Тёмный
No video :(

BON KALINDO 24 JULY 2024 KUSWANYA BASI PA WEDNESDAY 

Malawi Trends TV
Подписаться 41 тыс.
Просмотров 20 тыс.
50% 1

Опубликовано:

 

6 сен 2024

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 76   
@KelvinLaudon
@KelvinLaudon Месяц назад
Kuyankhula ndiye mukuyankhula koma anthuwa kusamva big up kalindo your the genuine the DC
@user-st6bt5vv9c
@user-st6bt5vv9c Месяц назад
Ngati inuyo a DPP, UDF AND AFORD simugwizana mutaphe matiparty ndinu mutizunzisa koopsya pamene bolani inuyo muli ni ndalama muzatha kuthawa koma ifeee tizangosowa Ngati mmene zinkachikira mu mcp yapitayo😭😭😭😭😭😭 tikulira kodi kumwera kuno singathe kukhala nigwizano wa zipani kupanga chimozi please akaliyati apm,Atupele choonde choonde pangani chimozi zukani tikutha tonse muno please
@user-rl5zq1qr4d
@user-rl5zq1qr4d Месяц назад
Chisankho nthawi zambiri zimatengera amene waimirayo kuti ndi ochuka bwanji kuderalo chisanzo BT wawina wa independent kusonyeza kuti iyeyo ndi amene anali popular mangochi wawina uja ngakhale akanaima pa yekha still akanawina sanabvotere mcp amubvotera munthuyo chimodzi modzi chisankho Cha 2020 anthu anavotera mcp chifukwa Cha chilima namukonda amb
@AffectionateGeyser-fm7dl
@AffectionateGeyser-fm7dl Месяц назад
Zoona ma candidate ena imakhala character siyabwino ndiye anthu savotera the problem is not the party but candidate
@KunyengaMoyo
@KunyengaMoyo Месяц назад
Simukunama opposition ikugona, kmanso Madera omwe avotera MCP mitu yawo sigwira kuno ku Thyolo MCP taikana
@user-zh4di3ly1x
@user-zh4di3ly1x Месяц назад
Otsusaw akubowa ndipo akupsesa mtim ochenjeza schenjeze bwanji KT amve anthu away eshiiiii
@user-qp5zp2wk4y
@user-qp5zp2wk4y Месяц назад
Next year MCP might win opposition hasn't been active chiloweleni, so voting ndikumudzi ambiri amayenera kupangidwa convince
@ChimwemweKondowe-nj4lx
@ChimwemweKondowe-nj4lx Месяц назад
Vuto option yikugona kwambiri. Munthu oti akudziwa zoti atha akumenyedwa ndeu, amakonzekera kwambiri, lero ndi izo
@JeniferNyankhomaMndalasini
@JeniferNyankhomaMndalasini Месяц назад
11:07
@EllenPhiri-xt8pt
@EllenPhiri-xt8pt Месяц назад
Koma chilima timuliladi mpakamkapa chifukwa ndiyekhayo anakakhala active analidi msikilikali wa anthu osauka a DPP,UDF,AFORD alibe nazo ntchito iwowo bola zawo zilibwino sagona ndinjala koma akupha ife amalawi osawukafe eeeeeh koma achilima munatisiliyanji ifeee😢😢😢😢😢
@HalisonSolomon
@HalisonSolomon Месяц назад
KALINDO NDIYE AKUYANKHULA KOMA KUSAMVA KWA ANTHU OSUSA AGONA AKUFUNA KUWINA ZASANKHO KOMA ALI NDWIIIIII.NGATI AKUMETESA , AKUFUNA KUMENYEREDWA NKHONDO CHONSECHO ANGOKHALA
@TanishaLiffa
@TanishaLiffa Месяц назад
The DC 💪
@BrightNkhoma-xz4bg
@BrightNkhoma-xz4bg Месяц назад
Bon Kalindo 🇲🇼🙏
@user-gs9vr1lc9d
@user-gs9vr1lc9d Месяц назад
Akugonadi too much chifukwa amafuna mipando ya u Prezident,
@DavidJackson-ox4xm
@DavidJackson-ox4xm Месяц назад
The DC'S mwana woooopsa kwambiri akhalise Malawi
@user-xm3zl5cg6x
@user-xm3zl5cg6x Месяц назад
apepetula zisilu izi zitayen bon
@user-rm2xv8ys1i
@user-rm2xv8ys1i Месяц назад
Bon kalindo anayamba kale kuyakula koma position yili ziiii yikutibowaso bwanji😊
@user-co6sc8om5n
@user-co6sc8om5n Месяц назад
Opposition yonse ndiyausilu mwina akuziwana mpatumbo pa opposition
@AndrewChiponga
@AndrewChiponga Месяц назад
Ase karindo ndi doro maguys chisakho chizavuta chaka chamawa apapa zaonesa kuberedwa
@GeorgePhiri-ub2of
@GeorgePhiri-ub2of Месяц назад
Or zipani zonse zitasokhana sizingawinen inuyo mcp mmangodananayo chabe ndiye ubwino wake mulungu samakhala kwanu mbuzi inu simunati mulila shupit
@FrankMwachande
@FrankMwachande Месяц назад
😂kkk kukhunuka inuyo a opposition seriously .
@harrisbanda5891
@harrisbanda5891 Месяц назад
Opposition leaders osamva malangizo awanthu yamtundu wanji?, eish!, bon Kalindo, mtanyiwa alongside bakili muluzi tv akutivumbulusila zinsinsi zomwe asatanic'wa akuchita pobela zisankho , koma inuyo a opposition mwangoti machende phwii osatengapo action iliyonse y?, i think muli gulu limodzi ndila chikangawa inuu and musamawapusise amalawi agalu 🐕🐕🐕 osusa inu, chikangawa yomweyo galu iwee 🐕🐕🐕
@FrankMwachande
@FrankMwachande Месяц назад
True story the DC😢
@GeraldChisokeza-er5cf
@GeraldChisokeza-er5cf Месяц назад
Auzen adziwe
@EusébioLucianoGaiondo
@EusébioLucianoGaiondo Месяц назад
Bon kalindo 🔥🇲🇿
@user-kr1tf2tu7s
@user-kr1tf2tu7s Месяц назад
Wasowa chonena mkulu iwe ,,athu amawona wokha zothandiza osati zopanda tsogolo zanuzo.mcp mpakanampakana bacedwani mkutukwana kwanuko
@user-bw7bd5jt9h
@user-bw7bd5jt9h Месяц назад
Zoona a opposition akugona
@harrisbanda5891
@harrisbanda5891 Месяц назад
😂😂😂😂😂😂 boma ilooo , mcp oyeeeeeee 😂😂😂😂😂, mumkatitu mukufuna boma la anyamata oganiza Booo kkkkkkkkkkk chakwela mukati ndi m'busa owopa MULUNGU 😂😂😂, lero ndebwa?, muchiwonatu inuu simunati , ife tinaziona kale nkhanza zawo zinatikwana kale mdzaka zimenezooo, mchifukwa chake timasamza evrytime tikangomva za dzina la chikangawa mcp crocodile dancer party 😂😂😂😂😂, ine lero ndiye ndingoti chakwela yemweyoo , kuti waa waa waa 😂😂😂
@MsondaBanda
@MsondaBanda Месяц назад
The Minister Boni Kanindo, you see yourself how these options their mind is just to tuka each other , so it's not solution, Bon you are a big Minister
@Pangolinimw
@Pangolinimw Месяц назад
Mangochi athu ake alibe selu
@enocklimani1750
@enocklimani1750 Месяц назад
The Dc
@user-bf1sz6pu1n
@user-bf1sz6pu1n Месяц назад
Koma akudziwa ndalama zomwe chakwela ndi mcp yakeyo awononga chifukwa cha mpando waung'ono ngati umenewu ? Mcp ikufuna anthu aziyesa ngati akukondedwa. Chipani chanzeru sichingaononge ndalama zambilimbili chifukwa cha zinthu zofoila.
@blessingsnyalo-rp9ko
@blessingsnyalo-rp9ko Месяц назад
A opposition ndizisilu zawanthu😅😅
@GeorgePhiri-ub2of
@GeorgePhiri-ub2of Месяц назад
Ndipo inuyo okonda zotukwananu mukhaula mulimbana ndi ma bgy
@GeorgePhiri-ub2of
@GeorgePhiri-ub2of Месяц назад
Akulu akulu timanena nthawi zonse sosho midia singasinthe kanthu ndale ndi pagiraundi inu mmakhala bze kupeka maboza pano azanu alibze pa galaund mungawine? taonani kularonga anakumenyani 3 zilo koma simabva mukhaula ndipo simunati mcp simungaichose boma
@samanthamuller7643
@samanthamuller7643 Месяц назад
awa olo apange zonela anthu akumudzi ananaminza zachimanga koma akumangochi anthu opunsa kwabasi musapangeso zimenezo ku mp ndikuwuzeni ine ndiwina ndipo mangochi zizayivutisa tikawina inu mukavotera mcp yanuyo muziwa Malawi musayelekeze mistake ina mulilanayo anthu awa mene tikuvutikira pano inu zowona kwavutera kodi mvuto lanu ndichani inu achiyao mumazichemelera kuti inu ndaya odzindikira apa mwatani ìnu inu munali ndi mvuto lanji inu ❤Dpp UDF ilikoko zowona inu
@user-lc3nh2ju7w
@user-lc3nh2ju7w Месяц назад
Mmera poyamba
@DalitsoMatope
@DalitsoMatope Месяц назад
Adad mukugonatu
@ishmaelsiffah9900
@ishmaelsiffah9900 Месяц назад
Amene amaimila ku Mwasa ward pa ticket ya DPP ndimunthu osowa khalidwe anthu sanamuvotele chifukwa chachimenecho,iye uja ndiwaguru la Bam Bam lija limasokoneza pam baluku limamenya anthu lija pomwe uyu anaimila mcp ndimunthu wabwino kwambiri,fact yankhani imenei ndi imeneyo basi,tikamakamba za Bam Bam ndi guru la anthu lomwe linapangidwa kuchokera ku dzina la film ina yake ya anthu osokoneza aku Mexico ena amati B13,anthu amenewa ngati mukukumbukira mmbuyo muja ndi aja anamenya ndikubvula a UTM aja ameneo
@sinethembangubo3718
@sinethembangubo3718 Месяц назад
The DC bon kalindo avery dangerous child
@JohnAsendi
@JohnAsendi Месяц назад
Tivomeleze kuti ngati osapanga n'gwilizano ndithu sitingaboole PA Chakwera ochenjera PA sosho midiya shiti
@dondamissonchdziwe3958
@dondamissonchdziwe3958 Месяц назад
Eya zivoterani MCP ikumalizani kuku phani Nonse Wanthu opanda mzeru
@harrisbanda5891
@harrisbanda5891 Месяц назад
Amalawi apapa a opposition,'wa asatipusise coz dzikoli ndilathu, tiyeni tipange mademo ochosa akhwakhwananda amenewa m'boma mosogozedwa ndi Bon Kalindo, President wathu wa amphawi basii, opposition leaders are scared to be jailed and killed
@dalitson3558
@dalitson3558 Месяц назад
A opposition machende awo zoti amalawi akuvutika sakusamala what kinds of opposition parties are these , atikwana kwambiri
@harrisbanda5891
@harrisbanda5891 Месяц назад
Bon Kalindo please, pangani mademo oti tichotse guleyu pampando wa u President, munamulemba ntchito ndinu ndipo wayesedwa mayeso and wapezeka kuti walephela , mabwana akefe tikuti achoke basi , awoposition anamachende 😂😂😂
@JonaZimpita
@JonaZimpita Месяц назад
Chistilu uyu More Fare MCP wina afune asafune 2030 walila chokweza B,K
@harrisbanda5891
@harrisbanda5891 Месяц назад
Opposition leaders osapita kukhoti kukatenga chiletso choti achikangawa akuphwanya malamulo oyendetsela zisankho, nrb sikupanga bwino ndi mabungwe ena ambiri, instead mwangopindilila michila yanuyo mma trouser mwanu , mukufuna kuti amalawi atani komanso mukufuna kuti amalawi awomboledwe kumoto wachikangawu ndindaniiii?
@user-eh1mg3ww6d
@user-eh1mg3ww6d Месяц назад
Koma tipephele mulungu asithe nyengo ya ziko lathu posawelengela kuti zikoli ndi la Chakwela koma mulungu azilemekeze yekha kusitha ziko lathu
@KennedyKanyama-ce8lb
@KennedyKanyama-ce8lb Месяц назад
Zaoneselatu kuti DPP yatha. Udf yatha. UTM yatha. Afford yatha. Nanga ichi ndichani? Zoona awawa mmene akudzudzira zikoli alipo angawavotere?
@user-si7po9sd5i
@user-si7po9sd5i Месяц назад
Anthu aku opposition ndi opusa kwambiri
@user-ky4ce9gb6j
@user-ky4ce9gb6j Месяц назад
Ndipo kwambiri
@NelsonNdeke
@NelsonNdeke Месяц назад
Opposition is sleeping indeed ali ziiiii!
@harrisbanda5891
@harrisbanda5891 Месяц назад
Please bon Kalindo, mademo omwe mupangise akhale ochosela chakwela satana ameneyu pampando, atmalizatu amalawife satana ameneyu 👺👹👿☻
@ziyamporoma377
@ziyamporoma377 Месяц назад
Mau oti “zinthu sizikuenda” is not a political strategy pitani mukawafunse anzanu ku Zimbabwe 🇿🇼…..ndaletu ndikufikira anthu Pa ground osati Pa social media 🤣🤣mulira simunati
@Lee-lee-w1r
@Lee-lee-w1r Месяц назад
Kuyankhula motumbwa chonchi ndikomwe kudachotsetsa DPP mu boma. President wakoyo is even very far from the ground pomwe ukupanenapo. Mutha kuyankhula motumbwa chonchi chifukwa nzachidziwikile kuti chaka cha mawa mukuzalowa mboma mwachinyengo. Koma choti udziwe nchokuti muzachoka mboma muli ndi nkhope zamanyazi kwambili
@ziyamporoma377
@ziyamporoma377 Месяц назад
@@Lee-lee-w1rAnkolo mwanvako olo mfundo imodzi from opposition other than kungoti ‘sizikuenda’? Akakhala ma activist ndekumangotukwa daily. Boma ndilomweli basi mufune musafune 🤣
@Chiso2019
@Chiso2019 Месяц назад
Ndipo zoona zikunenedwa apa.....ndi mcp woyeeeeeeee .....kugona too much ku opposition
@MathiasJoseph-xv1hj
@MathiasJoseph-xv1hj Месяц назад
Uwundiuthenga waukulu ku opposition sure
@mayesojameskatete
@mayesojameskatete Месяц назад
The D.C. ❤❤❤
@HappyAbyssinianCat-xt2bm
@HappyAbyssinianCat-xt2bm Месяц назад
Ndpo ndi zoona atsogoleri athu akugona kwambiri kupanga masewera mcp ikhoza kutenga boma, ndpo akatenga boma tizavutika kwambiri, kulankhura ndye anthu mukulankhura km atsogoleri sakumva
@user-st6bt5vv9c
@user-st6bt5vv9c Месяц назад
Zoona mangochi ndichiani chachika anthunu bwanji nzeru mulibe mukunyengedwa ni deya kodi kumpoto anachita kubera koma inuyo a DPP, UDF, AFORD anthu opanda chikondi chisoni ni wanthu mwandiliza kwambiri mukukonda ndalama osakonda anthu mwatikhumudwitsa kwambiri
@DONNEXKhama-bk1gy
@DONNEXKhama-bk1gy Месяц назад
Zikupwetekesan Mutu izi zitayen
@chrisgremu740
@chrisgremu740 Месяц назад
Vuto anthunu MCP simuidziwaa
@user-ky4ce9gb6j
@user-ky4ce9gb6j Месяц назад
Zomvesa chisoni tu kwambiri esh
@user-sh1rj3ol3t
@user-sh1rj3ol3t Месяц назад
Zosusa zomwezo 😂😂😂
@PhilipMatolino
@PhilipMatolino Месяц назад
The DC zoona ? Apo ndie akubeladi ansaaaa!
@PatrickMkonongo
@PatrickMkonongo Месяц назад
🎉
@MatthewLameck
@MatthewLameck Месяц назад
MCP boma ilo 2030 wooooo💃💃💃
@harrisbanda5891
@harrisbanda5891 Месяц назад
Government less chikangawa Idiot 😡, tikuchotsani b4 2025 asatana akupha inuu👺👹👿☻
@user-ky4ce9gb6j
@user-ky4ce9gb6j Месяц назад
Palibe zimenezo mukunama
@Lee-lee-w1r
@Lee-lee-w1r Месяц назад
Ndipotu zoti muzawina sizachilendo chifukwa tikudziwa muzapanga chinyengo komatu muzaphana agalu inu
@YasinMusa-ym8lp
@YasinMusa-ym8lp Месяц назад
Abela mcp koma
@FrancisMakuluni
@FrancisMakuluni Месяц назад
Ndipo live
@chrisgremu740
@chrisgremu740 Месяц назад
Munyeraaaa
@tingamasi106
@tingamasi106 Месяц назад
Tikanyera iwe utiseta
Далее
EXCLUSIVE INTERVIEW WITH BON KALINDO
59:52
Просмотров 86 тыс.