Тёмный

CRUISE 5 WITH GEORGE THINDWA 

Joab Frank Chakhaza
Подписаться 61 тыс.
Просмотров 24 тыс.
50% 1

George Thindwa is a curious man. He is the Executive Director of the Association for Secular Humanism in Malawi and a confessed atheist. He says he has not set his foot in church, and doesn't see any need to. He does not believe in the existence of God or even the Devil. He is a well-accomplished Economist and once headed the Economics Association of Malawi - ECAMA.
Follow this program and hear more about his background, family and his arguments on how he thinks the world came into being.

Опубликовано:

 

15 июл 2019

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 76   
@mosessemuh9681
@mosessemuh9681 Месяц назад
Nthidwa ndi Genious, His brain is superpower.....! You're not alone Mr.
@ThumbikoChipofya-gq7sd
@ThumbikoChipofya-gq7sd Год назад
Ndiyambe ndikuthokoza aChakhaza pocheza ndi mkuluyu, poyamba background yake ( childhood development ) Ku mbali ya chipempedzo sinali bwino .Chinanso nchakut sakufunika kumuweruza koma kumupemphelera kuti apulumutsidwe ndi Ambuye Yesu khristu pot malemba akut mu nthawi yakusadziwa Mulungu analekelera ,nkhan siyongopita Ku mpingo koma kumdziwa womtumikira monga zinachitikira pa machitidwe atumwi9 ( nkhan ya mayitanidwe amtumwi Paulo).Kuonjezera apo Mr Thindwa choti mudziwenso nchakuti maphunziro ngakhale Ali ofunika simayankho amavuto onse amoyo uno ndikupatsani chitsanzo cha nkhani ya m' bible mu buku LA machitdwe atumwi chapter16:16-40 pa nkhani yomwe anamangitsa Paulo ndi Sila.Mutha kuona kut chayambi cha matenda awobwebwetuka uja monga luka ( wolemba bukuli) akufotokozera sichimene adotolo amatenda amisala angafotokoze .Akatswiri azachuma sangafotokozenso out chinsinsi cha kuchita bwino kwa omwe amapindula ndi zimezi ndi chiyan? Komanso gwero lakuvutika kwa wodwala uja? Palinso nkhani zawomenyera ufulu anthu kuyambira wodwalayo,Atumwi aja ngakhale amene anabesa chuma chawo kudzera mzomwe zimachitikazi palibe chomwe angachite munyengo ngati izi.Akupatsan funso mwadwala chipatala chalephera wina atakupempheleran nkuchira mu dzina LA Yesu Khristu mwayankha mododomatu? Mwinanso titakamba za Vuto la uhule anthu alangizidwa kuyipa kwa vutoli kupasidwa ndalama out apeze zochita koma osasintha enanso ndalamazo nkukhala Nazi koma osasintha Alonso ophunzira taonani pano Dziko likupereka ufulu kwa achinyamata kutenga njira zolera chikhalirecho zambiri sizawateteza kumatenda opatsirananapogonan KO'd akuchuluka otenga matendawa mdzina LA ufulu tinene kut zikuyenda ?mutha kuona kut Chifukwa chakuti chiwanda chili mkat mwa munthu uja sichinachotsedwe vuto lizingozungulira Muli ndi maphunziro abwino pezan zochita zabwino moyo wanu uli mdzanja la Yehova yang'aniran mathero ake Hebrews9:27 komanso Ku Genesis 3 akut unapangidwa Ku nthaka komwekonso udzabwelera bwanji maphunziro alibe yankho Ku vuto la imfa? Ndibwelenso Ku machitidwe 16 chimene chinapangitsa Paulo kuzindikira gwero la vuto lija ndiye mphamvu ya mzimu woyera( Mzimu wa chidziwitso ) Yemwe mungampeze mutalapa ndikuvomereza Khristu Yesu ngat mpulumutsi wa moyo wanu ( machitidwe2:38) nkhoswe imene Ambuye Yesu anawauza ophunzira akekudzawatumizira ndikuwatsogolera mu choonadi komanso kuvumbulutsa zinsinsi zochekera kwa Mulungu kudzera mwa mwana wake Yesu Khristu.Chiuta wawe namwe zuwa liweme.
@blessingsnkhwazi273
@blessingsnkhwazi273 5 лет назад
Well educated man koma omvetsa chison eeeeeee ayi, anthu anga akuonongeka chifukwa cha kusadziwa.
@martiusgeorge6514
@martiusgeorge6514 5 лет назад
Powerful God always with him that's why he like Rabecca Malope songs because in doing that he is praying
@andreamillar9896
@andreamillar9896 5 лет назад
Kuyipa kwa Makolo athu potsatengera Ana athu ku Church ndizimenezo a Bambo awu Satanic. Teach a child to know God while he is still young.
@mayababy1877
@mayababy1877 5 лет назад
Uphawi umapangitsa uchimo.izi akupanga pofuna ndalama.the songs he likes are highly spiritual. God loves you mumbuli wanuwo
@mwaibanda5877
@mwaibanda5877 Месяц назад
Unfortunately he is not as poor as you think.
@AngungaThatcherNgoma
@AngungaThatcherNgoma Месяц назад
Yes
@alfredkhogolo1715
@alfredkhogolo1715 Месяц назад
These are nothing but the facts
@blessingskakusa7836
@blessingskakusa7836 11 месяцев назад
Long live George
@edwardbanda5469
@edwardbanda5469 5 лет назад
God is calling him, that is why he loves Rabecca malope. God Himself will make way to bring this man to Himself. He is God of mercy.
@RodgersChikumbutso-jr7fh
@RodgersChikumbutso-jr7fh 24 дня назад
Akufunika kumupemphemphelela
@glorydelezah9629
@glorydelezah9629 5 лет назад
Thanks for the enlightenment, this is absolutely awesome
@Omwale
@Omwale Месяц назад
this guy
@aishachisale4267
@aishachisale4267 3 года назад
Koma zikomo🙌🙌 eeee
@kunsichilazarus9212
@kunsichilazarus9212 5 лет назад
And chimene chidakusangalatsani kuti muzikonda nyimbo za Rabecca ndi umulunguwo please musabisale bambo
@gloriakamanga7329
@gloriakamanga7329 5 лет назад
A Thindwa Rabecca amaimba gospel nde mumapempheranso.
@stephenlupanga1970
@stephenlupanga1970 5 лет назад
Joab ndi #1 kkkkk wampanikizatu munthuyu
@aishachisale4267
@aishachisale4267 3 года назад
Akuluwa a Eliya aposatu😆😆
@SimeonKamwana
@SimeonKamwana Месяц назад
Kodi National Anthem ija amayimba nawo kapena amaiwona kuti ndiyolakwika?
@Littlefair7
@Littlefair7 4 года назад
Titha kuphunzira kwambiri koma nkukhalabe opanda nzeru ngati akuluwa, ndi Mulungu Amene amapereka mphepoyo kutidziwitsa kuti mmadzi simuli bwino ndiye wina kupanga ignore that plain warning.
@DivineSyntaxMw
@DivineSyntaxMw 2 года назад
Ati Mulungu kulibe, kuyankhula kwa zitsiru.😏
@joelmkandawire954
@joelmkandawire954 5 лет назад
That is according to him, (he doesn't believe in God) not you and me, so leave him alone. It's not up to us to judge him.
@ralphhenderson5312
@ralphhenderson5312 5 лет назад
sizoona ngati munthu akutayika akonzedwe akusokoneza life is too short usakhale mbuli
@truthtellerlastonk.m.p4985
@truthtellerlastonk.m.p4985 3 года назад
@@ralphhenderson5312 who told you kuti akutaika????
@chesterphiri7523
@chesterphiri7523 5 лет назад
Poor soul, just being intelligent as he is explaining it's God's blessing.
@kingstonchawinga3869
@kingstonchawinga3869 5 лет назад
Eiiiish ambuye akukhululukireni
@frankmaluwa2749
@frankmaluwa2749 5 лет назад
Humble man friendly person, I'm very sorry for that papa about being arrested for the mcp government by Dr Banda
@kassimjuma8822
@kassimjuma8822 3 года назад
Dzimene mukuyankhula madala ndizopanda nzelu
@DennnisGogoda
@DennnisGogoda 7 месяцев назад
Bible limati, “ Chisilu chimati kulibe Mulungu “ I guess the man so just so ……Let me save my word.
@aubreywallo1987
@aubreywallo1987 5 лет назад
God forgive him!
@christopherchimbetete2196
@christopherchimbetete2196 Год назад
Chamba
@nchessie
@nchessie 5 лет назад
Adzakumane ndi wa njoka ujaface to face adzakambilane bwino
@joechimba742
@joechimba742 2 года назад
Inde mdala
@geee7672
@geee7672 5 лет назад
But Rebecca Malope is a Gospel artist
@ralphhenderson5312
@ralphhenderson5312 5 лет назад
Nchifukwa chake tikuti ndimbuli sakudziwa chomwe akupanga Mulungu amukhudze
@medsonboti1984
@medsonboti1984 5 лет назад
The holy spirit gives one the ability to sense the presence of God. If the spirit is not in you then there is no sense.
@youmad9087
@youmad9087 3 года назад
What spirit is that?
@aminbwanali3954
@aminbwanali3954 3 года назад
This man is the brother of falawo he deserved to be panished
@kassimjuma8822
@kassimjuma8822 3 года назад
Mulungu adzikukhululukilani madala
@truthtellerlastonk.m.p4985
@truthtellerlastonk.m.p4985 3 года назад
Apanga tchimo lanji???
@yankhomtonga6325
@yankhomtonga6325 5 лет назад
Looking at the comments it clearly shows how ignorant the so called christians are: Calling the non believer osazindikira. you guys need enlightment for sure dont just believe for the sake of believing
@georgesiwale8127
@georgesiwale8127 Месяц назад
Yes, I am wondering too. We need to wise up
@simonabraham7241
@simonabraham7241 Месяц назад
For sure, these so-called christians are something else 😂😂😂
@RedsonRichard
@RedsonRichard Месяц назад
Nanu munyanya mwakumana ndi wen wen Satanists
@ellenfumuyiliko1390
@ellenfumuyiliko1390 Год назад
Bola a Eliya aja amadziwa kuti Mulungu aliko osati phwephwa izi
@Littlefair7
@Littlefair7 4 года назад
Ndi omvetsa chisoni, infact he is worse than the devil himself. The devil doesn't dispute the existence of God, according to the book of Isaiah and Ezekiel, the devil wants to be like God the most high. This old man is totally out of his mind.
@johnsong2118
@johnsong2118 5 лет назад
komadi madala awa sangangokhalakhala,akuyenela amadya chamba
@Chikomukomu
@Chikomukomu 5 лет назад
All am seeing is confusion from this guy. He was contradicting himself during the chat
@user-hc6rc7yr8y
@user-hc6rc7yr8y Месяц назад
Satana uja ndamuona ndi maso lero😮
@manzykawika8988
@manzykawika8988 5 лет назад
Muziwerenga Bible Mr thindwa
@apatsamuula4676
@apatsamuula4676 2 года назад
Alibe thawi yowerenga bake akuyakhula xoduka mutu
@duncanchizizi6543
@duncanchizizi6543 3 года назад
Kkkkkkkkkkkkkk
@user-gk6bf7xe9g
@user-gk6bf7xe9g Месяц назад
Drange kwambir kapen fodya Wa chamba😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂
@peterbanda5425
@peterbanda5425 5 лет назад
Akuluwa mutu ukugwila koma
@CatherinePhiri-bw7wm
@CatherinePhiri-bw7wm Месяц назад
Bible linanenakale kuti the fool say there is no God, ndiye mukamawona anthu atelewa wosamadwabwayi p
@basharkhan8933
@basharkhan8933 5 лет назад
Ngati chili chamba chikugwira ntchito
@rashidjackson7085
@rashidjackson7085 3 года назад
Mkuluyu wangokura koma nzeru mulibemo. Google mwini wache ndi muthu osati mulungu ndipo nthawi zina siigwira network
@kunsichilazarus9212
@kunsichilazarus9212 5 лет назад
Kkkkkkkk koma Joab umakumana nazo inetu abambo awo komwe akulowa sindikudziwako.
@Littlefair7
@Littlefair7 4 года назад
According to the Bible Mr. George Thindwa ndi achitsiru, that's it and i can prove it and he has proven it himself kuti, he is a fool.
@mussahswallehchimisa5348
@mussahswallehchimisa5348 5 лет назад
koma abale mmmmm zodabwisa kwabasi munthu wankulu ngati ameneyu?? 😯😯😯
@weruzanicustom4954
@weruzanicustom4954 2 года назад
This atheist akungofunika maumboni amachilitso. Funso lakuchipatala lamuyimitsa mutu mpaka wavomera kuti akhoza kukhulupilira kkkkkkkkkkkkkk
@ellengwazanga6350
@ellengwazanga6350 5 лет назад
Bambowa ndi chiwanda, akufunika mapephero.
@truthtellerlastonk.m.p4985
@truthtellerlastonk.m.p4985 3 года назад
Zaziiii zenizeni 🚮🚮🚮 mapemphero achani??
@ndipo1
@ndipo1 5 лет назад
aaaah kumvets chisoni you dont believe in God- you missing out on a lot hey.
@youmad9087
@youmad9087 3 года назад
Omvetsa chisoni ndi iweyo
@ellenfumuyiliko1390
@ellenfumuyiliko1390 Год назад
Anangokula nzeru alibe🚮
@simonabraham7241
@simonabraham7241 Месяц назад
Ndiye mumlalikira bwanji ndi mau onyozawo?
Далее
CRUISE 5 WITH LUCIUS CHIKUNI PART 1   08 May 2022
58:54
CRUISE 5 WITH THERESA PHONDO
51:44
Просмотров 24 тыс.
A Lyton Mangochi ajatu uku😂
14:58
Просмотров 115 тыс.
CRUISE 5 WITH BYSON KAULA - DEATH ROW SURVIVOR
50:51
Просмотров 92 тыс.
CRUISE 5 WITH NAPOLEON DZOMBE
1:03:03
Просмотров 79 тыс.