NGATI YESU CHRIST ANATEMBERERA NKUYU CHIFUKWA CHOSABEREKA , INEYO NGATI MTUMIKI WAKE NDIKUTEMBERERANSO JERE KUYAMBIRA LERO NYENGOZAKO SIZIDZAKHALA MONGA KALE UDZAKHALA UKUZUNZIKA MOYOWAKO.ONSE ANA AKO APABANJA PAKO MDZINA LA YESU CHRIST AMENE ANAPACHIKIDWA PAMTANDA CHIFUKWA CHA TCHIMO LAKO,MDIKULENGEZA NDI MWAZI WAKE WA YESU USOWE MTENDERE , USOWEMTENDERE ,USOWEMTENDERE .
Pa dziko lapasi Pano akhoza Kukhala wandalama Koma mulungu ndi amene angaweruze pakuti tonse ulendo wake ndiwomwewu nayenso jereyo ulendo wake ndiwomweyo.
Osadandaula Mulungu ali mbali yanu..Mulungu akutonthozeni..ndipo Mulungu akumenyeleni nkhondo chilungamo chiyende ngati madzi....mulungu ali mbali yanu..
Thanks to you Hanifa Tv for bringing us this story Ndimakutsatani kwambiri nkhani zanu Koma mufunika kukonza pa editing zuoneka kt zimakuvutani kupanga edit zinthunzi zanu pena timakhala ngati tikuonera beyond the scene ija 😂😂😂😂😂
Chuma cha magaza muyaluka nacho ..kulora kuchosa Moyo wa munthu chifukwa Cha 3 pic of maize muli NDI tsoka ..poti muli NDI Chuma chambili mugure Moyo mubwezere Kwa mwini wake iwoso akubwezeren chimanga chanu ..Koma osaiwa nthawi ili mkudza yomwe mudzayankhe
Pepani akubanja, Zokhudza kwambiri 💔💔mzibambo ameneyo akafere kundende koma poti dziko lanthu likukomera olemera.. Idont think you will get the justice 💔💔
Apolsi athu ndi zitsiru za anthu chinyen go basi Anthuni mungomupha nanunso pitani pa sing'anga aphe wachumayo ndi apolosi onse achinyengowo analandira ndarama