Тёмный

Wansembe wamkulu wa katolika anayankhula zonyoza boma zayambaso kuzungulira dzina ndi Fr Tamani 

Malawi Trends TV
Подписаться 48 тыс.
Просмотров 20 тыс.
50% 1

Опубликовано:

 

14 окт 2024

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 74   
@ChembeWaimba
@ChembeWaimba 3 месяца назад
Mwalalikazi mwatenga book liti lamulungu, kusochera ndikusocheresa uku, aneneri onyenga
@festonphiri
@festonphiri 3 месяца назад
Good message fr
@DanMhone-iw6xg
@DanMhone-iw6xg 3 месяца назад
Sananyoze koma amalakhula zona zokha zokha komasotu wanenelatu kuti zochezatu sono chomusakila nchani ndye akunama
@erasmopedrombewe8842
@erasmopedrombewe8842 3 месяца назад
Esse padre falou a verdade, não é desprezo
@WinerdShadreck
@WinerdShadreck 3 месяца назад
This is good massage
@MassPastor-bn8ck
@MassPastor-bn8ck 3 месяца назад
Sindikuona chomwe Mkuluyu akuyankhula zonyoza boma koma kuti ambiri mwa ife timakondwa tikamalambalala chilungamo,koma chifukwa choti chilungamo chima pweteka ndichifukwa chake zikuveka ngati kunyoza kama ayi ndithu akukamba zona zake munthuyu. I wish if we can learn to stand for the truth like this Father..........
@adammadi8248
@adammadi8248 3 месяца назад
To speak the truth sikunyoza ,therefore tisiye mukalidwe woyika anzatu pamoto.
@kondwamlungu8384
@kondwamlungu8384 3 месяца назад
Amen
@MphatsoMhoney-xn2ft
@MphatsoMhoney-xn2ft 3 месяца назад
Very good and short speech
@chrismezalumo5698
@chrismezalumo5698 3 месяца назад
Very profound 🔥🔥🔥
@samuelazumah1050
@samuelazumah1050 3 месяца назад
Sananyoze koma chilungamo
@Maliko-bp1xn
@Maliko-bp1xn 3 месяца назад
Moyo wa munthu pali thupi ndi nzimu choncho thupi ngati likumana ndi mavuto akuyenera kulankhulapo kumene ,nkhristu ngati ali ndi njala angamve bwanji mau zikufunika zonse ziyende limodzi
@PeterRabson-z3w
@PeterRabson-z3w 3 месяца назад
Wakamba zoona wansembe amenei chakwera n boma lake sakuzaununkhanso mpando 2025 muzandivoera✋
@PatricMwadzera
@PatricMwadzera 3 месяца назад
Kaya ndizaliti koma he is saying the truth
@isaacpaulrabson2099
@isaacpaulrabson2099 3 месяца назад
Good point farther
@sankhwe
@sankhwe 3 месяца назад
Good one
@scoobymatola8314
@scoobymatola8314 3 месяца назад
Sakunyoza You can't run a government without knowing economics
@HevenChiwaya
@HevenChiwaya 3 месяца назад
This is great massages to the Malawi government if they have knowledge they have to change the direction
@MelvinVanRooyen
@MelvinVanRooyen 3 месяца назад
aaaa kunyoza kwake..kulipati pamenepo akuyakhula chilungamo
@mtimatrading790
@mtimatrading790 3 месяца назад
Ameneyu saopa anayamba kupalamula nthawi ya Bingu, anamupuputitsa mkulu wina wake magilasi a mmaso pa msonkhano.
@0wenNkhambule
@0wenNkhambule 3 месяца назад
Good Messnge Chakwela walephela you mast go
@clintonhodda9830
@clintonhodda9830 3 месяца назад
Kwacha yagwa kumene ndipo akuti Chakwera ndi ophunzira koma akulephera kuyendetsa dziko
@paulmanyamba5437
@paulmanyamba5437 3 месяца назад
Osati kuti wayankhula zonyoza anayankhula chilungamo osamadana ndikuuzidwa chilungamo ayi
@andyjames2050
@andyjames2050 3 месяца назад
Pali kunyoza apa ichi ndi chilungamo cheni cheni
@uzaleuzale8603
@uzaleuzale8603 3 месяца назад
Ndiye kunyozako kuli pat
@wilisonbornface4282
@wilisonbornface4282 3 месяца назад
Zoona kwambiri sikuwonapo cholakwika
@shayrafernandeslatif9556
@shayrafernandeslatif9556 3 месяца назад
Very true
@BeatGondwa
@BeatGondwa 3 месяца назад
Good good
@RobertLuka-wy9cl
@RobertLuka-wy9cl 3 месяца назад
🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏
@FrancoKaunga-rq2ki
@FrancoKaunga-rq2ki 3 месяца назад
Father you are number one! Chakwera is a big failure. Indeed we made big mistake to put chakwera as a president.
@LangfordMabaso-z7u
@LangfordMabaso-z7u 3 месяца назад
True mssg
@comradechimbayo3167
@comradechimbayo3167 3 месяца назад
Powerful
@PempheroMoleni
@PempheroMoleni 3 месяца назад
🤗🤗🤗🤗
@MabvutoMichaelPanagona
@MabvutoMichaelPanagona 3 месяца назад
Kunena zoona munthu wa mulungu sanafotokoze monyoza ayi ngati mukufuna kumutapa mkamwa mungomutapa mkamwa sindikuona chifukwa ayi.
@corretabanda7685
@corretabanda7685 3 месяца назад
Kunyoza boma ndie kuti chaani? Kudana ndichilungamo kapena?
@adammadi8248
@adammadi8248 3 месяца назад
Kodi povhota mumasanga kuti awa ndi abusa asavhote? Yet kufnyika and them there are experiencing the heat.
@FavourKadzembe-sg1yf
@FavourKadzembe-sg1yf 3 месяца назад
another Dc
@PhilemonLloydGalawanda-tz2zb
@PhilemonLloydGalawanda-tz2zb 3 месяца назад
Ulaliki wa kale uwu siwa pa 3 July 2024
@AnaffSayamika-uh6vg
@AnaffSayamika-uh6vg 3 месяца назад
Sananyoz akunena chilungam uyu
@jameschibwana2751
@jameschibwana2751 3 месяца назад
Vuto anthu mumadana ndi chilungamo, wanyoza chiyani pamenepa?
@lazaruschitsamba8394
@lazaruschitsamba8394 3 месяца назад
koma bwanji kunyoza wosatandiza maganizo
@WisdomMaseko-fi5sv
@WisdomMaseko-fi5sv 3 месяца назад
Andale ampingo
@actuarialscience2283
@actuarialscience2283 3 месяца назад
MCPigs ndi ufiti
@GraceMakoka-v2k
@GraceMakoka-v2k 3 месяца назад
Koma akunena chilungamo
@MabvutoMichaelPanagona
@MabvutoMichaelPanagona 3 месяца назад
Uthenga wa bwino zikomo
@RaphaelKweve
@RaphaelKweve 3 месяца назад
Palibe kunyoza apa ,,,,
@AlexNjanje
@AlexNjanje 3 месяца назад
Ineyo sindikupeza vutoo and Chakwera alibenso mzotheka mchifukwa kumakhala cabinet members ntchito yawo kumuuza presedent pomwe sipakuyenda bwino ndipo amamva ndi munthu osamangoti presedent ali ndi vutoo vutoo ndaammbaliwa tere basi
@rhodrickmpumila1820
@rhodrickmpumila1820 3 месяца назад
Ndi cadet wa DPP uyu ndikumudziwa bwino
@ThomsonNyirenda-df9io
@ThomsonNyirenda-df9io 3 месяца назад
Nothing wrong good
@viennasamuel2976
@viennasamuel2976 3 месяца назад
Pali kunyoza apa? Chilungamo ich
@GreshamKadzembe-tn8cq
@GreshamKadzembe-tn8cq 3 месяца назад
Kodi inu mesa ndi amene munalemba chikalata 1993 kuti mukufuna madipaty, ndiye mukuletsa chani zimenedzo ndiye ndarezo kuba basi onse akhara a kulowa aja ndi okuba ngakhare iweyo ukulankhula we kuti ukhare pampando utha kuba so
@TrizaGeorge-q8w
@TrizaGeorge-q8w 3 месяца назад
Nanuso musamakokomeze kuti zonyoza boma cholinga amangedwe akunena zoona aliyese pamene zafikapa olo mwana akudziwa kuti dzikoli sili bwino athu akufa ndi njala mwezi uno Kodi nangytifikile January athu akhala motani dzikoli lafika powawa tayendani m,mizimu athu afika pongomupepha mulungu kuti angowatenga chokhalilaso ndi moyo sakuchiona chifukwa Cha mavuto
@owenmoses9434
@owenmoses9434 3 месяца назад
Zonyoza??? In what way??? Nananuso mwayambae???
@AllanChabwela
@AllanChabwela 3 месяца назад
Chilungamo kkkkk
@AllanaChiphazi
@AllanaChiphazi 3 месяца назад
Ulaliki musamaphatikize ndizadziko pls
@simeonbanda4240
@simeonbanda4240 3 месяца назад
Rad the Book of Prophet Isaiah! He denounced the oppression of the poor and the injustices of the government. So its the responsibility of the pastors to denounce the envils of the government. Moreover the church has contributed significantly to the development of the country so it has a say where things go wrong
@MathewKalinkhu
@MathewKalinkhu 3 месяца назад
Kuswa kuswa, Chakwera ndi boma lake la MCP kumene aliko mutu waima, zoona zokha zokha, ndipo latikwana boma limeneli.
@DixonChimanya
@DixonChimanya 3 месяца назад
Uthenga wabwino chifukwa anthu mukuwalikiralawo ali pamavuto mu dziko lawo
@GanieAlidih-gu7no
@GanieAlidih-gu7no 3 месяца назад
Palibe kunyoza apa km kunenachilungamo
@abdukarimmponda5698
@abdukarimmponda5698 3 месяца назад
Zimakutuzo amalawi kumataegula..anakuuzan ndani kut kutimikira mulungu nde kut azionelera zopusa zikuchitika aba ndalama za anthu zamisonkho kubako siusatana? Nde ena akalankhula alakwitsa...munthu wachinyamata mmutu mukadali ndale za 1990 zachisoniiio,👺🤔
@Jfphiri-w7b
@Jfphiri-w7b 3 месяца назад
Rev....mwasokonela a Revrend yambani ndale...mwakanika inu kuthana ndi Santana Zaka zonsez....musatchukile pa ndale ..simudziwanso kulalika inu
@EvanceLiphava
@EvanceLiphava 3 месяца назад
Osamangosusa zilizonse akulu ngati inu mukumwa tea daily si onse amene akumwa tea ngati inu. Choncho ndi udindo wake ngati m'busa kulangiza nkhosa zake zammene dziko likuyendera. Palibepo za ndale apa nchirungamo chokhachokha
@Jfphiri-w7b
@Jfphiri-w7b 3 месяца назад
Its global...go to Zambia Kenya Haiti Amerika.....homeless...no tea r there....everyone must use his head to make things move urside
@MussaNgoma-r2k
@MussaNgoma-r2k 3 месяца назад
Stop politics, mwayiwara ntchito yanu
@EvanceLiphava
@EvanceLiphava 3 месяца назад
Where is the politics in this speech?? Learn to accept when things went wrong.
@YamieManda
@YamieManda 3 месяца назад
Kodi athu awa simadziwa,muve ndi toque yomweyo angakambe zabwino za mtundu wina?amafunana wokhawokha mtundu umeneu_
@RuthChilobwe
@RuthChilobwe 3 месяца назад
Kkkk koma politics yo sikuba. Sattargate @Cashgate @Achairs vashgate ..
@AllanaChiphazi
@AllanaChiphazi 3 месяца назад
Tidzangomvotera iyeyo, amalekeranji kukawadzudzula pamaso pa abomawo, lilipo boma lomwe linayamikiridwa ndi anthu amenewa? Popeza bolili lonse amalipezera zifukwa, zilalikani zoti anthu asiye kupanga ntchimo tiziopa tsiku lachimaliziro. Zamavote munayambitsa ndinu nomwe
@AllanaChiphazi
@AllanaChiphazi 3 месяца назад
Ulaliki musamaphatikize ndizadziko pls
@FrancisDay-br7xb
@FrancisDay-br7xb 3 месяца назад
Iwe kumeneko sikusaniza ndale ndi mpingo koma kuzuzula zoipa za boma
@EvanceLiphava
@EvanceLiphava 3 месяца назад
Lalikani wanu tiumvere
@GiftSnoxy
@GiftSnoxy 3 месяца назад
Nyani iwe wamva ukudziwa chan
Далее
КТО БОИТСЯ КЛОУНОВ?? #shorts
00:20
Просмотров 561 тыс.
ActionSA is briefing the media in Parliament
2:23:45
Просмотров 8 тыс.