Nkhani ikhale UTM , AFORD ndi UDF apange alliance, president achoke ku UTM ndekuti azapeza ma vote Ku north , central pang'ono koma ochuluka ku southern nde kuti azaiphula bho bho
UTM ISAPHATIKIZANE NDI DPP CHIFUKWA MKAZI WA LOTI ANAYANG'ANA MBUYO POTHAWA MOTO KU SODOMU..PAMENE NGELO WA AMBUYE ANAWAUZA KUTI ALIYENSE ASAYANG'ANE MBUYO. KOMA MKAZI WAKE WA LOTI ANAYANG'ANA MBUYO POGANIZIRA MOWA WAKE WOMWE ANKAPHIKA KUSOMUKO NKUMAGULITSA. IYEO ANASANDUKA CHULU CHA MCHERE. SO UTM NSO MUKAPHATIKANA NDI DPP MUSANDUKA CHULU CHA MCHERE.MUKHALA STUCK AND DORMANT DEAD WOOD .!!!
And madam Patrucia Kaluati being the leader of utm presidential.candidate.cos she is has got experience of leadership.by profession she is a teacher and again she has experience of political leadership.she was in dpp .wurh Bingu wamutharika and peter mutharika
A UTM panokhs simungalamule dziko ndpo position yanu izingokhala 3 or 4... Koma chifukwa chot ndinu okulamtima mumadzimva ngat muli nkuthekera... Kachipani ka ma MP 4 koma matama thooo🤣🤣🤣
A Kalindo zindikirani ichi dziko la Malawi ndi latonse, is not about resignation of its members in government positions. Stop misleading people, eg Usi won't resign cos he is serving Malawians not MCP.