Тёмный

Ine Sindingasiye U Akitivizimu - Bon Kalindo 

Nyasa VoiceBox
Подписаться 28 тыс.
Просмотров 16 тыс.
50% 1

On Nyasa VoiceBox, speaking for the first time since his arrest and release on bail, Bon Kalindo, Chairperson of Malawi First, says that no amount of arrests and intimidation will stop him from engaging in activism.
Ku Nyasa VoiceBox, polankhula koyamba kuchokera pamene adamangidwa ndikutulutsidwa pa belo, Bon Kalindo, wapampando wa Malawi First, wati palibe kumangidwa kapena kuopsezedwa komwe kungamulepheretse kuchita ziwonetsero.
#malawi

Опубликовано:

 

29 сен 2024

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 43   
@CourageSydney
@CourageSydney 3 месяца назад
Kalindo atiimira ngati yesu❤❤
@AlicksonMakata
@AlicksonMakata 3 месяца назад
Koma English ya munthu uyu plz plz akuchititsa manyazi maiko akutiseka kwambiri simungathe kupeza njira zothetsera ai,ai tithandizeni boma tikuchititsidwa manyazi ndi munthu uyu wotembereredwa .
@LeendaDeborah2005
@LeendaDeborah2005 3 месяца назад
Hmmm dziko lino ndi la azungu??
@CONLEY265
@CONLEY265 3 месяца назад
Manyaz mukuchta ndinu kkkk mbuli yoyamba ndiwe
@CaptainNyenga
@CaptainNyenga 3 месяца назад
😂 usamaseke ife timasowa tulo kkkkkkk welcome back DC
@MordecaiKansily
@MordecaiKansily 3 месяца назад
Umakwana born kalindo chilungamo chioneke palibe zoospyezana nthawi imeneyo inatha ndi kamuzu
@Hazel-mq4wg
@Hazel-mq4wg 3 месяца назад
I proud of you bon kalindo
@NeemaMatewere
@NeemaMatewere 3 месяца назад
There's God in this post,all I can say is Amen
@pillarsongreenphiri7345
@pillarsongreenphiri7345 3 месяца назад
Born kalindo umatha aise and osapanga matha iwe
@JunaKananji
@JunaKananji 3 месяца назад
Karido ❤❤❤❤
@tebogomaake9375
@tebogomaake9375 3 месяца назад
a bwana pitilizani nyimbo yo Lazaro wa Bethany nice song 😂
@josephykwendah2210
@josephykwendah2210 3 месяца назад
Bon kalindo ndi mwana oopswa kwambiri
@twavysibale4751
@twavysibale4751 3 месяца назад
Kodi akumachita kumulanda maphone?
@dinahmunthali5324
@dinahmunthali5324 3 месяца назад
Zonsezo nchabe koma nyimbo yooo 😂😂😂😂
@ibrahimalfred6539
@ibrahimalfred6539 3 месяца назад
Mr kalindo he is the hero of malawi what kind of a person who does not give up even if the arrest him 1M times he is a person who care about other people's pls Malawian let support this person please because if it's was you and I we was gonna give up let think Malawian please
@LeendaDeborah2005
@LeendaDeborah2005 3 месяца назад
👏🏽👏🏽👏🏽👏🏽👏🏽zoona ndithu
@bensonjamu4038
@bensonjamu4038 3 месяца назад
Booooorn Kalindooooo
@sithembilechatata1128
@sithembilechatata1128 3 месяца назад
Kumasiyanisaso ndi misala
@JonathanChimwaza
@JonathanChimwaza 3 месяца назад
Osaopa koma tiima pachulungamo
@UmodziBalalah
@UmodziBalalah 3 месяца назад
DC mwana ooopsa kwambiri 😂😂
@MordecaiKansily
@MordecaiKansily 3 месяца назад
Umakwana kalindo
@JosephLambiki
@JosephLambiki 3 месяца назад
😂😂😂😂😂
@StainDandize
@StainDandize 3 месяца назад
😂😂😂
@BilalAliyah-k1f
@BilalAliyah-k1f 3 месяца назад
😂😂😂
@ThomsonJackson-w6f
@ThomsonJackson-w6f 3 месяца назад
❤❤
@UmodziBalalah
@UmodziBalalah 3 месяца назад
😂
@limbiechisaka1027
@limbiechisaka1027 3 месяца назад
Koma mwana ameneyo ngati alikodi akamupeza anthu amupha kaya.
@MishaJames-zn5hp
@MishaJames-zn5hp 3 месяца назад
Tate wathu
@CheloyaaChikwatuu-ob2mt
@CheloyaaChikwatuu-ob2mt 3 месяца назад
💝❤❤❤ D C
@AbdulHameedNgulinga
@AbdulHameedNgulinga 3 месяца назад
Osawasiya amenewa tiye nawo winiko
@gladysbonongwe1038
@gladysbonongwe1038 3 месяца назад
More fire
@InnocentCcij
@InnocentCcij 3 месяца назад
Ndinu hero boss I give you a respect ❤
@PreciousTsogolani
@PreciousTsogolani 3 месяца назад
Abwana donate more kwa anthuwa akuoneka kuti umphawi wavuta
@vanessangomwa7535
@vanessangomwa7535 3 месяца назад
😂😂😂😂😂😂😂
@TooNajahInsideKoshah
@TooNajahInsideKoshah 3 месяца назад
Mumakwana popanga Donate kuboma lamalawi Mr bon kalindo
@ivychithyoka1551
@ivychithyoka1551 3 месяца назад
Bon Kalindo ,The DC!!!!!!!
@Estermogha
@Estermogha 3 месяца назад
Tianazoni present wathu
@MpumeleloZungu
@MpumeleloZungu 3 месяца назад
Umakwana kalindo......
@CONLEY265
@CONLEY265 3 месяца назад
😂😂😂😂Kalindo eish
@YUSUFBOBO-in5dm
@YUSUFBOBO-in5dm 3 месяца назад
Kalindo wooye
@VitumbikoChinoko-n7x
@VitumbikoChinoko-n7x 3 месяца назад
😘😘😘
@InnocentCcij
@InnocentCcij 3 месяца назад
❤Fire
@Mistermpandokhwinda
@Mistermpandokhwinda 3 месяца назад
Katswiri
Далее
Chakwera Will Not Win The Elections - Samuel Lwara
22:19
Главное рыба есть, а воды нет..
00:54
КВН 2024 Встреча выпускников
2:00:41
Ine Sindingakhale Pamodzi Ndi MCP - Bon Kalindo
18:14
Просмотров 2,8 тыс.
CRUISE 5 WITH BON KALINDO   PART 1
55:17
Просмотров 120 тыс.
EXCLUSIVE INTERVIEW WITH BON KALINDO
59:52
Просмотров 90 тыс.
US-Tanzania Tech Challenge
2:29:27
Просмотров 1,6 тыс.
Главное рыба есть, а воды нет..
00:54