Тёмный

CRUISE 5 WITH JOHN ZENAS UNGAPAKE TEMBO 

Joab Frank Chakhaza
Подписаться 60 тыс.
Просмотров 234 тыс.
50% 1

JZU Tembo, one of the most seasoned politicians in Malawi opens up about his past. Tackling issues of the cruelty associated with his party, Malawi Congress Party, why Dr. Hastings Kamuzu Banda needed a translator, whether he hated Gwanda Chakuamba and his views on the bickering going on in the MCP.

Опубликовано:

 

21 янв 2018

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 183   
@FrynessMoyo-to2du
@FrynessMoyo-to2du 9 месяцев назад
Great chigawenga this guy Mr kan'gono anaphapo mbalame ndi anthu
@user-xt7cw1uc2d
@user-xt7cw1uc2d 9 месяцев назад
This was one of the best interviews Joab did, very interesting and making anyone listening to complete it all. May the soul of bwana Tembo, rest in eternity
@frankmaluwa2749
@frankmaluwa2749 5 лет назад
Kkkkkkkkk mau omwe ndawakonda koposa mu program imeneyi ndi oti azungu ndi oyipa ndizoonadi mau achiwiri atolankhani osamaonjedzera nkhani those are great and good words from JZU Tembo thanks
@danbanda8577
@danbanda8577 6 лет назад
Thanks cruize 5 for the nice programme.Tadziwako zambiri.
@vincentkhoxxer1805
@vincentkhoxxer1805 3 года назад
Very fascinating I love this interview
@josiahkings413
@josiahkings413 6 лет назад
This is becoming my favourite channel
@CyprianoSandalamu
@CyprianoSandalamu 9 месяцев назад
May your soul rest in peace father JZU Tembo
@ishbhad
@ishbhad 3 года назад
Brilliant interview knew him when he was governor of reserve bank of Malawi.Interesting to hear Kamuzu spoke with his ministers casually in Chichewa not in English which he did in public.
@JimmyPfupah15799
@JimmyPfupah15799 9 месяцев назад
Your legacy will live forever 💛
@davidmhlanga2114
@davidmhlanga2114 6 лет назад
ZODIAK BIG UP GUYS FOR THIS PROGRAM CRUISE 5, PITIRIZANI NDITHU
@ronardchikabadwa1741
@ronardchikabadwa1741 5 лет назад
BIG UP MAN I HAVE ENJOYED THIS AND I HAVE LAUGHED
@harrychampiti7739
@harrychampiti7739 6 лет назад
Great man JZU
@aishatawakali9017
@aishatawakali9017 6 лет назад
A Tembo kukulatu uku. I like the way he answers the questions
@chimwemwechiundira6002
@chimwemwechiundira6002 4 года назад
Salute !!!
@henrymbewebilly1405
@henrymbewebilly1405 6 лет назад
Munthu wamkulu tsopano(JOHN Tembo)..... Special thanks should go to Zodiac.....Timakudalirani ....Aliyense mMalawi wachilungamo ayenera kunyadira Zodiak for the Programme
@imandah1
@imandah1 Год назад
I revisited this Cruise 5 program, what an epic. John Tembo remains one of the most shrewd politicians to date
@joelmatchindu1738
@joelmatchindu1738 6 лет назад
Amazing
@makiphiri3469
@makiphiri3469 Год назад
VERY interesting
@happynhlane5976
@happynhlane5976 2 года назад
Enjoyed it 👍
@user-ng6uu3me4q
@user-ng6uu3me4q 9 месяцев назад
Kapumeni bwino baba ife chisoni njeeeh kamba kankhanza zanu🙌🙌🙌🙌
@user-gm5pu3wb6o
@user-gm5pu3wb6o 2 месяца назад
Koma bambo John tembo ,sanathe kulongosola bwino bwino za kamuzu bwanji ,munthu sungaiwale , mother's tongue, akunamapo mbabo tembo
@charlyumubyeyi1007
@charlyumubyeyi1007 6 лет назад
Òoooh! Woow! Zingayambe kuyiwalika za borodi zimenezi! Opposition started long time ago!
@afzaalmalik6057
@afzaalmalik6057 6 лет назад
Mwalowetsa zibwana mmalawimo
@Littlefair7
@Littlefair7 5 лет назад
Ngati kuli Kotheka mudzacheze ndi a chair, kamdala kamakani tidzaseke apa, adzafotokoze mmene anasokonezera dziko lamalawi.
@osamabinraden9391
@osamabinraden9391 3 года назад
Sadali m'malawi😁😁😁😁😁😕😕😕😕😕😕 muthu wam'kulu ngatiuyu akulakhula mabodza😯😯😯 khalamba yabodza iyi
@vanreeds_98
@vanreeds_98 9 месяцев назад
RIP Baba John Zenus Ungapake Tembo #MCP Legend & Veteran Politician 🕊️
@aleixosementesemente8727
@aleixosementesemente8727 3 года назад
São fazes da vida
@dongadaofficial3154
@dongadaofficial3154 4 года назад
Big man😍😍😍
@mouricesaidi5348
@mouricesaidi5348 4 года назад
I think Tembo anali SPY wa Kamuzu,,,,,
@josephphiri7481
@josephphiri7481 6 лет назад
my suggestion is that since he is still alive on he needed is to come out and apologize for almighty God in heaven and those people of that country still today the government of Malawian has not compensate this people so John tembo he is killer and a plunder of resources of Malawi and his sister mama kazamila
@kamuzu1964banda
@kamuzu1964banda 6 лет назад
Joseph Phiri. Anapha ndani?
@Gundasonic
@Gundasonic 3 года назад
Yes.. He should be tried
@brendamdzagada-soko282
@brendamdzagada-soko282 6 лет назад
Very interesting
@alexanderkaunda9554
@alexanderkaunda9554 4 года назад
Gadama-chiwanga-sangala-matenje-there-waiting-for-you
@kaitanokagalu
@kaitanokagalu 6 лет назад
Mr Joab, this question of who allowed and or said Dr kamuzu Banda should be the life president, i think we should also know that, that time there was no multiparty system, therefore we should all agree that Kamuzu would be the life president because panalibe wina aliyese amene akanatenga udindo wa upulezident. And on top of that Malawi was like any other countries where we fought ndi azungu. So i don't see it kuti it was one person who said Kamuzu should be the life President.
@eliasenock5667
@eliasenock5667 5 лет назад
Nice one
@oscarmsiska393
@oscarmsiska393 4 года назад
This interview is Iconic, and DR Tembo the composure in him
@edwardoschando9233
@edwardoschando9233 9 месяцев назад
Watching this now!!! Rest in Jah eternal glory Baba JZU!!!!
@ithrees2315
@ithrees2315 6 лет назад
Anaamuna JZU
@FellaGondwe
@FellaGondwe 6 лет назад
Notice how he says "discipline" yachipani amapanga ndi anthu lol if he wasn't responsible for that he wouldn't have called it "discipline". He recognized that as discipline not oppression.
@georgezimba4702
@georgezimba4702 6 лет назад
Indeed seasoned politician. JZU Tembo.
@stephanchatatahshezi7036
@stephanchatatahshezi7036 9 месяцев назад
Rest in Eternal Peace gogo JZU Tembo agreat son of Dedza 😭😭😭💔💔💔
@EMtupa
@EMtupa 5 лет назад
Sir John Tembo akuoneka ngati akanakwanitsa kutumikira dziko lathuli
@paulnkhama3621
@paulnkhama3621 3 года назад
Atembo analakwachiyani mr Gadama mr chiwanga mr matenje mr sangala yr evil
@abisonchitukula6986
@abisonchitukula6986 3 года назад
i like this political gurus kkkk
@ndawakalimbuka1322
@ndawakalimbuka1322 6 лет назад
Big man
@blessingskaipa3617
@blessingskaipa3617 4 года назад
Wow nice
@ernestgama3718
@ernestgama3718 9 месяцев назад
May His Soul rest in peace
@dinaburger552
@dinaburger552 5 лет назад
Amakwana JZU Tembo
@dzuwabrands
@dzuwabrands 9 месяцев назад
Rest in peace Sir.
@lemonsimoko947
@lemonsimoko947 6 лет назад
joab timatsata program imenei kuno Ku Pretoria
@user-wd9yd1bg9n
@user-wd9yd1bg9n 9 месяцев назад
Munthu okupha uya , mukumuchemelera chani😢
@user-st6bt5vv9c
@user-st6bt5vv9c 2 месяца назад
Wakapeza a achina gadama, matenje,sangala ndi chiwanga omwe anapha iyeyo ali kumoto
@spizleaustin1531
@spizleaustin1531 9 месяцев назад
May his soul rest in peace
@Yellowchanges.
@Yellowchanges. Месяц назад
Why
@wiyulegwayi269
@wiyulegwayi269 9 месяцев назад
Rest well gogo ungapake John Tembo
@user-gy5hm5mc1v
@user-gy5hm5mc1v 9 месяцев назад
Hamba kahle our Legend
@alannyirenda588
@alannyirenda588 2 года назад
Can you imagine he's still defending 🙄 😳 kamuzu now while he's in the grave Liar!
@memorymbepula3772
@memorymbepula3772 4 года назад
Apa mwati bwanji pa nkhani yoyankhula Chichewa Kamuzu Banda? Mr Joel muzamufusenso wina pa izi
@wisdomlipenga4522
@wisdomlipenga4522 6 лет назад
JZU Tembo is old hence his memory and articulation of ideas is distorted a liitle bit, therefore its not appropriate to take his words seriously. For instance he declined being in an alliance with UDF during 2009 elections, a scenario we all know happened. JZU Tembo shall remain mwana wa nkango and iconic politician Malawi has ever have. His contribution to national building by working in numerous reputable public institution can not be undermined. Viva JZU. Viva MCP. Viva Chakwera
@giftsululu6864
@giftsululu6864 6 лет назад
stl in great validity
@kennedychinguwo1640
@kennedychinguwo1640 2 месяца назад
What kind of contribution did he do to this country,yokupha anthuyo!!! Kunzunza anthu basi,they did nothing including the fake Kamuzu Banda
@g5tkalimira2842
@g5tkalimira2842 9 месяцев назад
RIP legend
@alannyirenda588
@alannyirenda588 2 года назад
I hate this guy with all my heart, why he's lying to us? He was kamuzu banda's right man.... he knew everything that was going on all the killings and brutal
@Manishamalenga
@Manishamalenga 9 месяцев назад
Mulungu yekha akaweludza
@blessingskakusa7836
@blessingskakusa7836 9 месяцев назад
Rest in peace JZU Tembo
@Vincent-ce9cf
@Vincent-ce9cf 2 месяца назад
🎉
@wamwale8156
@wamwale8156 6 лет назад
Awa ndiye nzika za Malawi osati omwe akunkhala ma president aaaaaa or mbiri yamalawi sakuidziwa akungodziwa zolemba mmabuku
@willardabraham
@willardabraham 9 месяцев назад
rest in peace
@user-gs7wc3nx3q
@user-gs7wc3nx3q Месяц назад
Iweso unari munthu oyipa kwambiri
@williamnamakhula1908
@williamnamakhula1908 9 месяцев назад
Rest in peace
@elwinchirwa1218
@elwinchirwa1218 6 лет назад
amazing
@rachelbanda2131
@rachelbanda2131 9 месяцев назад
Rlp legend
@charlesmuwanya7845
@charlesmuwanya7845 9 месяцев назад
Bodza kamuzu samalankhula Chichewa chomveka bwino (fluent). Munthuyu anali wa ku Ghana. Anagula anthu ku Kasungu kunamiza dziko kuti ndi abale ake. Atolankhani ankaletsedwa kufufuza kapena kufusa mafuso anthu onse amene Kamuzu amati ndi abale ake. Ndipo anthu amene Kamuzu anagula ngati abale ake samaloledwa kulankhulapo zaubale wao ndi Kamuzu.
@mouricesaidi5348
@mouricesaidi5348 4 года назад
Now l believe kut munthu wa ndale ngwabodza,, when did Kamuzu speak Chichewa?
@rossbank7248
@rossbank7248 3 года назад
Kamuzu used to speak chichewa the video are there on RU-vid
@pansigaleta3438
@pansigaleta3438 3 года назад
Madala madala Jzu
@MrRamGee
@MrRamGee 5 лет назад
Bodza Kamuzu sankalankhula chichewa.
@Gundasonic
@Gundasonic 3 года назад
Yep... He is lying
@mataxsimon1737
@mataxsimon1737 6 лет назад
mxxxii, munthu oipa uyu joab adamufusa bwino koma akuthawathawa
@dingiswayokachina9987
@dingiswayokachina9987 9 месяцев назад
Rip veteran
@johnbanda6500
@johnbanda6500 6 лет назад
mkuluyu sadzatheka
@BostonStLungu
@BostonStLungu 9 месяцев назад
RIP
@arthurmwagomba7256
@arthurmwagomba7256 6 лет назад
Kip goin chakhaza nw waiting for winiko kkkkkkk
@wiseyk1435
@wiseyk1435 5 лет назад
Tembo amafunika 2hrs interview, amalankhula chimozi chimodzi🤣🤣🤣🤣
@TysonWaTysonKasukuwere
@TysonWaTysonKasukuwere 9 месяцев назад
May His Soul Rest In Peace. 14September 1932 to 27September 2023. Died at the age of 91.
@FatsanIbrahim-gj1mf
@FatsanIbrahim-gj1mf Год назад
Koma joaba umatha umandivetsa kukoma from Johannesburg
@oscarnandolo1198
@oscarnandolo1198 8 месяцев назад
Rip jzU
@chitsanzomafupa4877
@chitsanzomafupa4877 6 лет назад
munthu wamkulu kwabasi...machine opangila machine azake
@user-ig4zf5xi7f
@user-ig4zf5xi7f 9 месяцев назад
Rip
@Gundasonic
@Gundasonic 3 года назад
Haaa 😂😂😂😂😂😂😂he is lying about kamuzu speaking chichewa. He is protecting kamuzu legacy
@homeremedys3748
@homeremedys3748 2 года назад
Kamuzu he was speaking chichewa very well, wabadwa dzulo iwe ingokhala phee or uzionera zingayambe kuiwalika
@mamaafrika6675
@mamaafrika6675 2 года назад
Kamuzu amayankhula Chichewa ndi chitumbuka chomwe
@alexanderntawanga8297
@alexanderntawanga8297 6 лет назад
The long waited interview
@slembani
@slembani 6 лет назад
Thanks Joab and Zodiak
@sanabdul6397
@sanabdul6397 6 лет назад
Wow....that was really good conversation. Next time go to Dr bakili muluzi
@noelmunthali3516
@noelmunthali3516 Год назад
Kamuzu Chichewa baba tembo mukunamatu
@dennisimedi5347
@dennisimedi5347 6 лет назад
This guy looks like kamuzu banda
@makayikomkandawire7062
@makayikomkandawire7062 3 года назад
eekkkk
@markchirwa1610
@markchirwa1610 Год назад
Ineso maganiza choncho
@markchirwa1610
@markchirwa1610 Год назад
Ineso maganiza choncho
@hamisahyassin5383
@hamisahyassin5383 6 лет назад
vutola amalaw mukucheza ndi mmalwi weni weni nyimbo mukuyika zaazungu aaaa sizoona
@joabfrankchakhaza
@joabfrankchakhaza 6 лет назад
A Malawi siamvera nyimbo za azungu?
@chimwemwemoyo9374
@chimwemwemoyo9374 4 года назад
Iconic clap back!!!!
@davlinchokazinga1993
@davlinchokazinga1993 9 месяцев назад
What a legacy!! RIEP Baba Tembo
@amoschisisi2070
@amoschisisi2070 6 лет назад
This man reminds the Mwanza four,Dick Matenje, Aaron Gadama and others
@ithrees2315
@ithrees2315 6 лет назад
Amos Chisisi walking in unforgiveness spirit
@giftsululu6864
@giftsululu6864 6 лет назад
+I Threes only God could judge him because nobody knows how much God loves him enani or ukalàmba simuzaulawa
@ithrees2315
@ithrees2315 6 лет назад
Still living in the past dzuka Malawi dzuka
@chesterphiri7523
@chesterphiri7523 6 лет назад
Amos Chisisi kkkkkkkkkk yes this gentleman I think that he tried at all cost to clear his way in order for him to become the successor of Kamuzu & a lot of innocent people fell victim to this gentleman koma Ambuye sanalole.
@chesterphiri7523
@chesterphiri7523 6 лет назад
Gift Sululu that is very true God alone amakhala ndi cholinga ndi each & every individual. Mawu a Mulungu amanena kuti tchimo lingafiyire ngati Kapezi ngati Munthu atavomereza ndikulapa azayeletsedwa ngati Matalala. But this does not stop people to point out what people perceived to be ill. Judgement is reserved only for God.
@user-xk8tf5kw6r
@user-xk8tf5kw6r 9 месяцев назад
At kundale kulibe kufunsana maganizo😂😂😂 aise john tembo umakwana uyende bho😅
@harrisonkanyemba2770
@harrisonkanyemba2770 6 лет назад
Ulemu wanu a Tembo, tinakusowani
@lastonekaponya7675
@lastonekaponya7675 4 года назад
Kakkkkk kumamusowa alimoyo kikikiki
@eltonmaseya6511
@eltonmaseya6511 6 лет назад
Kkkkkk
@madalitsochabwera5903
@madalitsochabwera5903 5 лет назад
Ataaa pang'ono ataa kkkkk
@user-wg9tx5cw5x
@user-wg9tx5cw5x 9 месяцев назад
MHSRIP
@shukuranichinthenga236
@shukuranichinthenga236 Год назад
Koma John tembo experience inapweteka😂🤣
@user-tf6ld5xr8y
@user-tf6ld5xr8y 11 месяцев назад
All satans have soft talk,to hide their evil
@atambwalisametana6363
@atambwalisametana6363 Год назад
Mkulu ameneyu anali woopsezya wanthu.
@ngungunimussa3183
@ngungunimussa3183 3 года назад
Chakupha ichi 😞😞😞
@user-xc7fc1yv3u
@user-xc7fc1yv3u 9 месяцев назад
Tembo
@ChinsanjeChifundo-he2yc
@ChinsanjeChifundo-he2yc 11 месяцев назад
Ubale wantundu wanji? President wake adali ndan kkkkk
@mamaafrika6675
@mamaafrika6675 2 года назад
Kamuzu amatha Chichewa komaso chitumbuka amatha. Anaphunzira ku khondowe
Далее
CRUISE 5 WITH LUCIUS CHIKUNI PART 1   08 May 2022
58:54
Цены на iPhone и Жигули в ЕГИПТЕ!
50:12
DEFINITELY NOT HAPPENING ON MY WATCH! 😒
00:12
Просмотров 27 млн
Zlatan embarrasses Speed 😂 #ishowspeed
00:32
Просмотров 15 млн
GOtv Malawi Izeki ndi Jakobo Kukhala Awiri Simantha
19:56
CRUISE 5 WITH FISCHER KONDOWE
51:48
Просмотров 116 тыс.
Mkangano wa Lucius Banda ndi Bingu
13:20
Просмотров 132 тыс.
Cruise 5 with Rebecca Malope
39:09
Просмотров 28 тыс.
CRUISE 5 WITH NAPOLEON DZOMBE
1:03:03
Просмотров 79 тыс.
Mkangano wa Kamuzu Banda ndi Samora Machel.
29:19
Просмотров 197 тыс.
BON KALINDO & JACOB AT DISASTER COMMEMORATION
10:44
Просмотров 300 тыс.
Цены на iPhone и Жигули в ЕГИПТЕ!
50:12