Indeed zosatheka ndi munthu zikatheka ndi Mulungu.. Jeremiah:33.3 'Call to me and I will answer you and tell you great and unsearchable things you do not know.'Matthew:6.33 But seek first his kingdom and his righteousness, and all these things will be given to you as well. May God bless whose who's seek his kingdom and call upon him🙏🙏
There is God in Heaven,, akanakhala azimayi ena akanalolera kupha mwana or kumpengesa kufuna chuma,,but this ready anayima pa choonadi,,God has answered your prayers 🙏🙏🙏🙏
Linakakhala kholo Lina litavomeleza kupha mwana, may God show you the same love that uve shown on ur daughter by saving her life, I pray this shud be the beginning of ur breakthrough,Amen.
Hmmmm kukudani ko muli ndi kuwala Mamie kumene anthu amene Ali oipa sakuonela kukondwa koma kukuzunza mmene amadziwila mpaka akugonjetse... Koma mzimu wa mulungu ukakhala pa iwe sangakugonjetse mdani.... Mulungu alipo amatetezela Ana ake
@Rodwell, Please help her to get the school transfers for the kids so that they can be enrolled back in school. May the Almighty Jehovah continue guiding her in whatever she does. Chiuta ni mulala kwa ife tose.🙏🏿
Jeremiah 20 vs 8 whenever I speak,I cry out proclaiming violence and destruction .so the word of the Lord has brought me insult and reproach all day long . You are facing rejection ,persecution because of the name of the Name Jesus Christ ,you are so blessed mama to the kingdom of God
This is so touching.God is with you Mumie.Our good Lord will renew your strength and make you soar on wings like an eagle because you have put your trust in him.Real definition of a strong woman.
This tale is truly heart-wrenching, resonating with deeper layers beyond what meets the eye. It echoes the harsh realities of poverty, the dearth of education, and the insidious normalisation of male dominance over women. Sadly, this narrative is far from unique; countless women silently endure oppression at the hands of their partners, their voices unheard, and their pain unseen. By the way, who's the artist singing in the background?
Mdima uadana ndi kuunika, ine ndinauzidwapo kuti ndisamapemphere nkhani iyeyo alipo ndizipemohera akachokapo. I was chased out if the house kuuzidwa kuti ndichoke. Ndinachoka koma uku kunali ku south africa.Nkhani ya maiwa, mulungu alinawo ndi cholinga ndipo agwiritsitsa dzina la yesu...akamati nsilikali wa yesu ndiye mai awa. Satana ndo ogonja its realky sad she went though alot