Komanso kulemera pamaso pa kamuzu zizinali zocheza ayi ameneyu adzafotokoze bwino part 2 akunenayo akhatiuza kuti a Gadama ndi amzawo aja akhati mukutipheranji akuwakhoma ndi hamala iye anali kuti ????????
So You mean Bakili Muluzi anapeza scholarship yokaphunzira ma college akunja mzaka za mma 1960 ali osaphunzira? I think mbuli ndi iweyo palibe chomwe ukudziwa chokhudza Bakili Muluzi.
Bakili muluzi ankagwira ntchito ngati clerk wa Ku court poyambilira penipeni. Ndie ukati anali osaphunzira ukutanthauza chani. Moreover bakili muluzi anali principal wa Nansawa technical college, kamuzu banda anamusankha kukhala MP komanso nduna ya boma pa nthawi yomwe anali mphunzitsi wamkulu wa pa Nansawa technical. Ndie ukati anali mbuli ukutanthauza chani. He was even minister of education mnthawi ya kamuzu. Mwina unangomvera ma propaganda a anthu kuti bakili muluzi anali osaphunzira iwe
@@alankasiya7329 kutanthauza kuti ukutsutsa kuti Bakili Muluzi sanagwire ntchito Ku khothi ngati clerk? Sanagwire ntchito ngati principal pa nansawa college? Sanapite kunja mzaka za mma 1960 kukaphunzira ma college a ku Denmark ndi ku Britain? Sanakhalepo minister of education mnthawi ya Kamuzu? Ukamati we were mis informed what do you mean? Ife tikunena zoona zenizeni zooneka ndi maso pomwe iwe ukunena zongomvera anthu za mabodza. Bakili Muluzi was even minister of portfolio mnthawi ya Kamuzu, and you think munthu angakhale minister of portfolio ali mbuli?
@@charlesmuyaya8839 maphunzilo amene anenedwa kuti anaphuzilawo that's what I'm against kale anthu ankamphuzila up to STD 5 nkumapeza ntchito ngakhale Aleke Banda anali minister nthawi ya kamuzu koma anali ndi jc . Ngakhale ma minister ambiri muthawi ya amuluzi anali osaphunzira. Kukhala minister sikuphunzira