Bravo!! Mr. Kamangira Dzuka Malawi Dzuka. Ma youths this is the right way to fight for our country osati kutumidwa kuyambitsa zisokonezo. Nthawi yakwana kuti achinyamata atenge udindo to shape their future. This is very commendable. More fire bwana Kamangira.
Let all Malawi'an tigwilane manja timusspote mu njira ili yonse chinyengo chikuchuluka kundende angopezeka osauka okha mbava zikuluzikulu zolemela sazimanga Kaya ndalama let's lez fund to support this laywer
Apa Justice wo alowe mu khoti ndi a kamangilawo. Ndipo ikhale pa radio. Mlandu omveledwe ndipo ma CSO ndi ma Judge atatu amvele mlandu wo. Guys dziko limene athu akukayikila ma Court limakhala Lawlessness.
Dziko lidaipa ili it's better maiko anzathu adaonongeka koma ku zachuma adasunthako,koma sikwathu kuno umphawi wa thoo koma kumangopondeleza anthu osuka Iwo nkumalemera modabwitsa why Malawi??? For example njala ili muziko muno sibwino kumafinyana tokhatokha pofuna kusangalatsa anthu oononga dziko ndi odzikonda 😢😢😢
Osawanyengera a justice lenani Manda atumbukawo kuopitsa mtundu wao..ife a malawi tatopa ndi zachinyengo zimene atumbukawa amachita mma office a bomawo..kodi ndi umphawi kodi ? Nkuona Dr H kamuzu Banda anawathamingitsa atumbuka onse azipita kwao in 1987..cos they are all corrupt .them are thieves.. ndiye apa akapitiliza onse atumbuka adzipita kwao not live in the southernbregion or the central region.
Truth is a spirit from God. No one can attack the truth because it's a product of Holly spirit. No matter how much the corrupt judges would try to silence the truth, they cannot win. Kamangila is a God sent lawyer to save justice at it's extreme level
DONT LET THEM,BUT WE NEED THE TRUTH TO FOCUS IN OUR NATION .INDEED IT IS HAPPENING IN OUR GORVERMENT OF MALAWI.START WITH CHAKWERA AND ALL MINISTERS,JUDICIAL ,AND ALL DEPARTEMENTS.