Тёмный

Minyama yathu ngati amalawi ikuchokera pati? 

Bakili Muluzi TV
Подписаться 135 тыс.
Просмотров 76 тыс.
50% 1

Опубликовано:

 

21 окт 2024

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 222   
@princedetbozsmallboy1749
@princedetbozsmallboy1749 Год назад
Mkhoza kuona nokha kuti zikhaleyo kuyipa nkhope angakhale ndichisoni. Tomorrow never end will see
@farookousmane715
@farookousmane715 Год назад
We are all Africans...when I see a burund person I see myself.
@kubengovender6996
@kubengovender6996 Год назад
You're the great man in malawi!!
@markoviskyhernandez9706
@markoviskyhernandez9706 Год назад
Thank you very much brother!! You are the best even though you tell people who have no ears nor brains!! Pepani ndithu!!
@greychizaka4088
@greychizaka4088 Год назад
anthu odzikonda chabe
@raytavares2256
@raytavares2256 Год назад
It's sad even in Angola Malawians used to sell its former Africans who were fighting the regime and that's how they killed my father and tortured my mother as a Christian missionary helping children who were forced on armed labour. My mum helped and was hiding those children to a place of safety.
@markoviskyhernandez9706
@markoviskyhernandez9706 Год назад
@@raytavares2256 Sorry Dear Sister/Brother😔!! It's very sad to hear 🙆🙆!! But most of the time, the governments of Malawi and many Malawians show a surprising behavior!! Imagine that Malawi was the only black country which was supporting discriminating government in South Africa!! Can you imagine that!!??🤔🙆!! Go there in Malawi right now and see what they are doing to black african refugees. It's shameful!! Remember that there are more than 6 millions malawians in South Africa, more than 5 millions malawians in Zimbabwe, more than 1.5 millions in Botswana, .... without forgeting in Europe, America and other different regions of this Earth. But the animosity that they are inflicting to the refugees is surprising!! Nothing to say 🤔😔!!
@BenissoneErnesto-kn9bd
@BenissoneErnesto-kn9bd Год назад
Komaditu brother Malawi ndikachani panagaga ngati pamenepa anyamatuso ambir Ali maiko ena kuthawa kupandako kanthu kumalawi zinkhale Ng,OMA watani kd komatu zimenezi siku Lina zizamusata
@thomassimbaya197
@thomassimbaya197 Год назад
watching from zambia you are great big man ,thy is a gold scalndal that has just happened here in zambia at K K international airport which is very compliceted i wish u could search about it
@AhmaduWilson-jl2br
@AhmaduWilson-jl2br Год назад
Umakwana ulemuwanu big thanks for telling us true
@Wesleywisk-lf5hw
@Wesleywisk-lf5hw Год назад
Achakwelaso uthengau ukupezeni
@HusseinMm-z3j
@HusseinMm-z3j Год назад
Zikomo brother mumatitsangalasa 🙏🙏🙏🙏
@rickiez
@rickiez Год назад
And I quoted "za mawa sizidziwika" ndili wokudzika kwambiri. Thanks for the information may God bless you
@princedetbozsmallboy1749
@princedetbozsmallboy1749 Год назад
Zoona zake bra
@AishaMweso
@AishaMweso Месяц назад
Zikhale koma mmmmm mtule pas
@SufiaanMsusa
@SufiaanMsusa Год назад
Am here waiting you boss from Johannesburg
@raspeterkasengwa1390
@raspeterkasengwa1390 Год назад
Though you don't show your identity. You remain iconic
@anafieintuka8090
@anafieintuka8090 Год назад
Good history sir Inu mumatiuza zoona zokazoka, thanks sir
@alexjeremanuel2541
@alexjeremanuel2541 Год назад
Malawi Congress Party is a party that was not supposed to rule Malawi again
@wysonnamaona6497
@wysonnamaona6497 Год назад
For sure
@GiftMusorola-l2o
@GiftMusorola-l2o 11 месяцев назад
Nothing rong
@GiftMusorola-l2o
@GiftMusorola-l2o 11 месяцев назад
Nelson mandera never talk about kamizu
@Eric-gb9ms
@Eric-gb9ms 5 месяцев назад
Zoona big ine
@Musa1828-l5d
@Musa1828-l5d 2 месяца назад
Zooand izi
@frankfriday3141
@frankfriday3141 Год назад
From Johannesburg near alberton ulemu wanu Big nde chifukwe chake aku Mozambique samatipasa magesi khamusu anatenga gawo ifa ya Zamora
@josephchitsulo5882
@josephchitsulo5882 Год назад
Ndizoona, tilikonkuno ndipo akutisunga ndiomwewa
@fedson2050
@fedson2050 Год назад
Chakwera suzamva Munthu opanda Nzeru iwe ndi Mnzako Zikhale N'goma
@stevechikaonda3145
@stevechikaonda3145 2 месяца назад
I must admit that this unknown guy is intelligent and wise
@abudardachilangwe6791
@abudardachilangwe6791 Год назад
It's true...ndinakumana ndi muthu mu Bank kuno ku South Africa ndipo anati Dr banda munthu akathawa ku South Africa mkubwela ku malawi kamuzu amamugwila ndikumtumiza ku South Africa ndipo akafika ku South Africa amaphedwa ndikumangidwa.....I was ashamed kumva zimenezi
@anifoiuene6301
@anifoiuene6301 Год назад
Andrew chimwendo sanayendepo kupita ku dziko laeni asiye kuyankhula za utsilu.Anifo from Moçambique
@KennedyPhiri-h9h
@KennedyPhiri-h9h 2 месяца назад
Malawians people please let's wake up and fight for this country chakwela akutitenga wezi kwambili
@christophermomba7127
@christophermomba7127 Год назад
Thanks for information keep it up Bakili
@TrizaGeorge-q8w
@TrizaGeorge-q8w 11 месяцев назад
This is very powerful massage ❤❤
@johnman4619
@johnman4619 Год назад
Ndizomvetsa chisoni mbiri yadziko lathu mutati muoni the holl Africa ndife thokha amalawi tilindi mbiri yoyipa mu independence koma zonzezi ndi Cecelia and John tembo
@RaheemNgoma-pk1ev
@RaheemNgoma-pk1ev Год назад
Apa ndizothekano kumagona thx bradah man
@OmarAskimu-cn4ti
@OmarAskimu-cn4ti Год назад
Even makolo athu anatiuza zakuipa kwa MCP
@idrissaKGO
@idrissaKGO Год назад
Jerous siimapindula gyx amalawi
@christophermkhize1991
@christophermkhize1991 Год назад
Koma big inuyo mumakwana "nyelele mukuziponda lero mawa zidzadya ntembo wanu" ndimawutu akulu kwambili ngati amvela zimenezi ayenela kusintha zamawa sizidziwika
@chrisboyce229
@chrisboyce229 Год назад
Zoonadi brother Jealous simasunga mudzi tikuyenera kusintha A Malawi chifukwa Cha mawa sichidziwika
@NgendahayoSosthene-qn7qn
@NgendahayoSosthene-qn7qn Год назад
mukanena dzina ra charichi cyo ndikanafufuza umboni wa nkhani imeneyo rero romwe.
@greychizaka4088
@greychizaka4088 Год назад
Reference ya andrew chimwendo yandikhudza dont burn bridges you crossed.
@webstermbewe8395
@webstermbewe8395 Год назад
Thanks very much continue doing that
@ThokiseWiriyam-ws1ec
@ThokiseWiriyam-ws1ec Год назад
Chakwera ndimbuzi
@Yanazihhk2Hussenih
@Yanazihhk2Hussenih 4 дня назад
Chilunu ndizeru zachuma kwa ozindikila❤
@hopembendela
@hopembendela Год назад
Nkhuyu dzodwa mwana zipota mkulu thanks bro
@MohommedMartin
@MohommedMartin Год назад
Andrew chimwendoyo pa mtumbo pake, galu ya chabe chabe
@raytavares2256
@raytavares2256 Год назад
Thank you for revealing the TRUTH. You must write a book about this history. It's true Malawi never ever bothered to help South Africans and yet today they still go to South Africa to work. Even now they follow the same patterns. Look at how they prefer keeping criminals and yet on Sadec. Do you recall how Kwacha Ng"ambi committed crimes more than Bushiri in South Africa? And South Africa will always be loyal to Malawi. Look at the Wenela period?
@ThivadoartistDyson
@ThivadoartistDyson 2 месяца назад
Uchitsilu basi, zelu ngat mazula ku john sadziwa businesses safuna ntchito koma jerous ndi anthu.
@FredKanyerere
@FredKanyerere День назад
Powerful news brother.
@khumbozimba-r4h
@khumbozimba-r4h Год назад
Chanel yomwe ndimaikonda palibeso kuposer iyi ulemuwanu big
@titomethiwa4213
@titomethiwa4213 Год назад
Zikhale ndichisilu ndimuthu oipa kwambiri
@josephchitsulo5882
@josephchitsulo5882 Год назад
Tamugwileni mum'menye nachimutuyo, ana omwe anabadwila ku Malawi ko, ndi Malawian, chotelo akuzunzisa anawo
@charlesRajabu-cc4bx
@charlesRajabu-cc4bx Год назад
Always you mumanena chulungamo mumayipasa fire
@MussahGeorge-f5n
@MussahGeorge-f5n Год назад
From Pretoria, love ur stories
@BlessingsBanda-qn7xr
@BlessingsBanda-qn7xr Год назад
Mngopusa zikhale mbale zake mapoto ake komaso paniyo pake 😂😂😂😂😂😂
@patriciacraiton-sf5vu
@patriciacraiton-sf5vu Год назад
😂😂😂😂😂😂
@sammyree8843
@sammyree8843 Год назад
I have been following for while brother very educative as we grew up in a country that real history was hidden to us. Please can I donate to you?
@henrysoko3283
@henrysoko3283 Год назад
I wish to donate too, this man has brain washed me
@Littlefair7
@Littlefair7 Год назад
Amalawi ambiri ndi ma illegal immigrants ku America, koma ali ndi ma business, amaloledwa kutenga loan ku bank even kugula nyumba kapena galimoto pa ngongole,, ndipo akuchita bwino kuposa ma americans. Boma la America limatolera misonkho kwa onse koma mabulutu amene akuyendetsa dziko la malawi sakuona patali.
@Gibbs-yp6um
@Gibbs-yp6um Год назад
Mumakwana munthu wa'kulu kip on giving us nothing but the best history.
@ALuz980
@ALuz980 Год назад
Ndizoona Khalidwe la nyau siligatithandize
@DanielNgondo-rr9gd
@DanielNgondo-rr9gd 2 месяца назад
11 minutes ago.....58 thousand viewers....ayi zikomo
@TriciaMalikebu
@TriciaMalikebu 2 месяца назад
Kamuzu & his party, MCP will never change
@wysonnamaona6497
@wysonnamaona6497 Год назад
With you all times... Thank you for opening up our eyes.
@gladysbonongwe1038
@gladysbonongwe1038 Год назад
Auzeni asiye majelous
@BensoPias
@BensoPias Год назад
Best historian your nomber one
@EphraimNaveya-fc4iu
@EphraimNaveya-fc4iu Год назад
Nice 👍 talking sir,mcp it's one party that makes Malawi to be poor/minyama country
@bjmtalimanja5073
@bjmtalimanja5073 Год назад
Andrew chimwendo kumwamba siwukalowa ndithu
@alexKaudzu-f6o
@alexKaudzu-f6o Год назад
Pilizani bro kutsegula maso a Malawi
@daudimatolano1715
@daudimatolano1715 Год назад
Teach us, we are ready to support your work
@markoviskyhernandez9706
@markoviskyhernandez9706 Год назад
Munthu wakuda kugwilizana ndi anthu omwe amapanga za Apartheid !??🤔🤔!! Za wutsilu ziminezo ndithu !! And they had no shame!!???🤔🤔 There is nothing worst than to be on the wrong side 🤮🤮🤧🤧!!
@LouisAndrew-jr1yj
@LouisAndrew-jr1yj 2 месяца назад
History is the best teacher ✌️
@AndersonBishop-i2t
@AndersonBishop-i2t 2 месяца назад
Zoonadi kamuzu amadana ndi anthu akuda km azungu chifukwa chasakho yakeyo ndie chilango chipite kwa kamuzuyo basi ctingamufunile zabwn kamuzu amuike ku mbawula ameneyo ameen 🙏 ameen
@eidchinkhunda7777
@eidchinkhunda7777 2 месяца назад
Long life big brother may Allah bless you
@pastorbinuelf.lamusse6203
@pastorbinuelf.lamusse6203 Год назад
Timakunyandirani big kuchokera Kuno ku Moçambique Maputo.
@johnsong7236
@johnsong7236 Год назад
i always smile and learn something at the same time
@SandraMoses-y4l
@SandraMoses-y4l 2 месяца назад
Abale anzanga zikufunika tikavote mwanzelu serious chakwela ayi ndithu
@shabanitendo4781
@shabanitendo4781 Год назад
My bro now ur coming brz sizachilendo simukumuona chakwela amagwadra azungu
@aubreykanyenda8008
@aubreykanyenda8008 Год назад
Please TEACH US and don't stop teaching this Government too
@JafaliAlli-w7m
@JafaliAlli-w7m Год назад
zikhale ng'oma mulungu amulanga pompano ndi juma yemweyo mulungu akuwuona akuzunza anthu
@HevenChiwaya
@HevenChiwaya 3 месяца назад
We still learned a lot from you ❤❤
@josephchitsulo5882
@josephchitsulo5882 Год назад
Tamuuzeni kumeneko chitsiluyo, ifenso tilikuno kudziko la eni
@LUCKYM4787
@LUCKYM4787 Год назад
That the fact ndithu thank you so much bg mn
@daviemafunga
@daviemafunga Год назад
Inuyo is bstter kukhara brother wanga
@ElliasChikuluwadza
@ElliasChikuluwadza 2 месяца назад
Kkkkkk Kma mbakili muluz ndi mamunadi.
@jonathankwangulero4450
@jonathankwangulero4450 Год назад
Chakwera and his MCP has failed Malawians... But, politicizing the issue of Refugees is wrong. Ma refugee kulikonse amayenera kukhala in designated places. It's no rocket science.... Mpaka Refugee azipanga business aaah sizowonaa
@dondamissonchdziwe3958
@dondamissonchdziwe3958 Год назад
Chakwera, zikhale ng'oma MCP yonse panyini pa mawo,ifeyo panopa tiri kunja poyamba timalandira ulemu koma panopa tiku funa kumama ngiridwa ma camp amalawi akuvutika akuthawira maiko akunja komanso inuyo mukakhala kumeneko ku malawiko muna voteranji MCP kamuzu anawa siyira mizimu ya Ziwanda panyero pa amawo
@jameschipula4475
@jameschipula4475 Год назад
Mumatha ndinu madala-madala
@sipplezulu
@sipplezulu Год назад
Africa tigwirizane ndife anthu amodzi
@jameskachulu8141
@jameskachulu8141 Год назад
Ife kuno ndiye tilipo samativutisaso achewa ngovuta ndaonela pa chakwela
@ModaAckson-sd2yq
@ModaAckson-sd2yq Год назад
Koma 🇲🇼 anatengadi minyama
@UthmanKapungu
@UthmanKapungu 2 месяца назад
Congress is a total blood of Malawian and it's to us to choose again
@UthmanKapungu
@UthmanKapungu 2 месяца назад
It's a mistake
@JohnChibalo-wf8gr
@JohnChibalo-wf8gr Год назад
Boma la m c p langodzaza ndi mbuli zosazindikira chilichonse kuyambira business mpaka zolima Lima. Chomwe akuchidziwa ndi kuba ndiye poona kuti upresidernt uli mbali yawo ndiye angopedzerapo mwayi okuwabera ndi kuzunza mabulundi. Iweyo zikhale ng'oma ukati Sisi lomosoka m'mbali nkhati kumaliseche kwakoko.😅😅😅😅😅
@johndaka6368
@johndaka6368 Год назад
We are proud with u in Africa
@kondwanivyalema9449
@kondwanivyalema9449 2 месяца назад
Mzimu wa Chilima SKC uwuse mutendere
@matembanevermind-po3me
@matembanevermind-po3me 10 месяцев назад
Tchutchutchu mofatsiliranso ndpo,mumakwana bigy
@MefaKumwenda
@MefaKumwenda Год назад
Than you for explaining all history
@jeanmariehavugineza9382
@jeanmariehavugineza9382 Год назад
ine ndimafuna gupana support nchito zanu mutipatse number kapena njira yina kuti titandize nshito yi
@AfiyakazembeKazembe
@AfiyakazembeKazembe Год назад
Zoona big ine Kuno Western Cape Harare
@PreciousDouglas-d7v
@PreciousDouglas-d7v 8 месяцев назад
Ur de best tv
@markoviskyhernandez9706
@markoviskyhernandez9706 Год назад
Anthu akuda amene amadana ndi akuda ena anzao, ndi zitsilu kwabas!! Nkhani ya Chimwendo ameneyo ndi onvesa chisoni 🤔🤔!!
@PatrickChitekwe
@PatrickChitekwe Год назад
Ndiye anthu akuda ake aku RSA tu Xenophobia
@horagerva
@horagerva Год назад
Mulungu akudalitseni. Zoona mukunenazo.
@eunicemoyo6024
@eunicemoyo6024 Год назад
Shaaaaa kom malawi nsanje ndi ulesi wake ufiti bas kom mukuti ndi mbusaso 😏😏😏
@HamdanMasuku-b3n
@HamdanMasuku-b3n Год назад
Ndwe dolo ase keep up
@maxwellchibwe5956
@maxwellchibwe5956 9 месяцев назад
Ngakhale ena atsutse or ayi koma nkhaniyi ndiyoona kamuzu doesn't been regarded as pan africanist or one of greatest African leaders we had in Africa. Muone mu history ya Africa ikuonetsani zimenezi
@TonyBanda-ch6vo
@TonyBanda-ch6vo Год назад
Koma inuyo bigy munabwera respect to you .
@francombalasa3241
@francombalasa3241 Год назад
Ndichifukwa chake nyimbo ya fuko lathu imanena za njala, nthenda ndi nsanje.
@AleksaWilliams
@AleksaWilliams Год назад
Kumakhaladi ndi umunthu,ndizoyilanad zithuzi
@raytavares2256
@raytavares2256 Год назад
The question is this if there's no foreign currency in Malawi where is the president getting this foreign currency to get to Angola?
@giftdulamkalenga7344
@giftdulamkalenga7344 Год назад
Chakwera ndi opanda mutuu
@YunusuOfesi
@YunusuOfesi Год назад
Zikhale ng'oma ndigalu alibe chisoni ndi azawo
@BrownChinkhota-o2h
@BrownChinkhota-o2h Год назад
Ngati a MALAWI sitinathandize pomenyera ufulu chifukwa tilibe zothandiziraa
Далее
Abale ake a John Chilembwe ali kuti?
15:36
Просмотров 44 тыс.
CRUISE 5 WITH JOHN ZENAS UNGAPAKE TEMBO
59:58
Просмотров 237 тыс.
Europe ndi America amabisa ma Dictator chifukwa chani.
13:59