Uladi Mussa facing Lazarus Chakwera, joins MCP from Prison.
A Uladi Mussa alengeza kuti tsopano alowa chipani cha Malawi Congress Party (MCP). A Mussa alengeza izi lero ku Salima pamsonkhano wa chitukuko omwe mtsogoleri wa dziko lino a Lazarus Chakwera akonza. A Mussa ndi m'modzi mwa anthu omwe adachotsedwa mu chipani cha Democratic Progressive Party masiku apitawa.
SUBSCRIBE
28 янв 2024