Chawezi Banda! Chawezi Banda! Chawezi Banda! How many times have I called you? Ask yourself where is Steven Maseya, where is Hope Chisanu. Nawonso ankatero kazikangogwirani ntchito yanu osamalowerela nkhani za ndale muzanong'oneza bondo. I didn't expect this from you Deus big time!
Chawezi anayamba bwino koma waonetsa kuti akudya za MCP. Kunena zoona Boma komanso ACB lilibe umboni okwanira kuti Chilima ndi wa corruption kapena Chakwera akuopa kuti apangidwa involved no matter kuti constitution ikuwateteza. Pa za Nankhumwa,DPP siinampilingitse koma amaoneka kuti anali ndi dyera lolamulira DPP nthawi isanakwane. Nankhumwa anabweretsa mgawikano mu DPP ndipo at the end anaonetsa kuti MCP bought him to bring confusion in DPP. Chawezi nawenso ndiozitsata koma uli mbali ya Chakwera.Supposed to be Neutral ndie poti mwati the program is sponsored exactly we know the Sponsor.
Chawezie ndiwe zoba what you should know is dpp government siinamangeko vice president chifukwa nthawi ya dpp kunalibe katangale ngati pano and you should refrain from attacking APM and dpp in almost all your every program
Chawezi ukuoneka ngati ndiwe pro MCP. When analysing try to use logic, do not comment ngati ndiwe party loyalist. Nankhumwa sadekha koma is dull. Chawezi your profession is compromised.
You must be jocking?? Koma mwazidyatu za MCP moti really Chawezi you can go so low and say live on tv that we are on the right path when it comes to corruption? Like seriously?? what a shame. Am so disappointed in you personally.