Тёмный

The Court Of Malawi 

Jimmy Chimera
Подписаться 12 тыс.
Просмотров 57 тыс.
50% 1

Опубликовано:

 

22 окт 2024

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 41   
@Deajay-jn8cf
@Deajay-jn8cf Год назад
Kkkkkkk koma kumalawi kulizinthu 😂😂😂chizungu ngat vizungu shame my pipokkkkkk
@AlinaChauluka
@AlinaChauluka Год назад
Mzaziii basi mukusiya kulimbana ndimbamva zomwe zikuba ndalama za boma mmmmhh koma mulungu akulangeni ndithu
@stevemasuli8715
@stevemasuli8715 2 года назад
Uyu mumusiye. Chakwela ndi chilima ndinuyo munaba ndalama zambiri. Mulungu athane nanu
@LekeleniUledi
@LekeleniUledi 2 месяца назад
Mukuitha magay big up
@AlinaChauluka
@AlinaChauluka Год назад
Mukanati muzitero milandu iliyonse bwezi zilibwino koma mumapangira asauka okhaokha komanso mukulimbana ndizithu zomwe sizingathandize amalawi olopangono koma koma mulungu oziwa kulanga akulangeni ma judge nonse Malawi muno🙏
@esthergweje4038
@esthergweje4038 Год назад
Kkkkkk tiyeni tziyankhula chichewa apa zizungu si chathu ichi
@Johnmsewu
@Johnmsewu Месяц назад
Zangovuta abale chakwera wandikwana,.Maka moyo ophanawu ai
@alexanderkaunda9554
@alexanderkaunda9554 2 года назад
Chizungu mukuwuza ndani simuzatheka dziko losauka koma vizungu kkkkk
@yusufjailos
@yusufjailos Год назад
Boni yambomayo ndiye mbavayo kufuna kupaka phawiyo
@janetnpaul426
@janetnpaul426 Год назад
Basi inu peya peya kupit kukaona pomwe padulidwa mitengo mulungu akukhululukileni akuba ali mbweee misokho yathu mukulimbana ndizopelelazo
@yusufjailos
@yusufjailos Год назад
Onena chilungamo ndiye mukumanga chilungamocho asananene
@trinitykalima1840
@trinitykalima1840 Год назад
Ena akuba ma billion mulibe nawo ntchto kma kulimbana ndi mphw chifkwa cha mtengo umoz,inuyo ndi amuyaya? Enawa mukuwaponya Pat?
@masterjailos3913
@masterjailos3913 2 года назад
Kupusa basi munaonapo mzungu akuyangura chichewa?
@frankkamunde4575
@frankkamunde4575 2 года назад
Zopusa zeni zeni kusiya mbava zeni zeni zomwe zikuononga dzikoli kumakalimbana ndi munthu osauka ngati ameneyo azimbambo akulu akulu ngati inu mulibe manyazitu
@lacksonsiyadi943
@lacksonsiyadi943 2 месяца назад
Nkhalango mwamaliza maliza kugulitsa mitengo kwa olemela lero muli bzy nd mphawi
@tomothybanda9070
@tomothybanda9070 2 года назад
Mukumanga osawuka mukusiya akuba Gold ndi misonkho ya amalawi why amalawi? Ziwani chomwe chinapangisa kuti akalowe kunkhalango ndinu amu boma no jobs. And magesi amangoyaka 2 hours mukuganiza kuti amphawi iwe tiphirachani mumakomboni? Yambani kumanga akuba mubomawo ndi ena then pezani njira zabwino zathandizia amphawi.
@jafarilulanga6561
@jafarilulanga6561 2 года назад
muthu oti akudya bwinobwino sangarowe muchele ndikumadula mitengo? kod simukwaona amene akudula ndalama za malawi za misongo simumamanga? koma odula mitengo nde eeee☠️☠️💀💀💀💀😭
@zaidiealifualifu9989
@zaidiealifualifu9989 Год назад
Nde mukuvutikilanji ndi chizungu chosecho alipamenepo ndi anthu ot amava chichewa cholinga winayo akhale ndi mantha muwine likubwela tsiku muzuzayankha zimenezi
@chazembaunderson-dm2lu
@chazembaunderson-dm2lu Год назад
Nonse akhoti pantumbopanu mukulimbana ndiwodula mtengo koma wokuba ndalama zambilimbili mboma mukumusiya mbuzi muzatipeza
@dhaoudhiabedinegomaseko2363
Ndiye mwati milanduyu njowona kapena ndimacheza chabe?
@limbanimponda2721
@limbanimponda2721 Год назад
Ndisewero
@dhaoudhiabedinegomaseko2363
@@limbanimponda2721 ok koma samamaliza kaya eishhhh
@jvpondan4332
@jvpondan4332 2 года назад
Á malawi mukufuna umukhale ngati nafni skúti tidzizungu izitu ndi zopusa með mukutizunzatu tikamasauka kukhala opanda chuma
@danielkhinguirossejuliasse1214
Malawi dziko lotembereredwa kupondereza anthu osauka pamene aboma Akuba mabilioni aboma pamene munthu odura mtengo woti adyetse banja alake
@gesinasutherland9241
@gesinasutherland9241 2 года назад
choyamba mukuyenera kudziwa kuti dziko lanthu ndilosawuka
@promise3693
@promise3693 2 года назад
Kumamanga osauka kusia olemera popeza ndrama zao zuchitira umbon
@mcsellahntv6896
@mcsellahntv6896 2 года назад
Za ziiii.
@alephangoma2158
@alephangoma2158 2 года назад
Y not arrest leston Lazaro chilima Joyce peter bingu in gravy yard
@PatrickBello-kz5zm
@PatrickBello-kz5zm 11 месяцев назад
Kupusa
@AureumProtelligent
@AureumProtelligent Год назад
Chichewarising🤣🤣🤣
@wittinessnkhokwe
@wittinessnkhokwe 2 месяца назад
Eya kaya chichewa is our language
@stainlukali620
@stainlukali620 2 года назад
Zoputsa mkuvutitsa anthu osauka musiyaokuba.
@jvpondan4332
@jvpondan4332 2 года назад
Ndipo
@chazembaunderson-dm2lu
@chazembaunderson-dm2lu Год назад
Agalu inu munthu akusowa ntchito mumati ndiana azidya chani agalu inu koma inu ndiye kumaba ndalama muzalangidwa mizimutu ikakwiya
@promise3693
@promise3693 2 года назад
Ndinu opusa nose
@chicoyonas4641
@chicoyonas4641 2 года назад
Zachibwana 😠😠😠😠
@mcsellahntv6896
@mcsellahntv6896 2 года назад
Kodi ndi drama chani??
@dhaoudhiabedinegomaseko2363
Nane ndidziwe nawo
@alexanderkaunda9554
@alexanderkaunda9554 2 года назад
Yr fools
@masterjailos3913
@masterjailos3913 2 года назад
Amalawi English is not urs
@AlbunoCement
@AlbunoCement 2 месяца назад
Sibwino munthu amayiwala.abweze.foni
Далее
Senzo Meyiwa Murder Trial I 08 October 2024
1:55:15
Просмотров 76 тыс.
СДЕЛАЛИ СОБСТВЕННЫЙ МУЛЬТИК
25:15
THE  COURT (Malawi)
24:40
Просмотров 62 тыс.
The court
25:02
Просмотров 49 тыс.
СДЕЛАЛИ СОБСТВЕННЫЙ МУЛЬТИК
25:15