Zinthu zimakhala zobvuta ngati ma umboni palibe komano commission of inquiry singavute cz a presdent alinawo anthu omwe amapasa information komanso a Richard Banda akuwadziwa omwe anawauza zoti ndege ndi yozaza ndiye ma expart azivutika bwanji cz nkhani iyi nja straight forward, izitu zikuonesa kuti imfayi wasnt nutural death at all