Ntanyiwa mulungu akhale nanu bwana chifukwa cha kulimba mtima kwanu pofuna kulimbikisa mitima ya amalawi pa nkhanza zomwe boma likuchita , we love you comrede ntanyiwa may our mighty Lord continue protect you
Amene agule Likoma adzaluza ndalama chifukwa anthu aku Malawi sadaike Likoma for sale so mind you that you shall waste your money..becareful...Likoma it's owned by malawians..dont try it
MTANYIWA is a Chosen one whatever he gets is a blessed thing from the living God. Kuwadekhera Bas Brother Mtanyiwa, Satanic ya MCP yafika ponunkha. Brother Mtanyiwa keep it up God will never allow any evil to fall on you,the living God wants you to accomplish his Mission The true living God never fails. Stay blessed 🙏 Irmao MTANYIWA Stay safe a minha Irmao ✊✊ You are protected and covered in the blood of Jesus Christ.
Southern Region is blessed with three former presidents. There is no way people can lack food when they are there. That can't be the fault of a leader but out of selfishness. Unfortunately, any game that is played out of anger, is always lost.
Mulungu anasankha inu comrade ntanyiwa kuti mutiyimilire pa Kati pathu, ndipo Mulungu yemweyo ndamene atakutetezereni kwina kuli konse mutadzapiteko koma nde a pule agundika tu ndi mwana wawoyotu eishhhhhh China chilichonse mukufuna chikhale chanu nde mukatsamutsa anthuwo apita kuti? Ndakayika ngat anthu akulikoma ngati atadzakubvotereni
Kodi Malawiyi ali mumanja a anthu otani zinayamba zachitika nkale kugulitsa mbali ina ya dziko?? Tiziti achakwera, zikhale, kunkuyu, chimwendo, Hala ndi anyapapi enawo onse achita misala ndi mwazi waku chikangawa???
Palibe amene angakugwireni comrade ntanyiwa Allah ali nanu limozi mcp onse ndi mbuzi zawathu ndi manganya nayeso ndi mbuzi onse a mcp ndi mbuzi ndi dan lu
Mudziti wina akuba misonkho ya anthu omwe akudya chitedzeo ndi mwana wake mkumaba ndalama ku immigration Inu zanu zanthumba mwanu mukuthandiza anthu ndi akubeledwao,Koma chakwera he is cursed ndi family yake yomwe but they will pay for what they are doing