Тёмный
No video :(

UKU NDIYE YALAKWA, ANTHU AKUCHILIMBA BLANTYRE ZOMWE ACHITA🙌🙌🙌 

HOT 265
Подписаться 77 тыс.
Просмотров 197 тыс.
50% 1

Опубликовано:

 

4 сен 2024

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 563   
@chrisboyce2
@chrisboyce2 Месяц назад
Mfiti zopemphera Chakwera ndi mbale wake Usi ndipo anthu inuyo Mulungu akuyendelereni mwapadera ( SKC FOREVER IN OUR HEARTS 💔)
@timothynjakwa3913
@timothynjakwa3913 Месяц назад
ayambe ayendera amayako
@JessicaManda-zm1ug
@JessicaManda-zm1ug 28 дней назад
Amen
@AchinaKellz
@AchinaKellz Месяц назад
Inu agaru yehova wake uti,kupusa ziwanda yehova wamoyo sakhala ndimbava akuba akumpha, mulungu azakulangani osapota zopusa ukule garu iwe chairman
@EscoChingayipe99
@EscoChingayipe99 Месяц назад
Don't judge anyone only god can judge
@user-hl3st3cc4v
@user-hl3st3cc4v Месяц назад
Kodi ngongole imasitha dziko poti mukufuna mwaonjezere anthu mamvuto musise katundu osati ngongole
@ManganiStanley
@ManganiStanley Месяц назад
Ndipo live atsitse katundu
@CatherineDesire
@CatherineDesire Месяц назад
Ngongole pa campaign aoneke abwino
@prettytambala5687
@prettytambala5687 Месяц назад
God bless this thinking, ineso wad like why keeping poor malawians in a bandage yangongole mmalo mokaika mankhwala mzipatara, kutsitsa katundu, kuwaonjezera aziphuzitsi ma salaries kuti aliyese azifikira zinthu mosavuta. Izi zikungoperekaso mwayi kwa mbava za m,bomazo kuti ziziba ndalama in the name of kupereka ngongole kwa amalawi mxiiiii
@CatherineDesire
@CatherineDesire Месяц назад
@@user-hl3st3cc4v maona Ngati ndi thandidzo angobitsa Chichewa kodi NDI ngongore yangati ya fincca adzaole tidziwiya ,adzatenge timinda NDI tinyumba akalephera kubwedza
@Gautengstanzo
@Gautengstanzo Месяц назад
Zimayamba wez wez, sungapangile zinthu pakamodzi
@JasonMailos
@JasonMailos Месяц назад
Mwamchitq bwino munthu wakupha ameneyo angampeleke chilima zoona
@Henry-vw2cz
@Henry-vw2cz Месяц назад
Midzimu yakwiya😂😂😂😂😂😂
@Cathy-oc7vd
@Cathy-oc7vd Месяц назад
Anthu siyani kaduka.. mulungu simunthu.. Mulungu anaziwa kale kuti Usi azakhalapo vice president wa dziko la Malawi. Tivomereze chifunilo cha yehova pa dziko lathu la Malawi.
@tingamasi106
@tingamasi106 Месяц назад
Chifuniro cha mulungu kuti chilima aphedwe?
@user-nv3rf7bl7r
@user-nv3rf7bl7r Месяц назад
@@tingamasi106 eya
@SylvesterMoyowinah
@SylvesterMoyowinah Месяц назад
Mulungu okupha ameneyo siwakumwambayu ai
@esaMoha-dm4kj
@esaMoha-dm4kj Месяц назад
Awus mulibe nselu misimu yah andu 8 yinkukusatilani nkomaso awusseni amalawi ndege yinangwa bwanji osat samanyi munkunenaso mulungu ankuphasani matenda onyassa phamodsi ndi ashankwela mulungu anankuwonani 👌👌👌👌🙏
@user-nv3rf7bl7r
@user-nv3rf7bl7r Месяц назад
@@esaMoha-dm4kj inu mulungu????
@actuarialscience2283
@actuarialscience2283 Месяц назад
@@esaMoha-dm4kj pelepa kuwecheta iseseni. Ambuje Mlungu akunde yakuti uchimbichimbi uyiche kwa mmwejo. Ajaliwe wakulungwa.
@user-qw3hj1hc7s
@user-qw3hj1hc7s Месяц назад
Mcp chipan chonunkha kwambiri 😢😢
@user-nv3rf7bl7r
@user-nv3rf7bl7r Месяц назад
@@user-qw3hj1hc7s chonunkhila ndichiti???
@JamesNgwaya-vz1ox
@JamesNgwaya-vz1ox Месяц назад
Kupha
@patassonelucaszovuta3431
@patassonelucaszovuta3431 Месяц назад
Sewelo leni leni tikufelanji apapa pangosowa mulelemba
@LuundoJohnkabage
@LuundoJohnkabage Месяц назад
😂😂
@alicehananiya
@alicehananiya Месяц назад
Eya pakusowatso make sikono ndi winiko
@henryphiri6100
@henryphiri6100 Месяц назад
Dramatising politics .this guy is useless
@lucianogeoffrey4275
@lucianogeoffrey4275 Месяц назад
Nde mwati ndinu a UTM? Muzivere chisoni bwana😢😢
@WitnessPhiri-zr9uf
@WitnessPhiri-zr9uf Месяц назад
Nde anthu mukuwona akakupasani ngongolezo mulemela mumene Zinthu zikudulilamu tsiku ndi tsiku ndalama ya ngongole siyingakupindulileni asise zinthu pandalama yanu yochepayo ikupindulilani 😢
@JenniferFyson
@JenniferFyson Месяц назад
Powerful prayer 🙏
@user-nr4mi7pt8g
@user-nr4mi7pt8g Месяц назад
Anthu owopa mulungu ngati abusa a chakwera
@stevenfrancism3638
@stevenfrancism3638 Месяц назад
Amalawi tichenjere😢 kwambiri. Timva zinthu.lets think and work together.Tiwunikilane. and love each other ❤
@trymhango1509
@trymhango1509 Месяц назад
Abale mundiuzireko a vp nzeru alibe chifukwa iwo amayenera asanayambe kulankhura kunkhalakaye cohete ose pasonkhanowo popereka ulemu kwa skc ndikunena zimu wawo uutse mtentere kenako kuwapepesa a malawi zaifa ya chilima kwinako mkumakamba mbwerera zakezo
@MosesShaibu-ee8hn
@MosesShaibu-ee8hn Месяц назад
Amalawi chonde osayelekeza kuvotela izi
@spargomw
@spargomw Месяц назад
Ndani angavotere Manga? 😂😂😂
@user-hr6dj4xc8l
@user-hr6dj4xc8l Месяц назад
Musova
@footballhighlightsofficial7248
@footballhighlightsofficial7248 Месяц назад
😅😅😅
@fumbomumba5016
@fumbomumba5016 Месяц назад
Palibeletu Fundo apa koma A vp awa he's only proud kuti ndi vice president
@madakabichi2251
@madakabichi2251 Месяц назад
Kape uyu
@GeraldChisamba
@GeraldChisamba Месяц назад
​@@madakabichi2251kape umamudziwa koma 😂😂😂😂 mesa kape amakhala osauka ngat iweyo
@lameckmajiga5426
@lameckmajiga5426 Месяц назад
Bwana micle usi athu amakukondani kwambili!! Koma pa game yomwe mukusewela ndichakwelayi athu akutulukani chifukwa azindikila kuti inu muli under M.C.P mukanakhala kuti mukutengapo gawo muma program ama candle 🕯 komanso kuchita zomwe anthu ena a UTM akuchita mukanayenda moyela kwambili komanso zikuwoneka kuti mukufuna kuzutsa chipani chanu cho odya zake alibe mulandu!!! Ife tikanakuvotelani chifukwa cha chilima koma mwaluza basi!!! Pepani bwana usi!!!
@KizitoChikuni-dy9us
@KizitoChikuni-dy9us Месяц назад
Akuwa patipo anthuwo yogulisira kut tionere imeneyo? Zopoila
@user-pb7mn1kx4t
@user-pb7mn1kx4t Месяц назад
Blantyre inachulukadi mbuzi,am from by city koma delali ndi la nkhumba basi
@GeraldChisamba
@GeraldChisamba Месяц назад
Munachuluka amoya 😂😂😂😂
@YatoRoy-kt4lh
@YatoRoy-kt4lh Месяц назад
The guy has a good heart
@JamesIngeni-ku3qj
@JamesIngeni-ku3qj Месяц назад
Which good heart ndi oipa uyu trust me
@WedsonZuzewatayamakina-rn8yp
@WedsonZuzewatayamakina-rn8yp Месяц назад
Ndiye mwati chani😂😂😂😂 ine sindinatolepo mfundo atah olo pang'ono
@KennedyPhiri-h9h
@KennedyPhiri-h9h Месяц назад
❤❤
@geokah78
@geokah78 Месяц назад
We need a system that everyone fine support without being influenced by any political figure. Dr Usi reflect on this.
@user-qt7hx7hq4f
@user-qt7hx7hq4f Месяц назад
Nde munayenda basi nkumawauza anthu zoti ndinkavala ma kabudula awiri ..zitithandiza chani ngt a Malawi
@tiwongehojaney5873
@tiwongehojaney5873 Месяц назад
A chairman wo akalamba😂😂😂
@Cathy-oc7vd
@Cathy-oc7vd Месяц назад
Ndiye kukuwa mwalemba pa munthu wa nkhanipo akuwa pati reporter wa bodza iwe
@GeraldChisamba
@GeraldChisamba Месяц назад
😂😂😂😂 😂😂😂 always cadet amatero mix mizimu yama albino
@EmmanuelstoneyJere
@EmmanuelstoneyJere Месяц назад
Olo opepherayo akuona ngati akupanga sewero ndi manganya
@LawrenceBelson
@LawrenceBelson Месяц назад
Mizimu ya anthu 13 yayamba kuonesa unya nawo ayise kufupika ngt mchimba
@MillyKachepa
@MillyKachepa Месяц назад
😂😂😂😂😂😂
@augustMag
@augustMag Месяц назад
Apa ndiye ndikufuna nyimbo ija anayimba Joseph mkasa anasankha olakwika
@HappyBirchForest-zy8nq
@HappyBirchForest-zy8nq Месяц назад
Ndipo zoona
@user-qo3kg6rv9f
@user-qo3kg6rv9f Месяц назад
Komanso zokamba zake ndi zabwata bwata phuuu
@randettaclaan
@randettaclaan Месяц назад
Kodi Dr. Micheal Usi ndiu wa DPP kapena wa UTM///////////////// Nanga slogun ya woyeee ndi ya UTM
@juntoiman
@juntoiman Месяц назад
100 percent walankhula zondigwira ntima bale
@user-ky4ce9gb6j
@user-ky4ce9gb6j Месяц назад
Kkk
@user-ky4ce9gb6j
@user-ky4ce9gb6j Месяц назад
Zaziii
@NenaniMwamadi
@NenaniMwamadi Месяц назад
Zasewerooo bas usiì
@RachelKamanga-vt3fp
@RachelKamanga-vt3fp Месяц назад
Ambuye akupaseni moyo wautali me utsi muzina loti musinthe malawi wathu Ufumu unasata Daved kuubus chifukwa choti mulungu sakuva zaanthu
@user-vw7tj2ss3l
@user-vw7tj2ss3l Месяц назад
Fundo pa line katundu anali azanu anja inu ndi achimulilenji sakusiyan
@actuarialscience2283
@actuarialscience2283 Месяц назад
Mbuzi iyi ya MCP. Usi usanamize anthu ndiwe wa MCP. Wavala za MCP osati UTM. Ukunamiza ndani nyani iwe. Pamtumbo pako Usiku.
@ManganiStanley
@ManganiStanley Месяц назад
Galu kwambiri ndipo akundinyansa kwambiri
@omardyman8083
@omardyman8083 Месяц назад
Osaiwalatu ndimazimbabwe awaa​@@ManganiStanley
@user-zl9vj6hc6y
@user-zl9vj6hc6y Месяц назад
*wayankhulapotu .. Koma ndege inagwa chifukwa chani bwana*??
@LovenessShugar
@LovenessShugar 2 дня назад
Ine ndikufuna Dr usi ife tikufuna thandizo lawo ngongole atipase
@JohnKanjete
@JohnKanjete Месяц назад
🤗🤗🤗🤗anthu sakukufunani bamboo asikono mwakhalila mpando wamagazi 😊
@user-nv3rf7bl7r
@user-nv3rf7bl7r Месяц назад
Inuso ndinu a boza pena nanga akuwa pati apa chimutima cha nyawu icho
@HappyBirchForest-zy8nq
@HappyBirchForest-zy8nq Месяц назад
Ngongole muyambe mwaona tikuyandikila mavoti 4 years munalikuti kuti muwapase ngongole mwabwera nthawi yochedwa inu mwapha chilima nde mukuona kumene ali chilima akusangalala muvutikapo apa panya panu ana anjoka inu
@user-hr6dj4xc8l
@user-hr6dj4xc8l Месяц назад
Ngongole ilibe nthawi , utha kutenga olo tsiku lovota
@prettytambala5687
@prettytambala5687 Месяц назад
You can say this again, anthu tavutika all these years iwowa qnali pheee ,kumangokweza zinthu ndalama akusungira campaign? Rubbish
@HappyBirchForest-zy8nq
@HappyBirchForest-zy8nq Месяц назад
@@prettytambala5687 eti nde panopa akimalubwa zausilu aba ndalama za amalawi ena agwidwa nazo zana
@HappyBirchForest-zy8nq
@HappyBirchForest-zy8nq Месяц назад
@@user-hr6dj4xc8l khalani ndi umunthu inu nde ubwino wakuba ndalama ndi uti? Mesa kumangophelatu dziko chithyola anamupeza nazo zana president nkumati musiyeni azipita what doesn't mean you're rubbish
@patesnkajenda4258
@patesnkajenda4258 Месяц назад
Fundo palibe bwana ingodyelanitu basssssss😂😂😂😂😂😂
@user-im7sc2my4w
@user-im7sc2my4w Месяц назад
Uyudi ndi manganya srs ,masewero paliponse
@RatifMakiyi
@RatifMakiyi 5 дней назад
Usi Khala serious ukulongosola zithu zisamveka kutundu wa malawi
@HarrisMathew-ve5ib
@HarrisMathew-ve5ib Месяц назад
Akuti kukhalatu ma Team ampira uku 😂 😂
@alfredbamusi1093
@alfredbamusi1093 Месяц назад
Ndi ntchito yabwino kuti akuzipanga available to the public anthu apempha ngongole kuti upange boost capital chomwe ndi chabwino koma zimafunika kuti ayambile kukonza moyo wa ma customer amene ali anthu ogwila ntchito m'boma ndinso ma labour onse azipasidwa ma salaries omwe atazipanga match kukwera kwa mitengo ya zinthu omwe ndi ma buyer ama businesses amene akuvuta kupita pa tsogolo
@CathrineBizza
@CathrineBizza Месяц назад
Mfundolesi usawi kkkk
@ShepherdChisale
@ShepherdChisale Месяц назад
Musamatichotse feel nanu......penapake muzingodula pofunikila pokhapo. Ma Bandle akuvuta kale awa😢😢😢😢
@JumaGadaff
@JumaGadaff Месяц назад
Mwayankhula bwana koma ndege inagwa bwanji boss 😂inuyo bwana ndinu opanda mnzelu mulungu akukantheni chisanathe chaka muyankha mulandu
@HappyBirchForest-zy8nq
@HappyBirchForest-zy8nq Месяц назад
Umayankhula bho heavy
@user-nv3rf7bl7r
@user-nv3rf7bl7r Месяц назад
@@JumaGadaff kafuseni mulungu kuti ndege inagwa bwanji chifukwa ndamene amadziwa chilichose
@IanChidothe
@IanChidothe Месяц назад
Ndipo akudziwapo kanthu uyu
@rasnocuss4183
@rasnocuss4183 Месяц назад
Chirimba one love!!!!!🎉🎉🎉🎉❤❤❤❤🎉 mwana wapaden Manganya
@user-je8jm5uy1q
@user-je8jm5uy1q 27 дней назад
Zopepela zakozo osamantchula mulungu ukuwona ngati mulungu ndiwosewela naye
@UsenLashid
@UsenLashid Месяц назад
Tengani ndalamazo or musazabweze Ayi ndi misonkho anu atuzuza thawi yayitali tengani zaulere
@lawrencekayona9247
@lawrencekayona9247 Месяц назад
Ndinaonela atapanga comedy as a president of the republic of Malawi lelo izo
@LucyTatianahChikwekwe
@LucyTatianahChikwekwe Месяц назад
Usi mu ma speech akewa mmmm chikondi chikupelewera bwenzi ali mu chisoni 🙏
@prettytambala5687
@prettytambala5687 Месяц назад
Bambo asikono woyeeee😅😅😅
@DevisonHala
@DevisonHala Месяц назад
Monga muja mudamukondera chilima kuchikangawa pomupereka kuti aphedwe koma inuso mudzafa kulibe wa mbewu
@wotchidawood
@wotchidawood Месяц назад
😂😂😂😂 yakwiya ndi midzimu bambo uwona wamphesa chilima garu iwe
@FrankMasamba-uk6mc
@FrankMasamba-uk6mc Месяц назад
Iweyo Usi ukamalankhula kumatchula dzina la chakwela , panyapako kwambir
@mishecksipolo7153
@mishecksipolo7153 Месяц назад
😂😂😂😂😂😂😂akutopetsadi bwanji ameneyu
@AlexZanda-e5i
@AlexZanda-e5i Месяц назад
Ndakunyadilaniii amalawi welocom to Tanzania
@user-im7sc2my4w
@user-im7sc2my4w Месяц назад
Apapa yalakwa , Mr Usi mwakwiyisa anthu kwabasi shaaa
@johnmpatama1461
@johnmpatama1461 Месяц назад
Mzimu wa Chilima waononga microphone 😂😂😂
@LuundoJohnkabage
@LuundoJohnkabage Месяц назад
😂
@SamKaposa-i5c
@SamKaposa-i5c Месяц назад
😂😂😂
@user-nz7oz7lx5f
@user-nz7oz7lx5f Месяц назад
😂😂😂
@arthurkayuza
@arthurkayuza Месяц назад
Is that soccer player from chirimba?
@user-bp6cq5pe3c
@user-bp6cq5pe3c Месяц назад
Za ndale doest require presence of God. Ndale nzasatana who rules
@user-nj5vu8cd5l
@user-nj5vu8cd5l Месяц назад
My vote only for USI, I president of my heart
@user-oc6xd4tv9l
@user-oc6xd4tv9l Месяц назад
,😂,😂😂 akuti lathulija manganya woyeeee
@user-px9gd6fc6w
@user-px9gd6fc6w Месяц назад
😮e paka manganya oweeeee mmmmmmhhhhhhh
@SamKaposa-i5c
@SamKaposa-i5c Месяц назад
Mpaka bambo asikono woyeee😂😂😂😂
@IssahAluba
@IssahAluba Месяц назад
Zomwe akulimbana nazo athu awa zaziiii, noe mukuyenera kutsitsa zithu mtego komaso mudziwe kt kugwa kwandarama yathu yakwacha mukuyenera kuganiza kwambili mukapanda kutelo zithu zizativuta mpakana kale
@JaneMhango-zl6pt
@JaneMhango-zl6pt Месяц назад
Kujaila kungongola ndiye mulephere kubweza ndalamazo. Dziko la malawi latha ili. Ma president ake ndi akuba onse.
@user-lk8kj9zv6x
@user-lk8kj9zv6x Месяц назад
Komano za ndege ya kuchikangawa zinayenda bwanji
@Extratremendouszeus
@Extratremendouszeus Месяц назад
Sangayankhe ..ndi yudasi iscariot
@tamalangoma2765
@tamalangoma2765 Месяц назад
I thought kafukufuku adakali kuchitikabe?
@Extratremendouszeus
@Extratremendouszeus Месяц назад
@@tamalangoma2765 look sharp..use common sense. Pakamwa pa usi sipanalankhule zachilima mpaka lero
@elbeys783
@elbeys783 Месяц назад
Awaso nde ayi, athu akuvutika osamuuza za umphawi wanu muli ndalama osamatipusitsa
@RhodaBandah-sh1ir
@RhodaBandah-sh1ir Месяц назад
Chakwela satipasaso nsimayo Ukuyakhulabwanji iwe manganya
@JackNagoli
@JackNagoli Месяц назад
Koma ma comment wa abwana mukuwaona? 😂😂 timaganiza kaye zokalakhula sitikufelanjitu iyi iya
@Gautengstanzo
@Gautengstanzo Месяц назад
Zimayamba wez wez am sure manganya akonza zinthu, very soon katundu atsikaso
@RhodaBandah-sh1ir
@RhodaBandah-sh1ir Месяц назад
Ngongole sisitha zithu bwana ..mungowawonjezela mavuto Kasiseni zithu kuma shop full stop
@REXCHARLESKAJAWO
@REXCHARLESKAJAWO Месяц назад
Bambo asikono ife sitikufuna ngongole ai, coz ngongole yo ndiye mavuto oooopsa Kwa ana anthu. Koma pangani zoti zinthu zisike pansinka kuti aliyese athe kufikira mtengo wakatundu osiyana siyana emwe mtengo wake wachita kuopsa ngati muja uchitila mkango
@GIFTEDWARDCHIGUMULA
@GIFTEDWARDCHIGUMULA Месяц назад
MP wachinyamata and chi player mbambande🤜🤜🤜, msikawo akonzedi eee
@user-mf5ce9wj4m
@user-mf5ce9wj4m Месяц назад
It's so sad to see Malawian are still fooled by MCP.what a hell
@EdwinHowardmkandawire
@EdwinHowardmkandawire Месяц назад
Bola Ali vice president basi olo anthu atakuwa
@user-kr1tf2tu7s
@user-kr1tf2tu7s Месяц назад
Iweyo ukati kumdula kwa zithu,,Ausi amapanga zithu usakafunsa ama factotry bwanji za umburi
@DeliaKaduya
@DeliaKaduya Месяц назад
Musanayambe kukamba zasewerozo mutatiyankhako kaye funso likumatisowesa mtendereri, Kodi ndege inayenda bwanji ku chikangawa? Zangongole zanuzo ifeyo ayi, munali kuti ndi chakwera wanuyo? Nkhani ndikusisa katundu, zinazo mukakambirane ku state house
@AbdulhameedWyson
@AbdulhameedWyson Месяц назад
Chisilu iwe
@DeliaKaduya
@DeliaKaduya Месяц назад
@@AbdulhameedWyson tangopita ukalandire nawo ngongoleyo munthu iwe
@SurprisedFlamingoBirds-ko1dw
@SurprisedFlamingoBirds-ko1dw Месяц назад
Uyu SI wa UTM ayi,asagawanise chipani,ingoimilani indipendent yo basi
@manfredzalirabetha2440
@manfredzalirabetha2440 Месяц назад
Galu wamuthu uyu yudas scariot wamuphetsa chilima iwe sizikupindulira zimenezo mzimu wa chilima ukuzunzani nonse ku chikangawako
@clintonhodda9830
@clintonhodda9830 Месяц назад
Musapusitsike Chakwera anabweranso modzichepetsa
@EnockMaluwa
@EnockMaluwa Месяц назад
Wise words Dr utsi
@user-vq5fe6mo6o
@user-vq5fe6mo6o Месяц назад
Koma abale osapha wanthu mlungu azakulangan inu ife kumuz timavutika timasowa chakudya kamba inu atsogoleri kukweza katundu tikhulupilirapo chan apa
@AnitaChakwana
@AnitaChakwana Месяц назад
Ati olo magalimoto apange ng'wing'wing'wii uyu anazolowela sewelo 😂😂😂
@kelvindickson
@kelvindickson Месяц назад
Kkkkkkk munafulumila kumusogoza nzanu ndichifukwa zambili zikungooneka zopelewela
@earnestchapita2194
@earnestchapita2194 Месяц назад
Nanga bwanji asilikari sadaseke maso popemphera bwanji
@MeshackLondwa
@MeshackLondwa Месяц назад
I don't think bodyguards closed their eyes 😂😂😂😂😂 , Amen.
@DarlingtonChinyamunyamu
@DarlingtonChinyamunyamu 2 дня назад
Chinyamu50
@HappyAbyssinianCat-xt2bm
@HappyAbyssinianCat-xt2bm Месяц назад
Ife àngon tikulira mwana wakwathu kuntcheu kapolo iwe galu iwe olo mcp sitikuifuna ukulankhura zapambolo pako
@EscoChingayipe99
@EscoChingayipe99 Месяц назад
Amen powerful player
@KestenMukhwapa-qp2gj
@KestenMukhwapa-qp2gj Месяц назад
Za ziii zeni zeni zopanda ndi Schererville womwe
@HalisonSolomon
@HalisonSolomon Месяц назад
Iwe ukati kaduka ukutanthauza chani nawe zausiru , MULUNGU wake utiyo amene anaziwakuti mfiti usi adzakhala vp, u vp ochita kupherau ndiye ukamutchule MULUNGU usatchule dzina la MULUNGU pachabe akukwapula , us si MULUNGU koma anapangana ndi chakwera kuti aphe chirima kenako ampase u vp ngati akutuma kuti uziwaikirakumbuyo agalu amenewa ndiye wauponda awa palibe chao afiti opemphera
@user-qh4dd6nq3k
@user-qh4dd6nq3k Месяц назад
Kma chilimba 😂😂 zoti anthu aliokwiya ndi ifa yachilima ndiye aziti ndiambuye
@FrynessMoyo-to2du
@FrynessMoyo-to2du Месяц назад
Koma manganya ndi udindo wa VP sidzikugwilidzana guy's 😂😂 iyi ndi minyama
@Shelifibraheem
@Shelifibraheem Месяц назад
Zamakabudula akowo anthu apindula nazo chani pomwe anthu akugona ndinjala. Dzuno pamenepo panali ena lelo ndiwe ndipo mawa ndi ena samala osatenga Malawi kusowa zochita.
@PetrosGere
@PetrosGere Месяц назад
Kķkķkkk Koma nde kunabebatu
@yusufsadic2930
@yusufsadic2930 Месяц назад
Ndikuon ngat Anthu anu okuthandiziran sadakuthandizen Kungokhal ngat sewer sinthan okuthandiziranio
@user-xr9mc5hg5t
@user-xr9mc5hg5t Месяц назад
Munthu ukamangitse okusakira mtchele
@SylvesterMoyowinah
@SylvesterMoyowinah Месяц назад
Kodi muli pa campaign 😢😢 kodi
@umboneyusufu4499
@umboneyusufu4499 Месяц назад
Aka manganya ngati adalephela mayeso awumphunzitsa nde lelo angatukule Malawi
@IbrahimkDyman
@IbrahimkDyman Месяц назад
Kodi uyuyo akuona ngati ndioziwa tchito 4year yathayi anali kuti (manganya ayenera kubwerera ku tikuferanji)
@vincentkhunsanama584
@vincentkhunsanama584 Месяц назад
Ngongole mumupatse munthu ogulitsa zitumbuwa mwati
@IdahCharles
@IdahCharles Месяц назад
Ukudabwa mmesa uli pamenepo kamba ka imfa😢
@CharlesChagudubuka-rm6bh
@CharlesChagudubuka-rm6bh Месяц назад
Tamangodyani ndalamazo bas,uku tikudikira report la kuchikangawa,koyenda ndege ma hours 3800, ngati imayenda wapansi
@HappyBirchForest-zy8nq
@HappyBirchForest-zy8nq Месяц назад
Ndipo inu
@user-su2dq5lr1h
@user-su2dq5lr1h Месяц назад
Amalawi azanga Pena mukamalakhula muziganiza osamangokamba zithu zopanda umboni musiyeni usi ndi thawi Yake iyi yakwana
@FrankHaruni
@FrankHaruni Месяц назад
Akuluwa alindifundo dxopusa kobasi adximuudxa Chakwela dxoti mulungu simuthu amasithadi kom osati kwaife ndiwe galu kobasi
Далее
FAULT FINDING- Episode 168
12:25
Просмотров 45 тыс.
MILLION JAMOASI 2024 4K
2:17:51
Просмотров 11 млн
3d printed demon core vs real
00:24
Просмотров 6 млн
BON KALINDO KUNG'ALULA MWA NYOO!! 5 September 2024
43:54
DRIVING SCHOOL- Episode 166
15:17
Просмотров 99 тыс.
Zomwe Zinachitika Kut Ndege Isowe
5:19
Просмотров 249 тыс.
Oimba omwe ananyozapo Bushiri
13:06
Просмотров 490 тыс.
TIKUFERANJI 25 MAY 2019
29:39
Просмотров 529 тыс.