Тёмный

WADZIDZIMUSA ANTHU UKU VP NDIKA SURPRISE VISIT ku Chikhwawa District Hospital...atutumuka😂😂😂😂 

LIKI-LIKI Ladies
Подписаться 50 тыс.
Просмотров 17 тыс.
0% 0

Опубликовано:

 

26 авг 2024

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 93   
@Vinic-f3w
@Vinic-f3w Месяц назад
Malawi needs such heart ❤,,,, continue VP
@abangaabanga4677
@abangaabanga4677 Месяц назад
I commend this, this needs to be encouraged, please continue, with this kind of mentality Malawi will rise, God bless 🙏
@DeborahHetekere
@DeborahHetekere Месяц назад
This is good development that's the spirit that we need as malawians,,,this is exactly what Late Dr Claus Chilima wanted
@mthawisakaunda
@mthawisakaunda Месяц назад
Zipatala za boma mavuto aakulunso ndomweo. Ogwra ntchto amafika nthaw yomwe akufuna and sayambanso ntchto nthaw yomwe afklayo amayamba wakhala kae akut kupumula then ayambe kugwra ntchto. Imafika mpaka 9 asanayambe ai. Chomwe amadziwa nkutukwana ma patient bas
@giftsululu4274
@giftsululu4274 Месяц назад
Ku utm''' '' mukuona koma... Mwataya gold
@user-dy4gc2hr5e
@user-dy4gc2hr5e Месяц назад
Kkkkkkkkk koma vic wake kashoti
@veronicamalisero2671
@veronicamalisero2671 Месяц назад
A VP ndipo muyendele ma office onse aboma,,,....amakhala pa mtambasale anthu awa..keep it up, ,,,....
@masalinodovu1705
@masalinodovu1705 Месяц назад
Excellent Mr VP izi nde zofunikira kwambiri
@FloridaOssy19
@FloridaOssy19 Месяц назад
❤❤❤❤❤❤ mwayamb bwino a manganya
@DinahNantchengwa
@DinahNantchengwa Месяц назад
Proud of you Mr president, zikamatele dziko lathu liziyenda bwino, anthu muzipatsla amataililadi koma akamalombikitsidwa choncho ziziyenda
@vanalphamphaya3518
@vanalphamphaya3518 Месяц назад
Big up the VP continue the good work you started when you were there long time.
@robertkalima874
@robertkalima874 Месяц назад
This is great. ife ogwira ntchito mboma tikugona kwambiri. Ngati sitifuna ntchito titsanzike
@Ella13400
@Ella13400 Месяц назад
Mr Usi pitilizana mwina malawi akhonzaaa.......
@AfickDaud
@AfickDaud Месяц назад
Kukhala ngat madam akunyumbatu Mr Manga kkkk mukuchta kukhalana mmene mukuendamo
@omarlux3434
@omarlux3434 Месяц назад
Osafuna.asye ine ndikuva kukoma ndi vp wathu
@user-nj5vu8cd5l
@user-nj5vu8cd5l Месяц назад
Zama reform please a vice president yambsnipo before 2025
@RiaThomKata
@RiaThomKata Месяц назад
Well done Mr president
@ChifundoChikakwiya-kf1is
@ChifundoChikakwiya-kf1is Месяц назад
😂😂😂 It is promising slowly but let's hope greedy people won't disturb him
@elisaPhiri-k1e
@elisaPhiri-k1e Месяц назад
Ma patient kumvetsa chisoni pogona pamene ndalama zaboma zikungobedwa mmm
@nyasavoicebox
@nyasavoicebox Месяц назад
Good on the Right Honourable the Vice President for being positive. Especially when dealing with the young nurse. Samakalipa koma kulangiza kuti mavuto akunyumba aliyapo iyi ndi ntchito anthu amakudalilani muziyesesa ku bwela ku ntchito on time. Even when dealing with the DHO the conversation sinali yoti ine ndiwonke kuti ndine VP but after reprimanding her he made her feel safe to elaborate on the challenges their hospital and district are facing. Politics aside, this guy may actually care about improving Public Service Delivery in Malawi.
@DanMhone-iw6xg
@DanMhone-iw6xg Месяц назад
Zikachita bwno tiziyamikilako wakulu mwayamba bwno
@abbasjutasi909
@abbasjutasi909 Месяц назад
Iwe nde akuphela kutulo iwe za ndege wachepa nazo Good job apule
@mcsellahntv6896
@mcsellahntv6896 Месяц назад
😂😂😂😂😂 olo pa Lunch
@RotNkhoma
@RotNkhoma Месяц назад
Let's continue mr vp you need to go different department of government9, we need great malawi
@GraceGonani
@GraceGonani Месяц назад
Anthu ogwila ntchito boma amatailila kwambili mwina apa atengelapo mphutzilo😊
@HassanMaganizo-im6nk
@HassanMaganizo-im6nk Месяц назад
Kkkkk kodi limeli ndi sewero lakutiferanji kodi😂😂😂😂
@mayesouldphiri9889
@mayesouldphiri9889 Месяц назад
Iyi ndi tikuferanji ya srs 😂😂
@TizifaBanda-xn5tm
@TizifaBanda-xn5tm Месяц назад
Civil servant kumakhala ngati ant civil servant.worse ku chipatala it's beyond ntchito.
@user-ib7li8pm5h
@user-ib7li8pm5h Месяц назад
Uyu apwetekaa anthuu
@GiftDaftala
@GiftDaftala Месяц назад
Sizikukhala or pangono he can't even afford chilima's footsteps
@blessingsmunthali9202
@blessingsmunthali9202 Месяц назад
Understand that Mulungu atilenga mosiana and everybody is unique 😊
@user-mi3fw1zg8b
@user-mi3fw1zg8b Месяц назад
Mr VP Usi u did it well 👏
@GraceZumazuma
@GraceZumazuma Месяц назад
Anakapangaso check ku pharmacy ngati kuli mankhwala okuti odwala alandira?
@user-nj5vu8cd5l
@user-nj5vu8cd5l Месяц назад
Well done VP usi. Ntchito yofunikira
@mthawisakaunda
@mthawisakaunda Месяц назад
Nurse kukanika kuyankha mafunso a a Usi in English Kkkķk Malawiiiii...bolakotu a DHO 🎉
@chigokhalid9420
@chigokhalid9420 Месяц назад
Wakwanisa komanso Mbali ina anali mantha plus I think sanaganizile Kut akumana ndi VP
@MtenjeHassan
@MtenjeHassan Месяц назад
Zayambika 😂😂 big up mr usi....
@fredbmazuwa8066
@fredbmazuwa8066 Месяц назад
VP you have got my thumb
@brothertonekathyole7349
@brothertonekathyole7349 Месяц назад
Keep it up our VP!
@user-nu1dj3jh7b
@user-nu1dj3jh7b Месяц назад
That's my VP ❤❤❤❤
@ChimwemweDemelo
@ChimwemweDemelo Месяц назад
Big up Mr vp
@FestoniehJim
@FestoniehJim Месяц назад
Izi ndie zalowa sewelo ndithu
@MenasKaliati
@MenasKaliati Месяц назад
Uyu ndiwasero basi😂😂😂
@BrendaJali
@BrendaJali Месяц назад
Good move
@user-to5rp9fu8b
@user-to5rp9fu8b Месяц назад
Mukawaopsezeso ku mapasport uko kuli chinyengo
@janemanyamba7201
@janemanyamba7201 Месяц назад
Uyu ndiye atithandizadi zoona
@AllanMwakalenga-wn5ib
@AllanMwakalenga-wn5ib Месяц назад
Yalakwa apa...mwachedwa ku vepi a nurse
@user-ux8qz1tg7l
@user-ux8qz1tg7l Месяц назад
Iwe ma nganya 10pn munthu apanganao cani 😂😂
@AllanMwakalenga-wn5ib
@AllanMwakalenga-wn5ib Месяц назад
Tikuferanji 😂😂
@EllinaBitto
@EllinaBitto Месяц назад
Ndendende😂😂😂😂😂😂😂
@Marionphuxymw
@Marionphuxymw Месяц назад
Kkkkkkk kma adaa changa ndichala pakamwa
@GustoAjasi-fl9oo
@GustoAjasi-fl9oo Месяц назад
😂😂😂😂 ausi anachenjela eee
@osmanafadi4801
@osmanafadi4801 Месяц назад
Wamisala anaona ndewuu
@user-co5yu3fs4r
@user-co5yu3fs4r Месяц назад
Powerful musatsiye
@tracybennie7783
@tracybennie7783 Месяц назад
Ine. Ndiye. Ndikalila. Malilo
@TizifaBanda-xn5tm
@TizifaBanda-xn5tm Месяц назад
Ndawala zikuswedwa eeee
@anthonynkhoma4265
@anthonynkhoma4265 Месяц назад
New sheriff in town
@user-tk6qh9zs7h
@user-tk6qh9zs7h Месяц назад
Zofunika zimenezo a VP. Ma Civil Servants ambiri matama komanso kumalimbikira ntchito, kukula Mtima komanso kudzikonda. Akuti ntchito ya m'boma imavuta polowa. Achangamutseni ndithu.
@abdulsalammkwepu3321
@abdulsalammkwepu3321 Месяц назад
I remember achilima anayambaso chonchi kenako nae alowa mu system...... Hope this will no stop
@StevenKamtsokwe-zn4vr
@StevenKamtsokwe-zn4vr Месяц назад
Zoonad chilimaso amkatero
@KunyengaMoyo
@KunyengaMoyo Месяц назад
😂😂😂 Km manganya
@HappinessMilanzi-b2m
@HappinessMilanzi-b2m Месяц назад
Zikuoneka kuti mutithandiza
@user-cm3pl3pb9u
@user-cm3pl3pb9u Месяц назад
Kkkkk ine ndimaona ngati sewelotu😂😂😂😂🎉🎉
@mzeewandembonyirongo2972
@mzeewandembonyirongo2972 Месяц назад
😂
@FrancisNyayi
@FrancisNyayi Месяц назад
Kkk
@mcsellahntv6896
@mcsellahntv6896 Месяц назад
Ngati zenizenitu, nkana unampeleka Bhiyeni umafuna zimenezi.
@EllinaBitto
@EllinaBitto Месяц назад
😭😭😭😭😭😭😭😭😭
@emmanuelkenneth4768
@emmanuelkenneth4768 Месяц назад
😅😅😅😅 well planned
@Uncle_B265
@Uncle_B265 Месяц назад
Ngati azimaliza ndiyen tione
@ruthkaoloka4772
@ruthkaoloka4772 Месяц назад
ndi drama kodi?
@EmmReece
@EmmReece Месяц назад
mcp iwinaso bad
@AlinafeSolomoni
@AlinafeSolomoni Месяц назад
Koma akuoneka ngati afika movuta koma ndimunthu ochezeka
@EvanceSteven-u5g
@EvanceSteven-u5g Месяц назад
Nice
@jonathanmbewe4246
@jonathanmbewe4246 Месяц назад
Mupitenso ku immigration mukawonekeleko bwana
@user-xe5lb4uf3n
@user-xe5lb4uf3n Месяц назад
Bola zipipitirire
@Choicemlw
@Choicemlw Месяц назад
Mu manifesto a Tonse alliance anati ankadzalowa m'boma anthu azipita ku ntchito <a href="#" class="seekto" data-time="510">8:30</a> Aiwala nthawi yomweyi kodi?
@KunyengaMoyo
@KunyengaMoyo Месяц назад
Akuyankhula ngt akupanga tikuferanji
@clintonhodda9830
@clintonhodda9830 Месяц назад
Ukuoatenga anthu ngati zitsiru USI government ukuti kulibe ndalama koma zomwe akumagawa kumusonkhano akuzitenga kuti?
@user-xx4yi4mq5m
@user-xx4yi4mq5m Месяц назад
ipase moto usi bola osazasitha mukazapasidwa mwayi.......try hard this year 2025 boma....
@user-mm3es3ph7h
@user-mm3es3ph7h Месяц назад
Malume mukukwana
@StellaErias
@StellaErias Месяц назад
Pitilizani bwana azimayi oyembekezela timavutika zipatalamu agalu amenewa amazimva ubwana zipatalamu
@user-qs3vs8kz6n
@user-qs3vs8kz6n Месяц назад
Mulunguakupatseni phamvu
@ellensambo6323
@ellensambo6323 Месяц назад
❤❤
@willieBillschiumbuzo
@willieBillschiumbuzo Месяц назад
Ipatseni moto a vice ama <a href="#" class="seekto" data-time="641">10:41</a> wonjeza kubwera mochedwa kutchito ma nurse akafika ayambe kaye aseweretsa 4n then aziyamba cha ma 9 kugwira tchito
@danielkhinguirossejuliasse6106
@danielkhinguirossejuliasse6106 Месяц назад
ndiye wapanga sewero lamphamvu
@EmmReece
@EmmReece Месяц назад
mcp iwinaso
@user-hl3st3cc4v
@user-hl3st3cc4v Месяц назад
Zandale ziduse uko nawo anthu ogwira ntchito chipatala za boma amapanga matama muzapanadi
@mthawisakaunda
@mthawisakaunda Месяц назад
Ma nurse ku malawi osadziwa English Kkkķk km zlko. Usi wayesetsatu
@geltrudenamuthuwa5945
@geltrudenamuthuwa5945 Месяц назад
Aaaa za ziii 🚮
@anthonynkhoma4265
@anthonynkhoma4265 Месяц назад
Ananena kuti asenda aliyense waulesi
@FlorenceBillyGama
@FlorenceBillyGama Месяц назад
Ubwana syndrome inavulaza a malawi ambiri
@AishaUthman-mg7db
@AishaUthman-mg7db Месяц назад
😂😂😂😂
@user-eu3qz2so4n
@user-eu3qz2so4n Месяц назад
Zapamwamba
Далее
Only I get to bully my sister 😤
00:27
Просмотров 21 млн
C’est qui le plus fort 😂
00:18
Просмотров 7 млн
Siyatha News | 6.00 PM | 27 - 08 - 2024
42:24
Просмотров 22 тыс.
THE COURT..(Malawi )🤔
20:45
Просмотров 192 тыс.
Only I get to bully my sister 😤
00:27
Просмотров 21 млн