Zimene analankhulapo a Nkuche ndi a Bamusi ine sindikugwirizana nazo. A purezidenti ndi munthu ngati ife tomwe , tikuwanena kuti ali involved mungoziyi ndiye tiyembekezera bwanji iwowo kuti aulutse report imeneyi? Nawonso zikuwawa m'mtima zowanena kuti ali involved. Akawulutsa iwo automatically mnenanso kuti ndi abodza. Ine ndikuganizira kuti ndibwino a MDF ndi amene awulure report limeneli kuti pasakhalenso chikayiko chinachilichonse pa a purezidenti.