Тёмный

Mbiri ya Dr Bakili Muluzi PART 1 

Bakili Muluzi TV
Подписаться 112 тыс.
Просмотров 93 тыс.
50% 1

Dr Bakili Muluzi ndi president wakale wa dziko la Malawi🇲🇼

Опубликовано:

 

22 янв 2021

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 77   
@fanizoabrahamchimbalanga6529
@fanizoabrahamchimbalanga6529 3 года назад
God bless bakili muluzi adathandiza amalawi kuwachotsa muumbuli waukulu
@amisichiphiri8227
@amisichiphiri8227 2 года назад
Kwambiri anatisambisa kumanso
@ImeedFranck
@ImeedFranck Месяц назад
😂😂😂😂😂😂
@bonjechaula8542
@bonjechaula8542 3 года назад
1981 bakili muluzi anaba ndalama za makad a MCP, mbava yeni yeni.
@Littlefair7
@Littlefair7 3 года назад
Kodi achair kuba anayambira patali eti? Mpaka kuba £6? Ndi kudzasololanso K1.9bn
@franciskaponda8608
@franciskaponda8608 3 года назад
Komanso kulemera pamaso pa kamuzu zizinali zocheza ayi ameneyu adzafotokoze bwino part 2 akunenayo akhatiuza kuti a Gadama ndi amzawo aja akhati mukutipheranji akuwakhoma ndi hamala iye anali kuti ????????
@mosesharoldngolombe
@mosesharoldngolombe 10 месяцев назад
Anyamata apa town❤
@FrancisNyayi
@FrancisNyayi 18 дней назад
Better anatipangisa tinkhare ndi maphone pano tikunvera pa phone good man
@lastlevel1999
@lastlevel1999 3 года назад
We will waiting for part 2
@davidbulla9390
@davidbulla9390 Год назад
Wonderful di
@AbdulsharifulKalipinde-m6u
@AbdulsharifulKalipinde-m6u 2 дня назад
Kuba kwa nzeru Kopanda kudandaula munthu wina aliyese Osati kuba kuyambira anthu onse a boma
@maongambonde1004
@maongambonde1004 3 года назад
Kamuzu inali mbalame
@EsnatSayiwala
@EsnatSayiwala 2 месяца назад
Wow ❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
@ibrahimyusufu3927
@ibrahimyusufu3927 2 года назад
FDU... NICE
@fredrickkhebozy6683
@fredrickkhebozy6683 3 года назад
Well done sir
@alexjeremanuel2541
@alexjeremanuel2541 Год назад
I like this man chair
@charlesmuyaya8839
@charlesmuyaya8839 3 года назад
Thanks for the info. Keep it up
@sharifsaidi6706
@sharifsaidi6706 3 года назад
Please upload it, we are waiting
@bashirbanda6519
@bashirbanda6519 3 года назад
Timakunyadilani tiphuzila zambili kuchokela kwainu
@olipamaseko2693
@olipamaseko2693 Год назад
Narrator sangayankhule zonse zoipa za Bakili ndi abwana ake amenewa agwira ntchito ku Bakili muluzi tv
@taongahshaba
@taongahshaba Месяц назад
❤❤❤❤❤❤
@hardworkkayuza6353
@hardworkkayuza6353 21 день назад
Anyamata othamanga pa town
@umaliisah6920
@umaliisah6920 3 года назад
Fast part 2
@BashiruIshumael
@BashiruIshumael 8 дней назад
Wachiyao kwao kutulutsa wangalutsa
@user-we4ue5dc4e
@user-we4ue5dc4e 2 месяца назад
Anatiombola ,palibe analimba mtima nthawi imeneija.
@olipamaseko2693
@olipamaseko2693 Год назад
Bakili anali wamabodza kwambiri ndi amene anapangitsa kuti dzikoli lisauke kwambiri atagulitsa ma company onse a boma ndalama ndi kunyambita
@nkhwaziaeros1845
@nkhwaziaeros1845 2 года назад
nkhani ya mcp or bakili muluzi? adha inu penapake simumakhala objective with your narration
@shabbanmatewere439
@shabbanmatewere439 3 года назад
Dr Muluzi /kuchitekete
@lovemapwina6661
@lovemapwina6661 3 года назад
Following
@yamikanimkanthama4354
@yamikanimkanthama4354 4 месяца назад
APA NDe mwakwanilisaatu
@richardnkosi1934
@richardnkosi1934 3 года назад
Anagwetsa dziko la Malawi koposa Mafia wakuba
@mouricesaidi5348
@mouricesaidi5348 3 года назад
oky?????? zako zimenezo
@m00n_pInK
@m00n_pInK 3 года назад
kuti malawi ilowe pansi ndi bakili akuluwa amakondela zoika apa.
@warlubie
@warlubie 2 года назад
I do owe his car from 1998
@humairamalombe295
@humairamalombe295 8 месяцев назад
Nawoni osawasiya abwele poyela masatanawa
@KametaMasina
@KametaMasina 9 месяцев назад
❤❤❤❤
@alexanderkaunda9554
@alexanderkaunda9554 3 года назад
Kudzindikira kodula dziwalo
@allanmakwiti5145
@allanmakwiti5145 3 года назад
Ali ndi ana angati?
@hurdgejanatu1812
@hurdgejanatu1812 Месяц назад
Wachi Yao uwejo
@luciuschigoga2607
@luciuschigoga2607 3 года назад
Nkhani ili apa nnja Bakili or MCP? Koma akulu awa😂😂😂😂😂😘
@charlesmuyaya8839
@charlesmuyaya8839 3 года назад
Monga wekha sukuona kuti zikugwirizana? The narrator akufotokoza zomwe zinachitika kuti Muluzi apange resign.
@olipamaseko2693
@olipamaseko2693 Год назад
Bakili anali nduna ya Kamuzu zonse zoipa amapangira limodzi ndi Bakili sikuti Kamuzu amapha yekha anthuwa ayi
@uthmanalex
@uthmanalex 3 месяца назад
@@charlesmuyaya8839 chisiyeni amwene ndichitsiru they miss understanding amavera alipanjinga 🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣
@PeaceIslsm
@PeaceIslsm 14 дней назад
DPP❤❤❤❤❤
@PeaceIslsm
@PeaceIslsm 14 дней назад
Bhobho 😊
@PeaceIslsm
@PeaceIslsm 14 дней назад
mt😂😂😂😂😂
@olipamaseko2693
@olipamaseko2693 Год назад
Or pano ma school achisilamu Ali kuti? Awa akungoyankhula za mmutu mwao pano ndi ndani anaphunzirapo sukulu ya chisilamu ndipo zili kuti?
@user-cy5ko2qw5d
@user-cy5ko2qw5d 4 месяца назад
Masukulu achisilamu kumalawi sukuwaziwa😂😂😂
@m00n_pInK
@m00n_pInK 3 года назад
zokuti anapha matafale simunanenetu amwene anakakhala wa mcp bwezi ndizoipa zomwe mutanena.
@charlesmuyaya8839
@charlesmuyaya8839 3 года назад
Nkhani ya Matafale anthu ambiri munayimva mukuthamanga. Amene anakasuma Ku polisi kuti Matafale wamubera katundu wake anali O.G ISSA. Matafale anapita Ku shop kwake ndi marasta anzake nkukaphwanya katundu yense. Sizikugwirizana ndi Bakili Muluzi izi.
@chikondimwale7517
@chikondimwale7517 3 года назад
Ati "mfana upange resign"
@goldencitytowerent9554
@goldencitytowerent9554 3 года назад
Hahaha eyetu
@hopesonnsongolo1049
@hopesonnsongolo1049 Год назад
Bakili ndi dolo
@chimwemwechimwaza7512
@chimwemwechimwaza7512 3 года назад
Bakili ndi mbuz imoz ya president mu africa opanda vision aaah tisabise apa
@m00n_pInK
@m00n_pInK 3 года назад
zoonadi abraz.
@BashiruIshumael
@BashiruIshumael 8 дней назад
​@@m00n_pInKndi dolo wachiyao tinakuonesani kuona patali panya panu
@Ibrahimson-su5ks
@Ibrahimson-su5ks Год назад
Skype Skills
@charleskafodya7019
@charleskafodya7019 10 месяцев назад
Bodza tu ili adapita ku Malosa uti???
@HamidavioletYassin
@HamidavioletYassin День назад
Vuto lake unali usamabadwe zovuta kukhulupilila
@goldencitytowerent9554
@goldencitytowerent9554 3 года назад
Mbiri ya Bakili ija mwalowaso za khaza za MCP kkk
@LouisjrSaka
@LouisjrSaka 3 года назад
😂😂😂😂😂😂😂😂koma adha
@goldencitytowerent9554
@goldencitytowerent9554 3 года назад
@@LouisjrSaka kkk koma kamuzu anamulakwira chachiku mukulu ameneyu, ofcourse a MCP anali akhaza koma kumapolako
@LouisjrSaka
@LouisjrSaka 3 года назад
@@goldencitytowerent9554 chomwe adalakwa kamuzu kwa mkulu ameneyo nchachikulu heve 🤣🤣🤣🤣
@alankasiya7329
@alankasiya7329 3 года назад
Zabodza izi Bakili sanaphuzile ankagulitsa matumbi ku zomba. School anaphuzila atasankhidwa kale u president
@charlesmuyaya8839
@charlesmuyaya8839 3 года назад
So You mean Bakili Muluzi anapeza scholarship yokaphunzira ma college akunja mzaka za mma 1960 ali osaphunzira? I think mbuli ndi iweyo palibe chomwe ukudziwa chokhudza Bakili Muluzi.
@danielmaluwa7896
@danielmaluwa7896 3 года назад
Bakili muluzi ankagwira ntchito ngati clerk wa Ku court poyambilira penipeni. Ndie ukati anali osaphunzira ukutanthauza chani. Moreover bakili muluzi anali principal wa Nansawa technical college, kamuzu banda anamusankha kukhala MP komanso nduna ya boma pa nthawi yomwe anali mphunzitsi wamkulu wa pa Nansawa technical. Ndie ukati anali mbuli ukutanthauza chani. He was even minister of education mnthawi ya kamuzu. Mwina unangomvera ma propaganda a anthu kuti bakili muluzi anali osaphunzira iwe
@alankasiya7329
@alankasiya7329 3 года назад
U have been mis informed Bakili ankamphuzitsidwa school ndi Dr Ken lipenganga Ali kale president. Jce and msce anazipeza Ali kale president.
@charlesmuyaya8839
@charlesmuyaya8839 3 года назад
@@alankasiya7329 kutanthauza kuti ukutsutsa kuti Bakili Muluzi sanagwire ntchito Ku khothi ngati clerk? Sanagwire ntchito ngati principal pa nansawa college? Sanapite kunja mzaka za mma 1960 kukaphunzira ma college a ku Denmark ndi ku Britain? Sanakhalepo minister of education mnthawi ya Kamuzu? Ukamati we were mis informed what do you mean? Ife tikunena zoona zenizeni zooneka ndi maso pomwe iwe ukunena zongomvera anthu za mabodza. Bakili Muluzi was even minister of portfolio mnthawi ya Kamuzu, and you think munthu angakhale minister of portfolio ali mbuli?
@alankasiya7329
@alankasiya7329 3 года назад
@@charlesmuyaya8839 maphunzilo amene anenedwa kuti anaphuzilawo that's what I'm against kale anthu ankamphuzila up to STD 5 nkumapeza ntchito ngakhale Aleke Banda anali minister nthawi ya kamuzu koma anali ndi jc . Ngakhale ma minister ambiri muthawi ya amuluzi anali osaphunzira. Kukhala minister sikuphunzira
@kool2493
@kool2493 3 года назад
He was more worse than useless
@abdulrafiquekalembo469
@abdulrafiquekalembo469 3 года назад
Following
Далее
Mbiri ya Dr Bakili Muluzi PART 2
26:23
Просмотров 87 тыс.
DIY rocking horse for your kid #diy #parenting
00:57
Просмотров 3,4 млн
NOOOOO 😂😂😂
00:15
Просмотров 2,2 млн
PATRICIA KALIAT WABWENZA MOTO KACHIKENASO
12:51
Просмотров 2,9 тыс.
CRUISE 5 WITH JOHN ZENAS UNGAPAKE TEMBO
59:58
Просмотров 234 тыс.
hot Current..Kumkuyu Vs Namalomba
1:14:23
Просмотров 45 тыс.
Times Exclusive featuring Bakili Muluzi - 11 May 2024
58:41
DIY rocking horse for your kid #diy #parenting
00:57
Просмотров 3,4 млн