly how government lives in denial. Very interesting. All this time there is nothing you can point that the minister was able to answer. Like nothing
@Littlefair7
@Littlefair7 Год назад
He forgot we're in a democracy with his dictatorship mentality.
@rasulrayman4517
@rasulrayman4517 11 месяцев назад
Increasing the AIP beneficiaries will mean increase in poverty on household. This initiative is pathetic n we can't do better. Smallholder farmers are failing to extend their farm sizes due to high level of dependence on AIP same way as we depend much on foreign Aid. Teach more farmers on how they can manufacture mbeya fertilizer and do some extensions to their farms..
@thondoyaenterprise3795
@thondoyaenterprise3795 11 месяцев назад
Big up minister for taking these kids to school.
@Mbesa09
@Mbesa09 Год назад
I love The Hot Current and I always look forward to it. However, for so long, I have had issues with the show to where the hosts don't usually "think" of how important this show is to the students in colleges and universities world over. It is very difficult for a student to use what is said on this program as real evidence because the hosts take it as a discussion would have with someone at a bar. The hosts are barely ready for it and do not cite their outside sources, something that, maybe, morden universities do not accept. Much as I was not in agreement with The Minister, he seemed to challenge the hosts to produce evidence of what they wanted to ask him. I know the hosts, more specifically, Brian Banda, is educated enough, he should take this as a learning process and always cite his sources when asking the people 'he' invites to the show. This program has been a wonderful addition to Malawian programs but if it was done the right way, it could do much better than it has already done. Let members of parliament use it as a source of evidence in parliament. Let people sue one another using this program to change the face of Malawi. That cannot happen if the discussion is only done as a casual discussion. I was impressed seeing the minister showing his notes on things because he is an educated fellow who knows not to say something on a national television without evidence. Fox News in America paid big money for spreading false news without proper evidence. Please, Times Television, let your producers cite their stories or use the word "hypothetical" so some of us can really know if it's worth it or not.
@user-ux8bc6wy1i
@user-ux8bc6wy1i Год назад
😂
@tadalarhostinchiphwanya7891
Hundred percent I agree with u. I think it's high time Times find some guys well-informed on today's current affairs and issues to do so socials economics and governance.
@ezekielchihana2927
@ezekielchihana2927 11 месяцев назад
@@tadalarhostinchiphwanya7891true
@BenissoneErnesto-kn9bd
@BenissoneErnesto-kn9bd Год назад
Nduna imeneyi ndichisiru chamuthu ndposo ndisatana ndikufunisisa kt mulungu amulange panse pompa aziwe chimo lake akuphesa A2 osalakwa Aku ruwanda ndimuthu oipa kwambir ameneyi osamusekerera chisiru chamuthu ndiwadyera kwambir
@christopherbokosi514
@christopherbokosi514 7 месяцев назад
Nduna imeneyi ndimanyi
@kamuchirwa8940
@kamuchirwa8940 Год назад
The worst hot current, zikhale is too much into politics.
@geee7672
@geee7672 Год назад
...I really wonder why the anchor seems to be touting this guy a if he has some extra-ordinary skills and talent. What does nyama zikulu-zikulu mean? Lets not get excited and worship the same people who are promoting poverty amongst us. And I think we are micro-managed by Rwanda and collecting kickbacks by hunting refugees that he still seeks to kill. Well, I look at it as the most stupid thing for us to be proud of having more AIP beneficiaries. Instead of graduating these subsistent costly farmers into viable and productive citizens….on the US ambassador, I have never seen an ambassador who enjoys strange diplomatic protocol. He even finds himself in locations eating mandasi with locals, now, if he enjoys that freedom, then it is not a problem if he decides to walk into a media house as a news source. After all, the Malawi economy is surviving on debts, loans and credits that he approves every week, perhaps every day…The problem in Malawi is lack of ambitious leadership. We, currently do not have anyone fit for the position he holds in this government apart from the female ministers.
@user-uz6tr2db6g
@user-uz6tr2db6g 8 дней назад
Nzeru ilibe ndunayi
@KinziwindassoniKinzi
@KinziwindassoniKinzi 3 дня назад
Nzeru ilibe ndunayo ubwino wake 2025 mbava zikuchoka
@user-qs2tx7wt6g
@user-qs2tx7wt6g 4 дня назад
Mwakumana ndi nyama zikuluzikulu ndichochenjelaaa ichiii
@stanleymatolabanda5460
@stanleymatolabanda5460 Год назад
Useless cabinet minister who could not explain 🚮
@g_deonm5793
@g_deonm5793 11 месяцев назад
I like this . The minister is a very interesting political figure., He was able to spin out of questions and provide alternative view and he slipped out of Brian's popular "monkey wrench" questions.
@moseskavalo3304
@moseskavalo3304 Год назад
Now tell the minister about Quantitative and qualitative data, qualitative part of AIP is negative osamatinamiza apa
@languitoneelias9972
@languitoneelias9972 Год назад
Wakumana nawo anzako akhambi iwe Brian umaziona ngati ozindikila ukamafunsa mafunso amzako apa taziyankha osati zibwibwi its true pamafunika kumakamba zinthu uli ndi umboni osati kumangopeka nkhani or ena akangoyim a foni basi mwakhulupilira One day adzakutenga sukudziwa Kuti akukuuza zimenezoyo ndiwamalamulo becareful Brian de
@patricklimiton1023
@patricklimiton1023 11 месяцев назад
Inuyo kuzitenga kuzindikila ??
@leonardjika2100
@leonardjika2100 Год назад
A NEW VERSION WISE GOOD THINKER WILL GOVERN OUR LAND SO HELP ME GOD
@PeterThawi-jc7zl
@PeterThawi-jc7zl Год назад
This zikhale ng' oma has shown he is an intellectual....he can cite his sources...Brian Banda didn't come prepared...this time.i hope u do better next time around.this minister has killed the interview.
@lumbizayigadama-wd9ox
@lumbizayigadama-wd9ox 11 месяцев назад
No ndiwopoira
@louisbonongwe8537
@louisbonongwe8537 11 месяцев назад
Aaaaaa awanso
@lewisbonongwe8518
@lewisbonongwe8518 Год назад
Azikhale muziopa kumwamba uliposo moyo wina oposa umene mukubela anthuwu kudziko kuno, Musamale
@rashidsaid2232
@rashidsaid2232 3 месяца назад
Mr Zikhale Ng'oma udindo wakulilila sakudziwa chimene akunena
@user-hy4ty2ig1t
@user-hy4ty2ig1t 11 месяцев назад
I do understand a minister wants everything wth a prove coz amalawi timangoyankhula zongomva,,,is really nyama zikuluzikulu wth more intelligent I enjoy this kkk
@TrizaMaluwa-by9jw
@TrizaMaluwa-by9jw 3 дня назад
Andunawo nzeru alibe sakutha kuyankha funso
@vukanifracksonchinkonde7324
@vukanifracksonchinkonde7324 11 месяцев назад
The minister is intelligent,has really handled the hosts,he is really based on facts from my observation.A china Brian and pamkuku accept a defeat,the guy has really outweighed you.
@lloydchinyenye7704
@lloydchinyenye7704 11 месяцев назад
Exactly
@AustinChingoma-el4wo
@AustinChingoma-el4wo 11 месяцев назад
Exactly the host defeated
@moseskavalo3304
@moseskavalo3304 Год назад
We are sad Nation
@keithmlenga4657
@keithmlenga4657 11 месяцев назад
You, not we😅, I am not
@PeterThawi-jc7zl
@PeterThawi-jc7zl Год назад
Guys let's gather here for comments😂🤣🤣🤣
@dellingsmunthali2669
@dellingsmunthali2669 11 месяцев назад
Nyama zikulu-zimulu dada zikhare munthu murara chomeneeee ntchindii zikumwenererani chomene pa yankho rakut president azakhara chakwera motoooo💥💥💥💥💥💥
@augustinechibbalazi8897
@augustinechibbalazi8897 7 дней назад
Zinkhali Ng"oma is skilful at his work.Hon.Minister please,keep watch on illegal influx of immigrants here Malawi.
@SautsoBandah-lf4so
@SautsoBandah-lf4so Год назад
Guys u r losing control of your interview
@giftmakoyo1441
@giftmakoyo1441 2 дня назад
Mpaka ali ndi nyolo ndani aaaaa ife tiwope unyolo za ziiiiiiiiii
@BenissoneErnesto-kn9bd
@BenissoneErnesto-kn9bd Год назад
Watching from mozambique
@innocentissah2636
@innocentissah2636 Год назад
Nduna yoononga dziko kwambiri, katangale ali thoooo
@jacquesnsabiyaremye3166
@jacquesnsabiyaremye3166 Год назад
Akuti zinthu zitsika😢! Koma Chimunthu chi ndi cha Pokoso bwanji!!
@user-kr8bn1bb8c
@user-kr8bn1bb8c 6 дней назад
Nduna iyi ikhadzangolowatsa mboma it means dera lakero ladzaza zitsiru zokha zokha
@mercythom5868
@mercythom5868 7 месяцев назад
Poyamba ndimaona ngat Times imadana ndi DPP koma now ,,,,,ndazindikira kut it's only times yomwe tingaipange trust❤❤❤❤❤
@chrispinechirwa2655
@chrispinechirwa2655 3 дня назад
Uyu si nduna koma chigawenga😢😢😢 wofunsa mesa ndi mtola nkhani?
@joaquegerman2250
@joaquegerman2250 Год назад
Wadya 2.5 biliyoni ameneyo
@fedson2050
@fedson2050 11 месяцев назад
Ameneyo mumamuitaniranji wamakani ngat ameyo
@user-qs2tx7wt6g
@user-qs2tx7wt6g 4 дня назад
Koma akunena zoonaaa
@wakisawinga2744
@wakisawinga2744 7 дней назад
Now I know what he meant by being the strategist 😢😢😢😢
@Sabina-hw4js
@Sabina-hw4js 9 дней назад
People are sleeping for days without food yet them are having big stomachs
@dalisoulphiri3094
@dalisoulphiri3094 Год назад
Za trend zo munthu wakumudzi azidziwa bwanji abale?
@leonardmussah7902
@leonardmussah7902 Год назад
This has been one of the poorest interview so far, the minister has failed to take all the questions & frankly speaking he has acted as a football commentator
@user-hb1ff2wd8c
@user-hb1ff2wd8c 6 дней назад
Zikhale ndi mbuzi kma adzinga azake bas akukanika kuyakha mafutso ake amakani bas born kalindo must release 😮
@jeuzywandasigner4908
@jeuzywandasigner4908 7 дней назад
This is why you can't choose your family partner kukhala okuthandizila cz pakakhala vuto saangayankhule olo kusamala zaena apadela kuposa m'bale wake olo m'bale akulakwisa Malawi ali pa moto i hope wi know what to do next year to save our lovely country mayi Malawi 🇲🇼🙏🏾
@charlespaulbanda8136
@charlespaulbanda8136 11 месяцев назад
I like how nduna imeneyi pays attention when someone is on the flow
@ancientnkhata1137
@ancientnkhata1137 3 месяца назад
He pays attention to details Eish
@madalitsoonale5338
@madalitsoonale5338 11 месяцев назад
My Malawi 😭😭😭😭 y having useless minister like this one, useless government too😭😭😭😭😭
@mbumbajilowele6511
@mbumbajilowele6511 Месяц назад
Akuluwa angonenepa ndi achisilu kobasi😊
@chawackchinthenga6696
@chawackchinthenga6696 Год назад
Just remind you Chilima will never stand for 2025 presidential candidate 😢
@aronluka8086
@aronluka8086 Год назад
Duna imeneyi kodi imakhalira kuti zoti anthu adalandidwa ma 30 pn iyeyo sakuzidziwa koma ameneyi
@nickmumba2131
@nickmumba2131 11 месяцев назад
Kkkkkkkkk Nduna he doesn't know what's talking about
@user-nz1tf2ie6n
@user-nz1tf2ie6n 6 месяцев назад
Wotching from South Africa
@ephraimkadamika
@ephraimkadamika Год назад
Minster uyu ngozikonda
@DavieJames
@DavieJames Год назад
Let the minister answer questions not asking questions
@thomasbodo4099
@thomasbodo4099 11 месяцев назад
The Minister is not serious on what he is saying he cant say all is well with Malawians just becoz his familly and relatives are well
@user-eb2gi5dt6o
@user-eb2gi5dt6o 2 месяца назад
Koma ndunazi zikamana manyazi zilibe eish
@chikoko-uj2tt
@chikoko-uj2tt Год назад
Tell him mr Nanyon is a human being also
@user-pt8wb4vw6r
@user-pt8wb4vw6r Год назад
Azikhale akukwana pa udfend
@precioussauli2887
@precioussauli2887 Год назад
Honorable Minister is not able to take questions as asked. It is normal for AIP beneficiaries to increase as the population of the country is also growing extremely. And regardless of the increase of the beneficiaries, only a few out of the ones that were supposed to benefit this year benefited.
@James-uq6hv
@James-uq6hv 11 месяцев назад
Kkkkk kids are taken into a class, the kids have their sponsor, bravo to the minister Zikhale for the response trying to educate a bulutiwa
@wezzieneba9238
@wezzieneba9238 2 месяца назад
As for Brian and your colleague, I think you lost direction on the main theme of the program. Next time try to stick to what has been prepared, not flowing by the emotions of the visitor. You were taken up ending in no concrete and tangible issue at the end. Wishing you all the best. All in all, YOU ROCK GUYS!!!
@livemonkaposka3714
@livemonkaposka3714 Год назад
Ali busy kuba ndalama zobwerekazo
@alfredmankhwali-ku3ef
@alfredmankhwali-ku3ef 4 дня назад
Nkhani si nambalayo ayi , koma kodi ikumafikira onseo .
@francistonysanena5349
@francistonysanena5349 7 месяцев назад
Mr Based on facts😊...
@MphatsoSimiliwadi
@MphatsoSimiliwadi День назад
Very wise minister
@farmupmalawi
@farmupmalawi Год назад
Chisilu chimenecho chikundisekesa heavy
@MathewsLiwonde
@MathewsLiwonde 7 дней назад
Alibe nzerhu nduna yoipa iyi amapemphera mpingo wanji zonse chauta akuwona mulibe nthawi musamuka.
@loveborn1085
@loveborn1085 2 месяца назад
Two term ya president iri mu constitution ya Malawi Koma ngati president sanachite bwino ndipo anthu sakufuna kuti aimenso kachiwiri, anthu amasapota presidential candidate amene akumufuna nkuwina. Sindiye kuti president amene sanamalize 10 years yakeyo ndiye kuti apita ku khotitu ai.
@user-xz6uf8uk8t
@user-xz6uf8uk8t 4 месяца назад
Koma ngati a Brayan Banda ngati atolankhani amaimila athu chifukwa chifukwa chiyani amaka mba mokhalira mbali imodzi
@omarajibu860
@omarajibu860 Год назад
Economy ikhala bwino bwanji utanena kuti zinthu zilibwino?
@kestinmacheso-zc7cz
@kestinmacheso-zc7cz Год назад
Akugwilisa ntchito mphavu sakuyankha mafuso bwanji mbudz yanduna iyo
@vusoacquaron9084
@vusoacquaron9084 Год назад
2.5 billion dollars ya Kagame
@Sabina-hw4js
@Sabina-hw4js 9 дней назад
Whether kukwera or not people are suffering.
@MphatsoMgaiwa-sr7vn
@MphatsoMgaiwa-sr7vn 11 месяцев назад
Abrian mumacheza ndi chitsilu kwambili
@joshbosh6157
@joshbosh6157 10 месяцев назад
Brian, mkulu uyu ndiwachabechabe. Mayankhidwe ake ndi achabechabe, ndipo ndangotaya nthawi yanga pa program imeneyi
@awesomechannel7752
@awesomechannel7752 10 дней назад
This guy need an evidenve from you guys but was he producing the the documentantion ya constitution yo?
@raytavares2256
@raytavares2256 11 месяцев назад
Today Brine wanyachuka and exposed pa mtunda chibwibwi when did Brian start stammering? I realised how deflated he was. He was hiding what Brian has been doing and after seeing that he is being exposed he was like a flat tyre.
@MsosakaisiAdamson-pg6uv
@MsosakaisiAdamson-pg6uv 11 месяцев назад
Iyi ndi mbuzi yamunthu ,, brian muzititengera anthu azeru iwowo anadya ma 30pin afeteredxa mpaka pano sitikupindula nd boma limenero
@user-xd9fp2bw8j
@user-xd9fp2bw8j Год назад
mukungovutikatu a brian ndigaluyi dzikoli akuona ngati ndilamayi awo tikakumana komweko
@preciouskasusu1271
@preciouskasusu1271 Год назад
Kuyakhula kwa anduna kosapatsa chiyembekezo aaaa
@phillipstamaley7901
@phillipstamaley7901 10 месяцев назад
Brain wawoneka m'sana after kubisala m'mbatata
@user-wd7lk7nx7m
@user-wd7lk7nx7m 9 месяцев назад
Ku Malawi kulibe nduna yopanda zeru Ngati imeneyo galu weniweni
@dinganinedsontchongwe610
@dinganinedsontchongwe610 5 месяцев назад
The minister is using his position to defend himself but he is not true from what he is saying.
@user-jr9oh3ye9u
@user-jr9oh3ye9u 11 месяцев назад
Mximm zautsiru anduna anuwo akuyankhula zichani😊
@user-th4dg9bn9i
@user-th4dg9bn9i 11 месяцев назад
Thanks zikhale
@user-ix7pb6hk2w
@user-ix7pb6hk2w 5 месяцев назад
Nduna ya manya mavote mwana kale ndi a make koma sizitheka ife tikuziwa mulimonse
@GiftMakowa-k9f
@GiftMakowa-k9f 19 часов назад
Uyu panyapa xikhale Ng,oma kaye kutopa mawonekedwe
@FelixChimsNyirenda
@FelixChimsNyirenda 10 дней назад
Malawian politics is a dirty game and Malawian politicians ndiankhuluku kwambiri
@TimbaTv001
@TimbaTv001 8 дней назад
Thise brains are just old brain yomwe ilibe vision pa Malawi akudzatsaka pension ya executive. Aaa basi tikufunilani kufa konvetsa chison
@JamesChimera-hw1nv
@JamesChimera-hw1nv 2 месяца назад
Atola nkhani ahot current amakhala ndi mbali koma Chilungamo chimafunika osati kusokoneza anthu
@user-cn2mg2ee2p
@user-cn2mg2ee2p 8 месяцев назад
Mpakana 18 minutes musanayambe kumufunsa mafunso uyu ndigalu kwambili nduna yopusa kwambiri
@daviegunde5287
@daviegunde5287 Год назад
A nduna sakukwanira kukhala kuyimira boma pa program yi coz akukana kuyankha mafunso. Next time ndi bwino kukana kukhala pa program
@dellingsmunthali2669
@dellingsmunthali2669 11 месяцев назад
Mmm ayizikomo MOTi nthawi yomwe anthu akudandaura kut president akuyenda kwambiri osaziwa kut ondevu zamwai anali mugulu😃😃
@FranciscoMandawala
@FranciscoMandawala 12 часов назад
brian tawasiyan awa ndiopepela saziwa kut munthu amayankha with explanation.
@bugadada5752
@bugadada5752 4 дня назад
Zikhale Ngoma zinazo ayi 😂😂😂😌
@user-lr7ix1tm5b
@user-lr7ix1tm5b 7 месяцев назад
Anduna atuluka mimba itaphya ndimafunso eish Brian ndiwe wamwano😢
@WinerdJombo
@WinerdJombo 9 месяцев назад
Uyu akuti ife sitikuvutika aaaaa😢 pokhapo wandikwiyitsa kwabasi ndipo mapwa.... ake ndithu
@christopherbokosi514
@christopherbokosi514 7 месяцев назад
😂😂😂😂😂😂😂😂
@abubakrmustafa6105
@abubakrmustafa6105 Год назад
Zisikarit mwarephera bwana😜😜😜😜
@molicieeosama8877
@molicieeosama8877 Год назад
Duna yachibwana kwambili
@princedavidmapiri2876
@princedavidmapiri2876 Год назад
Nkulu ameneyu ngopusa zeedi musazamuitaneso akuzitenga ngati ngochenjera musiyeni azawona 2025
Далее
hot Current..Kumkuyu Vs Namalomba
1:14:23
Просмотров 39 тыс.
CRUISE 5 WITH PATRICIA KALIATI
59:03
Просмотров 155 тыс.
Times Exclusive with Nick Chakwera - 27 August 2022
1:02:22
Times Exclusive featuring Atupele Muluzi - 15 July 2023
1:06:57
KAFUKUFUKU PA IMFA YA ACHILIMA
30:18
Просмотров 85 тыс.
CRUISE 5 NYEMBANYEMBA   12 February 2023
1:01:33
Просмотров 174 тыс.
LUCIUS BANDA EXCLUSIVEINTERVIEW - 20 MAY 2021
56:54
Просмотров 70 тыс.
CYCLONE FREDDY FUNDRAISING DRAMA #malawi
1:31:45
Просмотров 423 тыс.