Guy we need to be serious us Malawians munthu ngati uyu akupanga zopusa BT ilibe madzi wina akukwera njinga uku dziko likuvutika guys kumalawi tikulephela kutukuka chifukwa we have time to waist
Zinthu Zina ndizabwino ndithu koma zikaonjeza zimaonongeka. Asakomedye kwambiri kupanga zimenezi coz amadziwika ndi Drama ndiye zina zikufunika ka control kuti pazikhala kusiyana
What is the main purpose of doing these toors,had it been that that they ware not correcting allawances it was good,this is one way of wasting resources,,,, shame on you
Kamunthu kofupika ndi nzeru zomwe kamunthu aka kabalalika mwazi wachilima ukuwazunguza anthu amenewa mzimu wa Chilima SKC WHERE EVER YOU ARE KOMA DANDAULO BWANA CHILIMA MUNATITENGELA NASONGOLE PAKATI PA TILIGU MANGANYA AKUSOKONEZA ZINTHU KOMA MAYI KALIYATI ACHIGWILA BWINO CHIPANI NDI FREDDO KISS K
Kodi malemu Dr Chilima adakakhala oyimba and nkuchitika monga zidachitikieamu pano mukuti adaphedwa ndi ndani? ( not kuti am happy ndi ya anthu 9 aja , inenso ndiokhudzidwa kwambiri) Uzimu ukusowa apa ndichifukwa timangolankhulapo anthufe))
Awatu ndi masanje basi , mtsogoleri wa dziko kukacha adzikhalira kupanga zimenezi.. za drama basi..dziko kulilowetsa chibwana basi..I don't think this is the way to tackle issues affecting Malawi right now...
What is this guy trying to prove? We don't want poverty n eating at such a place is never nice. We ought to promote standard things not subsyandard restaurants after all you might get cholera. You're not pleasing anyone