Samalani abale nonse mu dzina la yesu awa tikuti ma profit ndi asing'anga akutiphera abale athu ngati ndondocha kenaka ndikuwanweza ali olumala ife tiziti profit koma uyi. Tili masiku otsiliza osaiwala zimezo abale chonde abale samalani nawo amenewa
M'bale wako oti wamwalira angabwere akuoneka ngati munthu wina mkumati ndameneyo zoona?guys come on come on,these so called prophets asokoneza anthu Kwambiri,
Don't stress your self please,munthu àmene mukunenayo ndi scammer amango panga pretend ngati wa asma nditambwali ameneyo he used Kuma panga zakeko ku Lilongwe around kanengo komanso area 43 titamuzindikira maplan ake adathawa
Anali yemweyo kapena ayi? Nkhope imasiyana bwanji? Mprothet ameneyo anamutumiza Mulungu kapena ndani? You and your prothets are fools and you don't know God.