Mr.Kamulepo and this man Bon Kalindo,we don’t need Chakwera to proceed ruling this country up to November 2024.Please let’s organise tough strategies for him to step down.Bravo Kamulepo,Bravo Bon Kalindo
To be honest Malawi is going backwards people voted for Tonse alliance for hoping better life but federal system of government is the only way enough is enough.
Mr. Kamlepo Kaluwa, ndine Mponda kuno, ndidakali kuno ku Soweto, but a'm taking my pension next year, I will be meeting you next year. I think u remember, Japheth Nkhoma, Mr. Kanyongolo, Mr. Maseko all from Soweto
Take that word .they will not manage what is coming , i believe something big is coming i say it again something big is coming anyamata soon azuka ndipo it will be like Kenya 🇰🇪 anthu akatopa amatopa kuti topi kungotopa basi
Inu a Nonse Alliance ndinu mwaba cilungamo CA a Malawi . Leromukamaphedwa, nokha mukudabwa! Mumanena kuti Peter wadaba vote za Chilima ndi za Chakwera. Za Atupere ndi ena Peter sanabe. Bwanji bwalo lamirandu linalola zipani 9 zikhale pamodzi? Tsono lero mukuti mukubwerera ku Cipani cimodzi? Pamenepa opusa ndani?
Mcp yapalamula chitedze,,, when you pray for the rain deal with the mad too,, Chakwera umva madzi chaka chino ine Mulungu anandiyankhula momveka bwino kuti akuvupula kowopsya,uyaluka,, ngati ungathe umupatse makobili Mulunguyo tiwone, my God is exposing you this year you are finished,, awa ma prophet mwawapatsa ndalamawa akukunamizani ask me i will tell you what the Mighty Lord God said,, your judgement has just begun enjoy it
Once an eagle always an eagle. We believe in you the real freedom fighter legend Kamulepo Kaluwa. We're going to vote without their stupid ID'S protocol