Тёмный

PROPHET DAVID MBEWE WASAMBWAZA OPPOSITION- ndipo wati mukamalimbirana mipando simuzawina 

NZIKA TV
Подписаться 6 тыс.
Просмотров 42 тыс.
50% 1

Опубликовано:

 

4 авг 2024

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 99   
@KingsleyWakusa
@KingsleyWakusa 10 месяцев назад
Video iyiyi ikamupedze Nakhumwa,,, straight point
@austinharawa720
@austinharawa720 10 месяцев назад
Powerful saying man of God.....
@Homeofpeace321
@Homeofpeace321 10 месяцев назад
This is true, Opposition Mps and leader of Opposition ali weak kwambili, akungoganiza zautsogoleri
@MaryRasmussen-mr4zo
@MaryRasmussen-mr4zo 10 месяцев назад
Amen May God bless you
@Homeofpeace321
@Homeofpeace321 10 месяцев назад
I wish Born Kalindo azatiimilire u president 2025
@MarkManyowa
@MarkManyowa 10 месяцев назад
🤣🤣🤣🤣
@henryphiri6100
@henryphiri6100 9 месяцев назад
Zoona pastor Mbewe akulephera kutsutsa koma akufuna kudzalamulira.chiyembekezero cha anthu ndichotani kwa anthu ngati amenewa.Boma la MCP likutizuza.ndalama zikupezeka ndizoyendera maulendo ake.ndipo mkazi wa Chakwera ndi galu.mzimayi wathundu wanji olephera kudzudzula mamuna wake kuti bambo anthu akuvutika uku.
@user-ty5ih9uo3r
@user-ty5ih9uo3r 10 месяцев назад
Prophert Mbewe .izi ndizona zikhazokha anthu mumalawi muno akuvutika kowophya malawi alipamoto .kuiguptonso pangono .Mulungu ayendere malawi.Mbava sitikuzifuna .usogoleri wazuza anthu uwu
@rashidadan2533
@rashidadan2533 10 месяцев назад
True mr prophet , here in malawi we don't have opposition parties , all of them ndi adyela, even pac nayonso inalowa mbwelela
@innocentliyawo3943
@innocentliyawo3943 10 месяцев назад
The dude is spilling the facts
@Biath-m4b
@Biath-m4b 12 дней назад
Powerful
@FrancisMazamba
@FrancisMazamba 3 дня назад
Zoona zake
@stanleykaludzu-bm4pm
@stanleykaludzu-bm4pm 10 месяцев назад
Very very true Man of God
@user-md5uv2cg6i
@user-md5uv2cg6i 10 месяцев назад
Nankhumwa ndi wa mcp simuziwa
@KonkaMonka-ir2ug
@KonkaMonka-ir2ug 10 месяцев назад
You are a great person
@chikumbutsotsalangu5511
@chikumbutsotsalangu5511 10 месяцев назад
Good advice sir
@ConfusedAstronaut-qv6wq
@ConfusedAstronaut-qv6wq 5 месяцев назад
Great
@alexjeremanuel2541
@alexjeremanuel2541 10 месяцев назад
Prophet Mbewe you're right about opposition and what I can see here is that Malawi has no opposition leader and because of weak APM that's why all these things are happening if it was Bakili or late Bingu this wouldn't happened
@inessmsiyambiri8517
@inessmsiyambiri8517 10 месяцев назад
Ndagwilizana nanu prophet
@user-nz8mq4ff3e
@user-nz8mq4ff3e 10 месяцев назад
This reall prophet David mbewe what he said it's true
@user-oi2fv1pd1y
@user-oi2fv1pd1y 10 месяцев назад
Zoona kulibe oppositon kumalalawi kuma aphungu odzikonda ndi adyera osaganizira anthu osauka
@SquareKandulu-kg3ui
@SquareKandulu-kg3ui 2 месяца назад
Continue 😂
@FlocyMollyGrant
@FlocyMollyGrant 10 месяцев назад
This is so true,,,if they are wise enough let them start now,,,it's high time our leaders start seeing this nation that it is for all of us the government and the opposition
@user-hf4xb5ij3o
@user-hf4xb5ij3o 5 месяцев назад
Kumeneko ndiye kuyankhura
@user-ub1mw7ce5p
@user-ub1mw7ce5p 10 месяцев назад
God is very Merciful and All_Knower. Almighty God knew that in fact there are no opposition parties in Malawi, then God has brought the hope for poor Malawians hon. Bon Kalindo, the president of the poor Malawians. This is shown by the way the called opposition parties in Malawi are silent while nothing is working in Malawi. Only hon. Bon Kalindo is condemning this bad leadership. May Almighty God bless our president Bon Kalindo and his comrades with long live and strength against the devils sent to destroy our peaceful and beautiful country, Malawi.
@mphatsolupiabanda6910
@mphatsolupiabanda6910 10 месяцев назад
They must show leadership now like this dude kalindo
@user-pt8wb4vw6r
@user-pt8wb4vw6r 10 месяцев назад
Amen
@francomwachandejnr6745
@francomwachandejnr6745 10 месяцев назад
Very true
@aminrajab5482
@aminrajab5482 10 месяцев назад
Zooona mbewe
@asiyatujuma5507
@asiyatujuma5507 10 месяцев назад
❤❤❤❤❤❤❤❤❤
@kennethjere9502
@kennethjere9502 9 месяцев назад
I agree he is right.
@user-ep5di5nv4i
@user-ep5di5nv4i 9 месяцев назад
He is right
@user-frasernamaona14
@user-frasernamaona14 10 месяцев назад
Mawu bwana prophet
@lloydmakumba6479
@lloydmakumba6479 9 месяцев назад
I agree
@proactiveisaacbandah4072
@proactiveisaacbandah4072 10 месяцев назад
Exactly
@robertrichman9376
@robertrichman9376 10 месяцев назад
Chilungamo chimawawa, uyu chilungamo anabadwa nacho
@SolomonNjolomole
@SolomonNjolomole 10 месяцев назад
Auzeni zoona Ali tondovi kupusa angoti ndwiiii kungoyanganira .
@AbelKaludzu
@AbelKaludzu 9 месяцев назад
Exactly MoG
@stephanchatatahshezi7036
@stephanchatatahshezi7036 10 месяцев назад
Zowona zake,
@mayesojameskatete
@mayesojameskatete 10 месяцев назад
Zoonadi man of God
@AffectionateDachshund-tz6dk
@AffectionateDachshund-tz6dk 6 месяцев назад
Ndale zapamalawi anthu akutaya nazo mulungu kusatila mdale nconco mulungu akakwiya mudziyankhula zambiri inu anthu odziwa mau amulumgu nanga mukuphatikizilanji ndizachikumja inu ndiye musintha zinthu analipo anzanutu alipo lerowa amayenda bawo kudya usipa pamsika komaso kudya midzimbe ndi anthu komapo amazitcha ku mdiopemphela kom pano zikut tangopitilizani kuuza anthu zanjira yakumwamba bs musapanga ziwiri zandalezi mudana.ndikholo lanu amene ali mulungu
@user-xe9hp2tc4t
@user-xe9hp2tc4t 10 месяцев назад
powerful message
@fosterkatemba1269
@fosterkatemba1269 9 месяцев назад
I don't agree
@MatemangaMoyo
@MatemangaMoyo 20 дней назад
Munthu uyu wayankhula chilungamo​@@fosterkatemba1269
@patrickmacheso5062
@patrickmacheso5062 10 месяцев назад
Especially Nankhumwa is busy fighting with APM and he think like it's easy to be a President of Malawi while people are dying with hunger in the hands of Chakwera.
@sulaimanamiduh5633
@sulaimanamiduh5633 10 месяцев назад
Mawu amphamvu mr mbewe
@user-eh1mg3ww6d
@user-eh1mg3ww6d 7 месяцев назад
Mulungu atisakhile president oopa mulungu
@evaromeo1897
@evaromeo1897 9 месяцев назад
True
@MastonStanley
@MastonStanley 4 дня назад
Kulidandaulila dziko
@inessmsiyambiri8517
@inessmsiyambiri8517 10 месяцев назад
Kaya ndi nneneri onyeli koma akunena chilungamo
@user-pf5er7gc9s
@user-pf5er7gc9s Месяц назад
Mfondo yabwino kwambiri a prophet
@nellikkmwenda7087
@nellikkmwenda7087 10 месяцев назад
Zowona
@CharlesTambala-zn2bd
@CharlesTambala-zn2bd 10 месяцев назад
Things are not okay.... our country looks so pathetic
@SharomKapenga
@SharomKapenga 10 месяцев назад
This is true
@chimwemwechiundira6002
@chimwemwechiundira6002 10 месяцев назад
Truth
@mcsellahntv6896
@mcsellahntv6896 10 месяцев назад
It's true though.
@AlickChima
@AlickChima 10 месяцев назад
Thus my prophet talking ., Tell them.greedy zombies busy waiting for their turn to loot....sizitheka.
@vusoacquaron9084
@vusoacquaron9084 10 месяцев назад
Vuto atsogoleri anthu saganiza zokodza dziko lathu koma kutupisa mimba zawo
@user-ec9sq1ul7o
@user-ec9sq1ul7o 5 месяцев назад
Ndiwe cisilu ukunamizira mulungu eti
@khadijailiyasa5315
@khadijailiyasa5315 10 месяцев назад
Awuzeni busy kumangokangana uko
@Littlefair7
@Littlefair7 9 месяцев назад
Za ziii.
@user-ty5ih9uo3r
@user-ty5ih9uo3r 10 месяцев назад
Prophert mbewe abwera poyera mosaopa kuzuzula boma .kusiyana ndi achakwera anabisarila kuti Ndi abusa koma boza lokhalokha .oyitanidwa ndiambili koma osankhidwa ndiochepa .
@victorbanda9039
@victorbanda9039 10 месяцев назад
Uĺaliki kuchokera palemba lanji m'baibulomo aneneri achinyengo ukatero naweso ukuzipangira kampeni
@AffectionateDachshund-tz6dk
@AffectionateDachshund-tz6dk 6 месяцев назад
Ndinconco kumene
@AnessNezala-jt5fe
@AnessNezala-jt5fe 10 месяцев назад
Ndipo mulungu azikuonjezilani masiku ena amen
@victorkaunda8551
@victorkaunda8551 10 месяцев назад
Wat do u expect wen you put MSCE graduates to deal with crucial matters concerning the economy and country
@isaackaphuka
@isaackaphuka 10 месяцев назад
Zoona
@EmmanuelThom2-xf6ij
@EmmanuelThom2-xf6ij 10 месяцев назад
Nankhumwa ndi mbuz
@shadrachbongololo1143
@shadrachbongololo1143 9 месяцев назад
Ndipo ndikhazika ma speaker Ku parliament Kuti mwina nankhumwa amve
@ChristinaSimwaka
@ChristinaSimwaka 10 дней назад
Sure farther tell opposite
@jeanbotomani9081
@jeanbotomani9081 10 месяцев назад
Mau zosaenda olo
@alexjeremanuel2541
@alexjeremanuel2541 10 месяцев назад
It will be a very big mistake for people to vote for Nankumwa as a presidential candidate and he's not supposed even to be called Vice President of DPP. That's why DPP will have no future and it's shameful for the party that was strong to finish like that because of selfish people like this
@tenexchikumba
@tenexchikumba 9 месяцев назад
Sananeso MP wa DPP kut there opposition is doing nothing
@lukainnocent5380
@lukainnocent5380 10 месяцев назад
mawu koma awa Iwo Ali busy kunyoza chakwera chifukwa akufuna mpando zausatana basi
@greychizaka4088
@greychizaka4088 10 месяцев назад
dzidzudzuleni dzitsirudzi
@husseinmoffatt
@husseinmoffatt 10 месяцев назад
Zoonadi dzikoli sililibwinoyi
@calvinjamal7117
@calvinjamal7117 10 месяцев назад
Nankhumwa empty head
@raymondchilimba7010
@raymondchilimba7010 9 месяцев назад
Well said fake prophet.... This time you nailed it.
@user-mj3ms4jt3b
@user-mj3ms4jt3b 10 месяцев назад
Mneneli wonyenga uyu, mwa uyli mulibe umulungu
@lewisbonongwe8518
@lewisbonongwe8518 10 месяцев назад
Kodi zome akunenazi ndi uneneri kapena zochitika
@ronaldchirwa2506
@ronaldchirwa2506 10 месяцев назад
Zomwe akulankhulazi ndizonyenga? You must be very stupid citizen
@MalizinZinazizi-in4wk
@MalizinZinazizi-in4wk 10 месяцев назад
Kkkk Anthu wenanu sidziwa kusiyanitsa zinthu.. apapa sakupanga uneneli apa akunena ZOMWE zikuchitika..kodi M kulakwa kudzudzula pomwe sipalibwino?? Huuuu umbulitu umenewu
@chrispartsogolani0928
@chrispartsogolani0928 10 месяцев назад
Ndipo live this is true man of God
@user-wd9yd1bg9n
@user-wd9yd1bg9n 10 месяцев назад
Munthu wamulungu sayenera kuopa apa ndiye waonesa kuti ndi mtumiki weniweni
@user-ec9sq1ul7o
@user-ec9sq1ul7o 5 месяцев назад
Ur prophet or multiparty member
@JohnChibalo-wf8gr
@JohnChibalo-wf8gr 10 месяцев назад
Koma zokuti mudziko lamalawi zinthu zikusokonera chifukwa opposition leader ikufooka idzo ndiye zoona opposition iri mbali ya m c p osati anthu ndiye.kusogoloku adzitisokosa muvotere nankhumwa tidziti ndizolondola ?pomwe asakuyimira osauka .😂😂😂😂
@Kamwachale
@Kamwachale 9 месяцев назад
How can DPP oppose the government that the citizens chose to the best of their knowledge. The citizens said DPP was worse than mcp how then DPP can oppose what the citizens chose as best. Don't accuse DPP because of your wrong casting of your vote, don't push DPP to clean the mess you created on your own, be the solution to your political mess
@edwinlerwill6978
@edwinlerwill6978 10 месяцев назад
Evil people what kind of man of God ?
@edwinlerwill6978
@edwinlerwill6978 10 месяцев назад
Shut up neneli onyenga uyu
@bjmtalimanja5073
@bjmtalimanja5073 10 месяцев назад
Wanyenga ndani
@ceciliakungwezo3517
@ceciliakungwezo3517 10 месяцев назад
anthu panja amadana ndichilungamo
@BladesBullets-pu5uw
@BladesBullets-pu5uw 10 месяцев назад
Pepani bwana, boza sitiliveka jekete ngati zikupweteka mukangoseka madata... Onyenga coz akunena chilungamo.
@user-wd9yd1bg9n
@user-wd9yd1bg9n 10 месяцев назад
Mneneli onyenga ndi chakwerayo
@thondoyaenterprise3795
@thondoyaenterprise3795 5 месяцев назад
Dude stay in your lane. U clearly shows u know nothing about economy and procurement. Otherwise u should have talk of solutions.
@ronaldchirwa2506
@ronaldchirwa2506 10 месяцев назад
Powerful
@user-nx7yz4qo8f
@user-nx7yz4qo8f 10 месяцев назад
True
Далее
кажется, началось
00:45
Просмотров 1,6 млн
Israel Malawi Farming, Listen to Prophet David Mbewe
5:25
CCAPYUM SERVICE
42:33
Просмотров 198 тыс.
ZION  BY PROPHET DAVID F. MBEWE # FROM LIWEC
6:52
Просмотров 34 тыс.
NANKHUMWA SIWOYENERA KUKHALA PRESIDENT TAMVANI IZI
5:56