Mukuyankhula motumbwa chifukwa mulimpogwila anzanu akusowatu zochita ku Malawi ko thats why akukayesa mwayi .Imeneyo campaign or you are preaching mawu a Mulungu
Malawi ali ndi vuto amafuna Kuti azawo asakhale pa bwino ayi,maboza okhaokha,thawi zogwadira Muthu kapena mupingo zinatha,tiyeni tiwafunele zabwino,go to South Africa ask Malawian people there, about work u can understand
Nanga zikugwirizana ndi chipulumutso . Lalikirani Za Ufumu wakumwamba . This is religion not Christianity. A Christian is led by the holy spirit . You preach by His will . Not by your sense of knowledge.