Тёмный
No video :(

#PROFESSOR_HASSAN_SAID_ZAMBIA 

1islam
Подписаться 3,1 тыс.
Просмотров 50 тыс.
50% 1

Опубликовано:

 

26 авг 2024

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 190   
@user-vh9uk1jy7w
@user-vh9uk1jy7w Месяц назад
I am proud from Christian to be Muslim ☪️ ❤❤❤
@SUWEDSHAMWKUPE
@SUWEDSHAMWKUPE 12 дней назад
Mashallh
@GoldenBarnet-hv3wj
@GoldenBarnet-hv3wj Месяц назад
Am proud to be a Muslim,Allah is great
@user-ub1vt2kq4s
@user-ub1vt2kq4s Месяц назад
Allah bless you professor mashalah❤❤❤
@SUWEDSHAMWKUPE
@SUWEDSHAMWKUPE 12 дней назад
Allihamdulilah to be a Muslim my dad please protect pokhala slamu paka ifa
@user-gd6zb2bv8f
@user-gd6zb2bv8f Месяц назад
Hohn 14 v 6, Yesu anati ine ndine njira choonadi ndi moyo. palibe munthu adza kwa atate koma mwa ine. Most of theses things brings conflicts among peoople, Palibe mpikitsano pa mawu a mulungu
@user-vn2mz7qd5i
@user-vn2mz7qd5i Месяц назад
Ndinali msilamu koma ndinasiya Chisilamu nditazindikira kuti YESU ndiye njira yowonadi.
@user-gd6zb2bv8f
@user-gd6zb2bv8f Месяц назад
Mulungu akudalitseni kwambiri, munapanga chisankho chabwino.
@HakeemJossam
@HakeemJossam 19 дней назад
munali msilamu koma Osazindikila kungopitako poti makolo Anu amkapita kumeneko
@user-gd6zb2bv8f
@user-gd6zb2bv8f 18 дней назад
Ambuye akudalitseni chifukwa ndi ochepa amene akumaona patali mu uzimu, ambiri ali komweko chifukwa anabadwila momwemo kapena makolo awo anawasiya mzikiti omwe anamanga, ambuye akuthandizeni in everything especially moyo wanu wa uzimu
@user-tk6qh9zs7h
@user-tk6qh9zs7h Месяц назад
Alhamdulillah kuti ndine Msilamu. Ma videos ngati awa adzipezeka ndithu pa RU-vid. In so doing zithandizira uthenga wa Allah kufikira ena omwe ali kutali mosavuta
@SelemanIssahAhmad
@SelemanIssahAhmad Месяц назад
❤❤❤
@RedsonRichard
@RedsonRichard Месяц назад
Nthawi yatha amsilamu inu musasokoneze choonadi
@user-jl6sq3ph1b
@user-jl6sq3ph1b Месяц назад
Akusokoneza ndi chani amenepo mmm
@sharifhenderson6982
@sharifhenderson6982 19 дней назад
Asokonesa pati 😂😂😂
@ghadaffmoosa7535
@ghadaffmoosa7535 12 дней назад
Ma sha Allah may Allah bless u sheikh SAID HASSAN ZAMBIA
@mickchiliko2796
@mickchiliko2796 Месяц назад
Alhamdulillah am proud to be Muslim. May Allah guide me and protect me In shaa Allah.
@ghadaffmoosa7535
@ghadaffmoosa7535 12 дней назад
In sha Allah
@EmmanuelstoneyJere
@EmmanuelstoneyJere 9 дней назад
Afarisi a lero ndamenewa ntchito yao nkuphwekesa Yesu basi
@UmarAjussu
@UmarAjussu Месяц назад
Allah akudaliseni ma sheikh nonse
@ChrispinLunda
@ChrispinLunda Месяц назад
Zamasiku otsiliza amenewa ndiwo omkana yesu aja zimene munthu udakhazikikamo sikopheka kukusutha amenewa simungawauze za mzimu oyela sangave ndiwo umaulula umazindikilitsa umaphuzitsa ngat ulibe mzimu oyela ungalive baibulo ukamaliva kuthupi mzimenezo zovetsa chison ambuye akuzindikilitsen amen
@tauhidtimba
@tauhidtimba Месяц назад
Kumva chichewa umafunikira kukhala ndi Zimu oyera kod?
@chiogamata2560
@chiogamata2560 Месяц назад
Ine anthu inu mmandiwaza apapa Kumva language yako yomwe zufunaso nzimu oyela?? Kukuuza kut iyo ndi kapu yomwela madzi, sumva coz ulibe nzimu oyera?? This thing of nzimu oyera, koma mmaudziwa, mungaufotokoze ndi malemba maumboni?? Concept iyiyi eeeeti eeeeeeish mumadyera guys 🤣🤣🤣🤣🤣
@sharifhenderson6982
@sharifhenderson6982 19 дней назад
Mzimu oyelawo anaulenga ndan??? 😂😂😂
@sharifhenderson6982
@sharifhenderson6982 19 дней назад
​@@tauhidtimbakayatu 😂
@ALICKMASANGANO
@ALICKMASANGANO 19 дней назад
Mmm baba moti ma verse akupereka muthuyu si amu bible
@dennismachemba9514
@dennismachemba9514 13 дней назад
Masha Allah may Allah Grant him jannat firdaus
@promisemakawa1556
@promisemakawa1556 Месяц назад
Im proud to b Muslim, mpaka imfa idzanditenge ndili msilamu
@MpondaBanda
@MpondaBanda Месяц назад
Alhamdu lillah proud to be one hu follows Allah's submission
@MussaMalon
@MussaMalon Месяц назад
Mashallaah Sheikh mulungu akudalitseni ❤.
@blessingsdouglas3
@blessingsdouglas3 Месяц назад
Aaaaaaa ine saidi Zambia nakhala nayepo ndi tambwali uyu
@FathimaMa2
@FathimaMa2 Месяц назад
Alihamudulilahi kwaine mpakana kwa asilamu ose pano pa dhunia mashaalhaa
@DIMZYRECORDS
@DIMZYRECORDS 19 дней назад
Minika ❤❤❤❤
@user-pw4dv1el3d
@user-pw4dv1el3d 20 дней назад
Allahu Akbar. Ma sha Allah. Na am ❤❤😂
@Chayibujackison
@Chayibujackison 21 день назад
Mashah allah ❤ ♥ 🙏
@ShaibuJackson
@ShaibuJackson 12 дней назад
Mashaalla
@frankkasamala6956
@frankkasamala6956 22 дня назад
We need you here at ntonda in ntcheu
@KassimIssa-bn3od
@KassimIssa-bn3od 20 дней назад
Mashalla Allah ndi silamu ndipo tikuphemba kwa Allah ndizafe ndi silamu
@PhiladelphiaManyumba
@PhiladelphiaManyumba 4 дня назад
Devil's deception 😢😢 beware my fellow Christian this is one of the last events Aim of this ceremony is to contradict your faith keep watching 😢😢
@AfredMbeta-pk1cn
@AfredMbeta-pk1cn Месяц назад
Ndizomwe timadikilira,go ahead
@IbrasyaicheWizyx
@IbrasyaicheWizyx Месяц назад
Alhamdulillah for choosing me to be a Muslim❤
@HarnetJauma
@HarnetJauma 20 дней назад
Am proud to be a Muslim ❤
@Robson513
@Robson513 Месяц назад
❤Mashallah
@mariamhassan6788
@mariamhassan6788 Месяц назад
Proud to be a Muslim Alhamdulilah ❤
@BysonBanda-z8q
@BysonBanda-z8q 19 дней назад
I am proud to be a Muslim
@JUBRANBULAYHl-yb4ke
@JUBRANBULAYHl-yb4ke Месяц назад
Mwenyezi Mungu, hapana mungu ila Yeye, Aliye hai, Msimamizi wa milele, Amekuteremshieni Kitabu kwa haki, kinachosadikisha yaliyokuwa kabla yake, na ameteremsha Taurati na Injili kabla yake kuwa ni uwongofu kwa watu. Na akateremsha upambanuzi: Hakika walio kufuru Ishara za Mwenyezi Mungu watapata adhabu kali, na Mwenyezi Mungu ni Mwenye nguvu, Mwenye kulipiza kisasi wewe katika Mwingi wa rehema, vipi hakuna mungu ila yeye ni mpendwa, Mwenye hikima ni yule aliyeteremshiwa kwako Ama waliomo nyoyoni mwao wanafuatwa Hawakusema kuwa kila mmoja Kwa Mola wetu Mlezi. na hawakumbuki ila wenye akili, tusipotoke nyoyo zetu baada ya kutuongoza bila shaka Mwenyezi Mungu hatavunja ahadi yake, mojawapo ya makusudio ya surah. Kudumu katika Uislamu baada ya ukamilifu na ubainifu wake, na kukanusha shaka za Watu wa Kitabu, hususan Wakristo Ni surah ya Madina iliitwa Surah Al Imran kwa sababu familia ya Imran imetajwa ndani yake katika aya ya surah. Herufi hizi zilizotengana zimemtangulia mwenzao katika Sura Al-Baqarah, na zinaonyesha kutoweza kwa Waarabu kutoa Qur’ani kama hiyo ingawa inaundwa na herufi ambazo Sura ilianza nazo, na kutoka kwao wanatunga hotuba yao. Mwenyezi Mungu ndiye ambaye hana mungu wa kuabudiwa kwa haki isipokuwa Yeye pekee na hakuna mwingine aliye hai ni maisha makamilifu yasiyo na kifo au upungufu.
@user-lk3ki9hi3k
@user-lk3ki9hi3k Месяц назад
Nawe hule Zambia ukuziona ngati ndi mngero
@rashidadan2533
@rashidadan2533 Месяц назад
I am proud to be a muslim , Komafunso langandiloti , Ndichifukwachani Muhammad timamupemphela chikhululuko komanso madaliso kwa mulungu ? Kodi Muhammad ndi azibale athu omwe anamwalila oyenela kuwafunila zabwino kwa mulungu ndindani ?
@JohnstoneMwandira
@JohnstoneMwandira Месяц назад
Dzina la mtumiki Muhammed likatchulidwa timanena kuti swalalah alaih wasalamah,( meaning , mtendere ndi madalitso amulungu apite kwa iye). Zimenezi even zimachitikaso kwa Azitumiki ena onse . Issah(Yesu) ndiye timati Alaih Salam Wasalatuh(Meaning, madalitso amulungu apite kwa iye). Nde zimenezi zimanenedwa kwa mtumiki winaaliyese akatchulidwa dzina.
@rashidadan2533
@rashidadan2533 Месяц назад
@@JohnstoneMwandira ok , ndichifukwa chani okhala atumiki a mulungu timawafunila mtendele ndi madaliso , chikhalilenicho anapanga ntchitoya mulungu .
@JohnstoneMwandira
@JohnstoneMwandira Месяц назад
@@rashidadan2533 Zimenezi akulamula ndi Mulungu akuti mfunireni zabwino mtumiki wanu. Nde Ife ndindani kukanira.
@user-jl6sq3ph1b
@user-jl6sq3ph1b Месяц назад
Iweso sisilamu tachoka apa
@LUCKYM4787
@LUCKYM4787 Месяц назад
Manshaallah brother
@ngozo07
@ngozo07 Месяц назад
I'm proud to be a Muslim
@SelemanIssahAhmad
@SelemanIssahAhmad Месяц назад
❤❤❤❤
@user-ei2yt3kf4x
@user-ei2yt3kf4x Месяц назад
❤❤❤
@MahometAli-e8w
@MahometAli-e8w Месяц назад
My lecture Said Zambia you miss me long time no hear you
@peterkinsLekera
@peterkinsLekera Месяц назад
Kwamuthu yemwe sawerenga ndikutsata za zipembedzo adupha nkhani zonse ndikumangosankha momwe akufuna pokwanilitsa zolinga zanu koma choonadi mukuchidziwa
@user-xu9rh1lm8o
@user-xu9rh1lm8o Месяц назад
Pelekan lemba nanu
@chiogamata2560
@chiogamata2560 Месяц назад
Pelekani zomwe mmawelenga inuzooo Ndanga izi zikuchoka mmitu mwao ngat?? 🤣🤣🤣🤣🤣
@khadijailiyasa5315
@khadijailiyasa5315 Месяц назад
Kodi simungayike apapa dawa yonse please tikuyifuna
@abdul-rasheedsalika
@abdul-rasheedsalika Месяц назад
Mposo abaleee, nanga kwinako tikakupezera kutiko sono
@YusufuYunusuSavielMakey
@YusufuYunusuSavielMakey 27 дней назад
Masha Allah pondipanga kukhara msilam ❤
@ghadaffmoosa7535
@ghadaffmoosa7535 12 дней назад
Ma sha Allah❤
@Chayibujackison
@Chayibujackison Месяц назад
Mashah allah sheikh awuzen ndithu❤❤❤
@user-lj7lm6ly7z
@user-lj7lm6ly7z Месяц назад
Chiweluzo chidzapelkedwa chifukwa Cha zintchito zarhu osati proud to be a Moslem or proud to be a chriastian nzopanda pake
@AlkadoNkundwe-wb3of
@AlkadoNkundwe-wb3of Месяц назад
Evidence please !!!!
@raphicallan5331
@raphicallan5331 Месяц назад
Proud to be a Muslim
@GiftSinalo-ku6zb
@GiftSinalo-ku6zb Месяц назад
Alhamudulillah to be a Muslim
@BindulaMtambo
@BindulaMtambo Месяц назад
Mashallah, please upload some more
@JazraJeffm
@JazraJeffm Месяц назад
I'm proud to be a musilim
@martinchimwala
@martinchimwala 23 дня назад
Proud to be Muslim
@SculptActiveSports
@SculptActiveSports Месяц назад
Minika!!!
@JohnAsendi
@JohnAsendi Месяц назад
Dawa koma imeneyo osati zakuti Achibeketi adali mfiti adakuphera agogo ako muzichita Dawa yolimbana ndi amene Sali Asilam timakunyadiran big kep it up
@AKHTARLINGSON
@AKHTARLINGSON Месяц назад
Anayankhulapo choncho iyeyu?
@danielmangalisobanda8356
@danielmangalisobanda8356 Месяц назад
Mr Hassan munaphunzira koma ndinu mbuli yothelatu kuuzimu ndichifukwa chake mukupembedza wovumbulutsa Quran naganiza ndikukhulupilila kuti mukupembedza Mulungu wamoyo, chonsecho ndiSATANA weniweni adamunamidza muhammad kuti ndiiyeyo adili kuvumbulitsila aneneneli amuBible
@Lionelmosse
@Lionelmosse 27 дней назад
Allahmdulillah ❤❤❤❤❤❤
@AbdurashidAhmad
@AbdurashidAhmad 6 дней назад
Tiyeni tafunile zabwino zonse makolo athu omwe anayima pakati pachowonadi chisilamu omwe alimoyo mpakana omwe anasogolera kale kumanda mulungu awapatse jan'na please
@omarmanduwa4127
@omarmanduwa4127 Месяц назад
MAA SHAA ALLAH
@MathpeterLemon-ls1ns
@MathpeterLemon-ls1ns 11 дней назад
Asilamu olambila mwala wa ku arabia saudi dzipumi biii ngati zoona
@BornwellOtala-dm1zm
@BornwellOtala-dm1zm Месяц назад
❤Ma shaaAllah
@YusufuUsumani
@YusufuUsumani 26 дней назад
1 muslim
@PatienceNgulinga
@PatienceNgulinga Месяц назад
Aaaaa Sheik openga uyu kanundu akumupweteka,, mutuwo kukulako ukumulemera
@chiogamata2560
@chiogamata2560 Месяц назад
Kung'alula zomwe mmazidutsa kutchalitchikoka nde mwadabwa nazotu?? Akutenga zammutu kapena?? Else likunama ndi Bible lotu pamenepoo 😂😂😂😂
@user-gd6zb2bv8f
@user-gd6zb2bv8f 18 дней назад
Anthu timasokoneza pakati pa Mulungu ndi Alla, palitu kusiyana kwakukulu, ndipo mudzadzindikira koma mochedwa kusiyana kwa awiriwa
@AbgirlChinheya
@AbgirlChinheya Месяц назад
Alihamudulilah❤
@tomthompson4429
@tomthompson4429 Месяц назад
Where is the other part of Seventh Day part? Let's PRAY that each one of us here on Earth meets GOD's Grace and know the truth, I Pray for you my muslim brothers. Amen
@SaymonMawaya
@SaymonMawaya Месяц назад
Maashallah
@IssahNgalinje
@IssahNgalinje Месяц назад
Mashaa Allah sheikh ❤❤
@cassimmeleka40
@cassimmeleka40 26 дней назад
ان الدين عند الله الإسلام
@UlandaHarjisonstone
@UlandaHarjisonstone 29 дней назад
Allihamdulillah pokhala msilam chonde Allah muzanditenge ndili msilam
@HaliJana
@HaliJana 28 дней назад
MULUNGU AKUONJEZELENI MASIKU AMOYO WANU ADALISESO MU MZELU ZANU
@AshrafSaidi
@AshrafSaidi Месяц назад
Jazakum llah khaira
@user-ky8eq5ek1p
@user-ky8eq5ek1p Месяц назад
Ma Sha AllAh Amee
@OmrahGeraldOmrahGerald
@OmrahGeraldOmrahGerald Месяц назад
MASHA ALLAH MASHA ALLAH MASHA ALLAH
@AbdullahRight-ld2vv
@AbdullahRight-ld2vv Месяц назад
Ma sha Allah ❤❤
@SABITISABITI-yv9jq
@SABITISABITI-yv9jq Месяц назад
🕋🕋🕋🕋🕋☝️☝️
@AsanteBilly
@AsanteBilly Месяц назад
MashaAllah ❤❤
@YasinMusa-ym8lp
@YasinMusa-ym8lp Месяц назад
Macha hallah ❤❤
@SolokingChimzy-yt7dj
@SolokingChimzy-yt7dj Месяц назад
Pakut ngat wakhungu alondole njira akukhungu onse awili azagwa mmbuna....mukazaziwa choona choona chizakumasulani
@user-gj7jh1yx7g
@user-gj7jh1yx7g Месяц назад
Inu chilungamo munachiona bwanji
@MarthaChizi-h1u
@MarthaChizi-h1u Месяц назад
MBULI ZA ANTHU NDIPO PALIBE CHIMENE MMADZIWA
@KelvinMangwengwe
@KelvinMangwengwe Месяц назад
Ma sha Allah ❤
@user-gk6bf7xe9g
@user-gk6bf7xe9g Месяц назад
Masha Allah ❤❤❤❤❤❤
@YatoRoy-kt4lh
@YatoRoy-kt4lh Месяц назад
I once met this Saidi Zambia for almost 8 hrs. Anafika pokwiya titamufotokozera zinthu zomwe iye samadziwa za chiyambi chachisilamu ndipo anakwiya heavy. Amene mumamudziwa ask him za anyamata omwe anakumana nawo usiku mnyumba ina ku mangochi. He ended up a failure on that meeting.
@GiftStephano
@GiftStephano Месяц назад
Chinayamba bwanji tiziwe nao
@user-sb8hi8vc9w
@user-sb8hi8vc9w Месяц назад
Ma shaallah
@mramir.s.smkubwa3985
@mramir.s.smkubwa3985 Месяц назад
Komano kunena chilungamo Alhamdulillah asilamu mulungu anawapasa mzelu ndithu
@shafiemulumbe522
@shafiemulumbe522 Месяц назад
Mashallah ❤
@masebermsanga7623
@masebermsanga7623 Месяц назад
Masha Allah ❤
@Shelifibraheem
@Shelifibraheem Месяц назад
Ameen thummah Ameen
@MariamJaffali
@MariamJaffali Месяц назад
Ma shaa Allah
@chiogamata2560
@chiogamata2560 Месяц назад
Kulowa kumoto kulipo ndiiithu 😂😂😂😂
@KassimShaibu-f6h
@KassimShaibu-f6h Месяц назад
Machalawu
@abhentomwcmwanjeza5771
@abhentomwcmwanjeza5771 Месяц назад
MaShaallah
@danielmangalisobanda8356
@danielmangalisobanda8356 Месяц назад
Mulungu wamoyo wovumbulutsa Uthenga wamuBible akuchitileni chifundo kuti mumudziwe.
@JafaBulhm
@JafaBulhm Месяц назад
Masha Allah Allah Akibari
@adamuhwaduh1080
@adamuhwaduh1080 Месяц назад
Ndipepha Allah kut ndidzamwalire kanali silam
@MussaLameck
@MussaLameck Месяц назад
Alihamdulilahi
@user-du4ng6gx3o
@user-du4ng6gx3o Месяц назад
Salaam aleykum...video muzimalidza osamayidula
@user-xu9rh1lm8o
@user-xu9rh1lm8o Месяц назад
Mashaalah
@UseniMailosi
@UseniMailosi Месяц назад
Mashaah Allah
@ThokozaniChadza
@ThokozaniChadza Месяц назад
Mashaa llah
@danielmangalisobanda8356
@danielmangalisobanda8356 Месяц назад
Ndikudziwa chimene ndikunenachi and i Challenge you
@GiftTwaya
@GiftTwaya Месяц назад
Allah akbr
@Creslevison-vj2sl
@Creslevison-vj2sl Месяц назад
SDA don't do this again cox contextual reading of the bible is vry important,astichocherese awa
@abdul-rasheedsalika
@abdul-rasheedsalika Месяц назад
😂😂😂😂😂 chilungamot always chimapweteka ndithu. Spend your time by searching for the truth.
@MadalitsoWillson
@MadalitsoWillson Месяц назад
❤ mashaallah
@ishmaelmadalet2591
@ishmaelmadalet2591 Месяц назад
When was this debate held
@MathpeterLemon-ls1ns
@MathpeterLemon-ls1ns 11 дней назад
Asilamu nonse ndi ma judger ndekha nonse moto ma vindictivist shupiti
@Randy-er2xo
@Randy-er2xo Месяц назад
Masha Allah shelk
Далее
CRUISE 5 ON MBENJE ISLAND   SALIMA   13 NOVEMBER 2022
1:11:15
MILANDU PA OKALA....Episode 24
11:54
Просмотров 275 тыс.
TIKU 06 AUGUST 2016
29:35
Просмотров 164 тыс.
TIPANGE  DAWA  SAID ZAMBIA
58:39
Просмотров 142 тыс.
BON KALINDO LERO PA 27 AUGUST 2024 |
17:02
Просмотров 4,8 тыс.
EXCLUSIVE INTERVIEW WITH BON KALINDO
59:52
Просмотров 81 тыс.
THE COURT..(Malawi )🤔
20:45
Просмотров 191 тыс.