Тёмный

Zomwe Apanga A UTM Kuchoka Ku Tonse Alliance Zandisangalatsa - Manza Wa Kwa Chinsapo 

Nyasa VoiceBox
Подписаться 25 тыс.
Просмотров 6 тыс.
50% 1

On Nyasa VoiceBox, a Malawian named Manze from Chisanpo in Lilongwe shares his thoughts on UTM's decision to exit from the Tonse Alliance.
Pa Nyasa Voicebox, M'Malawi wina dzina lake Manze wa ku Chisanpo ku Lilongwe akufotokoza maganizo ake pa ganizo la UTM lotuluka mu Tonse Alliance.

Опубликовано:

 

11 июл 2024

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 20   
@user-hm9nc7lz6e
@user-hm9nc7lz6e 26 дней назад
Kumuikapo manganya chifukwa manganya ndiyemwe anapeteka chilima mmanja mwa cakwera kuti amuphe ndimkona anamuika pampando at avice president akunama manganya wangoona kutenga sambi chabe
@Hamzamabvuto
@Hamzamabvuto 26 дней назад
I'm the first person to comment here I love UTM but I'm not the member of UTM
@MerryWayson
@MerryWayson 26 дней назад
Achita bwino kuthesa ❤❤
@JairoseManuel-p5p
@JairoseManuel-p5p 26 дней назад
Sanalakwise kuchoka
@SHEREEFKanthochi-ft3dm
@SHEREEFKanthochi-ft3dm 26 дней назад
inenso ndikunva kukoma zedi
@DannielOnions-fy3dc
@DannielOnions-fy3dc 25 дней назад
Nice one thanks U.T.M MORE
@susantembo2076
@susantembo2076 25 дней назад
UTM please forge ahead. Don’t listen to any other distractive noises
@doreenkaliati3166
@doreenkaliati3166 26 дней назад
Mumakwana inuyo more fire 🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
@raffickaffick
@raffickaffick 26 дней назад
Bravo fada
@AugustineTheu-of6nv
@AugustineTheu-of6nv 25 дней назад
Zikomo kwambiri nkulu wanga kwa mawu ako ogwira mtima. Inenso m'bale ndikanakhala mwana wa chilima mbuzi imene ija Chakwera ndikanamuthamangitsa pa maliro kuti asowepo. Amene uja si president ayi
@VeronicaChirwa-ct4os
@VeronicaChirwa-ct4os 25 дней назад
Manze ndagwirizana nawe kwambiri pa zomwe wanenazi. Inenso Chilima akanakhala m'mbale wanga sindikanalora kuti abwere pa maliro a Chilima. Ndipo ndikanachita zoti amalawi sanaziwonepo. Kaya ndikufa nanenso ndikanafera pompo. Chakwera ndi munthu oyipa kwambiri.
@stevenfrancism3638
@stevenfrancism3638 25 дней назад
❤❤❤❤❤❤
@doreenkaliati3166
@doreenkaliati3166 25 дней назад
Ineyo ndinakakhala m'bale wanga ndinakati Maliro sikuika tiyeni tikamutulire chakwera akadye sured pakanavuta komanso sinakalora wina aliyense wachipani cha MCP kupedzeke pa Maliro ndithu kunakachema
@Felista-m4q
@Felista-m4q 25 дней назад
Inenso ndanyadira kwambiri
@ErnestChansa
@ErnestChansa 25 дней назад
Mwalakhula fundo zabwino big chakwela ndi galu yambuzi fiti
@MacleanKwacha
@MacleanKwacha 25 дней назад
Ndipo ine ndizafunisisa anthu amenewa asazaikidwe,tizadyere nsima
@user-ui4ux5kc8d
@user-ui4ux5kc8d 25 дней назад
Ngakhale kufa kwake kwachakwera anthu tidzavina kusangalala ndipo kaya imfa imeneyi kwaiyeyu ikuchedwa patii munthu oipa uyuu akanafa koma ndithu ambuye timenyereni mkhondo afee ndithu presedent ameneyi
@user-hm9nc7lz6e
@user-hm9nc7lz6e 26 дней назад
Kuga mwacakwera anthu tidzakondwa komanso kuvina kuti chokupha chija chafa
@gracemkandawire8769
@gracemkandawire8769 25 дней назад
Tiyeni tizavotele UTM. Kuti mzimu wachilima uzause mu mtendele
@user-qp8kh2hj9o
@user-qp8kh2hj9o 25 дней назад
Ndipo izi ndizoona satana achite manyazi
Далее
Ku MCP Kulibe Utsogoleri - Samuel Lwara
13:29
Вы чего бл….🤣🤣🙏🏽🙏🏽🙏🏽
00:18
ТРУБОЧКА СКВОЗЬ НОС 😳
00:40
Просмотров 178 тыс.
best way out of the labyrinth🌀🗝️🔝
00:17
Просмотров 2,4 млн
A Malawi Muganiza Bwanji? - Mr Matemba
16:52
Просмотров 2 тыс.
Boma Latha - Samuel Lwara
5:09
Просмотров 8 тыс.
DPP Moto Moto Eya, Malawi Moto Moto Eya
13:31
Просмотров 592 тыс.
Вы чего бл….🤣🤣🙏🏽🙏🏽🙏🏽
00:18