A Malawi akuyenera kumpatsa Chakwera masiku osapitilira 10 kuti akhale atapereka lipoti ndipo akapanda kutero, mdziko muno mukuyenera kuchitika ma DEMO okakamiza Chakwera kuturutsa lipoti. Limpopo Fm yalengezanso kuti kuomberedwa kwa nsilikali ku Zomba barracks kuja idali plot yochokera kwa anyamsta a ku STATE HOUSE. DZIKOLI NDILANTHU A MALAWI. Tikulamulidwa ndi chipani cha magazi mudziko muno. Tipempgere kwambiri Ambuye atiturutse mu dziko lino la Farao.
Chakwera watchera kumwezi nkhanga zaona.iye amaona ngati ndiwochenjera koma apapa ndiye wapezeka.akufuna kumpasa deadline 10 days kuti amalawi awapasire report la ngozi ya ndege gulukunyinda ameneyo Dr chikangawa
Kukhala cheteko ndi chitsimikizo choti akudziwa po kanthu president wa dziko ndamene akanakhala oyambirira kutiero koma akuti asankha kukhala chete, nde anthu tingakhulupirile bwanji?
Give him time to meditate on that iissue.It's a very crucial bone of contention.However,he is here in the North accost him democratically to divulge what transpired.It is more than a grief to lose nine Malawians without knowing the apparent cause of the demise.
A Lazarus Chakwerawa akuzolowera pajatu za Sattar Gate iwowatu anali mugulu lomweelo lakubalo ndalama za a Malawi ; inatero utube channel .kuti iwo ndi nduna zao zonse ku parliament .anadya nao. Ndi Sattar yu Anapeza umbavau linali boma mdziko la Britain .koma iwowa anangomupana Saulos chilima yekha kuti chilima anali mbava .koma iwo ndi anzawo onse anadzibisa. Pano ndi apa akubisanso report ya ngozi ya ndege .report from German investigators ..😮😮😮 iwowa aulule nkhani zonse za Sattar Gate kuti anali involved ndi a ndani. Ndipo chilima amuoheranji pangozi ya ndege
Kukhala maiko ena president wa malawi' anthu akadakhala,ataiwala,zoti tidali ndi president ochedwa chakwela.koma, malawi' kaya tinaputsa, bwanji.taonani, anyamata ndi atsikana'aku Kenya Uganda Nigeria, koma kuno tingolidza konono koma kuziwa FB basi.kumangolongolola, kumeneko.