Km this kind of lecturing sometimes zumandikhuxa bwanj Mmalo moti muzapephelera amzanu chikhululuko bas muli busy achibekete Panopat kumalawik kuli zambil zoti kalel sizimachitikai inuo ophuziran muthawi yanu samasephan pakhan ya eid km lero ikangofik mumangotukwanizana apa Be humble muziwapephera amzanu chikhululuk jaman kozan zomwe zilipoz pano a a jaman
Ulaliki wabwino ndithu koma kuchula mbiri ya munthu omwalira kuti anali wa shirik its very unfortunate mukanangokhonza zimene inu munaziwona kuti ndizolakwika in directily not directily nkutheka ena analowa chisalam kuchokera kuzimene iye amapangazo inde tiwalemekeze ndi amene anasunga deen inu ozindikiranu musanabwere choncho tiyeni tiwapemphere chikhululuko osati kuwapepusa MAY ALLAH SHOWERS US ALL WITH BLESSINGS FOR BEING MUSLIMS
Koma amwene ndi makusati mukulankhulana kwanu kwaonesa kuti wabwera kuzalimbana ndi anthu omwe anaphunzira kale kodi tizinena kuti muli PA chiwongoko ndiinu choti muziwe ndi chakuti dini ndi ntchito sizingagwilizane mupite Kwame e mukuwanyozawo samalandila ndalama kutha kwamwezi pomwe Ena inu mumalandila ndiye kumati uza zabwino zomwe akuchita ungokhala zonse ndizolakwika alibe zabwino zomwe akuchita
Sheikh kodi mitiuza mu Quran pomwe aletsa kulandira ndalama ukagwira ntchito ya Deen pakati panu ndi ife pali Quran ndi MA hadith atumiki basi palibe zokangana