Chakwera vomeledza kuti dziko la kukanikani kuyendedza this is bad news 😢 😞 😕 😔 😳 💔 will don't need you go pls live Malawi alone APM come take care about your beautiful 💙 Malawi peoples 💙 😀 please mr president APM will need u mr president
Nde mkumati ndale what is kind of ndale for this malawian people, mkumati boma ndilomweli what is this? Koma anthu ena mukumati boma ndilomweli, please anthu amene mukut boma ndilomwelo tapitan mukawauze a president kut ife tikukhuta koma anthu kumuz akuvuta ,because anthu kumuz akuti boma silomweli chifukwa akuona mazuzo ,sikuti ndindale kapena chiyan chifukwa ine ndilibe mbali ndili overseas ,but am just kuva chison ndi mmene anthu akuvutikila mdziko lathu this is very sad story, inuyo inde khutan ndizopasidwazo koma kunja kuno kuli ena amene sadalira dzopatsidwa amadzilimbikilira paokha ,komano zinthu zikuvuta because ndalama ya sowa ndiponso ilibe mphawi zonthu zakwela, alimi ochuluka mudziko la Malawi ndiosauka amapeza ndalama movutika ,kuwatsitsila feteleza l think something it can be ok chifukwa kumudz
Drama kapena zoona, ndafunsa chonchi chifukwa choti pali a Camera, anadziwa bwanji kuti tipite ndi camera munthu akomoka. Vutolo ndi zoona lilikodi koma ili ndi drama.