Congradulation brian muluzi ndi amene adali mtsogoleri wa straight basi.muluzi ankanenelatu kuti iwe ichi ayi.iremember mike chilewe akalimbana ndi mr mtafu u mp ku mulanje koma muluzi adayisova yekha polankhula ndi mr chilewe kuti apatse mpata mrs mtafu.koma chakwela ndi muthalika nooo are the same too much sleeping.
Let them continue doing wat they are doing that’s wat is leading Malawians loosing hope in them mcp ndiyakhaza ndipo ipitilizebe kusanvanako zithandizira kuti achoke agalu amenewa.
Koma ngat akumenyana iwo okhaokha chonchi, ndie Chilima akanakhala ndi mtendere kumeneko. Komatu Bon uja ananena bwinobwino za kuipa kwa anthu amenewa a ndale za usikuwa.
Nthumwi zonse ku MCP conversation 2024,chonde onetsetsani kuti anthu amene apangitsa mpungwepungwe uwu asapatsidwe mpando. It could be that God just wanted to expose their wicked side or how incompetent they are as leaders.
MCP must go they think themselves not Malawians look they're busy fighting each other for the sits which it really shows us kuti m'bomamo ndi dimba lawo
In mcp there is no presdent coz off zitsitsi zawo chakwera he can nt do anything pomudzudzula zikhale kunkuyu chimwendo onse ndi ma presdent and the have power than chakwera.
The bleeding party woyeeeee wakupha MCP,muona aphana the Evil people of MCP Party woyeeeee, Chakwera wakupha Chilima yooo Mr Chikangawa aaa yomweyo Galu iweee
Mu nthawi ya boma la DPP a president a president ankalekelera ma boys and girls kumapanga ziganizo zolakwika za boma mapeto ake anapezeka nazo kunja kwa boma... Likewise, mu boma ili sizikusiyana ndi boma lijalo cos kuli anthu ena ovuta zedi musakaike mupezeka nazo kunja kwa boma next year for sure...
Nyama zikulu zikulu zimenezo nda zake atatu akuononga zonse I nkhalidwe lawo liwatsata mawa akuba kuwawa amenewo mawa alifatu amadziva anthu 7 menemu a iona kwa anthu amene anawauza ayouth