Koma chilima timuliladi mpakamkapa chifukwa ndiyekhayo anakakhala active analidi msikilikali wa anthu osauka a DPP,UDF,AFORD alibe nazo ntchito iwowo bola zawo zilibwino sagona ndinjala koma akupha ife amalawi osawukafe eeeeeh koma achilima munatisiliyanji ifeee😢😢😢😢😢
Amene amaimila ku Mwasa ward pa ticket ya DPP ndimunthu osowa khalidwe anthu sanamuvotele chifukwa chachimenecho,iye uja ndiwaguru la Bam Bam lija limasokoneza pam baluku limamenya anthu lija pomwe uyu anaimila mcp ndimunthu wabwino kwambiri,fact yankhani imenei ndi imeneyo basi,tikamakamba za Bam Bam ndi guru la anthu lomwe linapangidwa kuchokera ku dzina la film ina yake ya anthu osokoneza aku Mexico ena amati B13,anthu amenewa ngati mukukumbukira mmbuyo muja ndi aja anamenya ndikubvula a UTM aja ameneo
Amalawi apapa a opposition,'wa asatipusise coz dzikoli ndilathu, tiyeni tipange mademo ochosa akhwakhwananda amenewa m'boma mosogozedwa ndi Bon Kalindo, President wathu wa amphawi basii, opposition leaders are scared to be jailed and killed
Mau oti “zinthu sizikuenda” is not a political strategy pitani mukawafunse anzanu ku Zimbabwe 🇿🇼…..ndaletu ndikufikira anthu Pa ground osati Pa social media 🤣🤣mulira simunati
Kuyankhula motumbwa chonchi ndikomwe kudachotsetsa DPP mu boma. President wakoyo is even very far from the ground pomwe ukupanenapo. Mutha kuyankhula motumbwa chonchi chifukwa nzachidziwikile kuti chaka cha mawa mukuzalowa mboma mwachinyengo. Koma choti udziwe nchokuti muzachoka mboma muli ndi nkhope zamanyazi kwambili
@@Lee-lee-w1rAnkolo mwanvako olo mfundo imodzi from opposition other than kungoti ‘sizikuenda’? Akakhala ma activist ndekumangotukwa daily. Boma ndilomweli basi mufune musafune 🤣