Тёмный

HOT CURRENT 14 JULY 2024 | 

DZIWE TV
Подписаться 27 тыс.
Просмотров 23 тыс.
50% 1

Опубликовано:

 

13 июл 2024

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 97   
@patrickndojime1632
@patrickndojime1632 Месяц назад
Go on Guy's we wait to see the changes in Malawi eeeee from Bakili muluzi up to know am in RSA because of politics of Malawi throwing as away not thinking of coming back to home eeeeeeeeesh
@Yungjoe786
@Yungjoe786 Месяц назад
Chilima was assassinated that's the truth what more do u want to hear?
@user-lj8ug5lq8c
@user-lj8ug5lq8c Месяц назад
Guys keep it like this ,this is Hot current we know from those days congratulations
@JamesIngeni-ku3qj
@JamesIngeni-ku3qj Месяц назад
Manganya ndi mcp anapha chilima.
@Martha-m6e
@Martha-m6e Месяц назад
Usi si wa UTM. Munamuwona muja amarandira udindo muja? UTM yachita bwino kuwaturuka.
@gracemkandawire8769
@gracemkandawire8769 Месяц назад
Ngozi ija singozi ngozi ,,komanso yonse taona ndimafinso
@BambordKabambe
@BambordKabambe Месяц назад
😂😂😂😂😂 chaka chino ndi CHONG'ALURA
@JohnNjerenga
@JohnNjerenga Месяц назад
Kkkkk akut ipondeni fadha
@paulpaseli6310
@paulpaseli6310 Месяц назад
Apa ndiye mwabwelatu chilungamo chimenecho
@EstherChimombo
@EstherChimombo Месяц назад
🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥💯💯
@InnocentnMbale-zq8pk
@InnocentnMbale-zq8pk Месяц назад
Times muziwe kuti chilima agwila bwanji ntchito ndi chakwela mu 4years
@henryphiri6100
@henryphiri6100 Месяц назад
Masapota a UTM tonse tatuluka ku mgwirizano Chifukwa tinkasapota Chilima.Usi alibe masapota.
@user-oh9bh1cl3b
@user-oh9bh1cl3b Месяц назад
Well spoken guy's adzimva akawalalawa
@clintonhodda9830
@clintonhodda9830 Месяц назад
Walephera Chakwera kulamulira kuchedwa 4yrs ndipo akhala akungodandaula DPP mmalo mopanga ziganizo msanga
@OrtonKabbichi
@OrtonKabbichi Месяц назад
Sizachilendo olo pa ngozi ya ndege ija anachedwanso kukafufuza ayambe kuchotsa ameneo onwe amaenera kukafufuza za ngozi ya ndege
@patricksinyala1345
@patricksinyala1345 Месяц назад
Mtsukuluzi ukulankhula mopusa, kufooka kwa Ussi kunayamba Chilima alimoyo. Ndipo. Chilimma anali atamuzindikila Kale Ussi ukathyali wake.
@user-un6qv6sj3h
@user-un6qv6sj3h Месяц назад
Inu ussi siwa UTM 😂😂😂😂ameneuja ngawa MCP
@chitanibenito1109
@chitanibenito1109 Месяц назад
Chakwera so asamale zomwe wawona Nzake wa kwa merica zija zichitikanso kuno.
@symonmakata938
@symonmakata938 Месяц назад
Changucho chiyambile pa kafukufuku wa ndege inapha chilima kenako the public ikhala ndi changu
@user-hl3st3cc4v
@user-hl3st3cc4v Месяц назад
Dziko ndilathu osaonesa kutopa azibambo ipondeni thawi ino palibe kuopa ng,alulani basi ng,ambani
@user-jk8sh7fh2d
@user-jk8sh7fh2d Месяц назад
Usi atha ngati nankhumwa sure, olo kuthesako akufuna kukhaulisa manganya coz anamuziwa kuti uyu sitili limozi ndi wa mcp.
@JohnmarkNazombe-hi9xd
@JohnmarkNazombe-hi9xd Месяц назад
Dziko nkumasawukaaaaah!!!!!!!
@henryphiri6100
@henryphiri6100 Месяц назад
Masapota ake ati omwe atsatire Usi ku MCP. Musanamizane palibe yemwe angavotere MCP true member wa UTM
@EfeloYovita
@EfeloYovita Месяц назад
ngati bola Allience latha ndibwino kukhala opanda president cs chakwela polowa m boma unali mgwilizano maka utm inali ndimavoti ambiri kuposa mcp we must have emergency presidental election
@INNOCENTMOFOLO-io8tg
@INNOCENTMOFOLO-io8tg Месяц назад
MCP yayambitsa nkhondo yoopsa yokha amalawi sangasangalale nazo izi Zotsatila results zangozi kuli ziiiii mpaka pano what do you do
@GraceZumazuma
@GraceZumazuma Месяц назад
Keep it up Guy's ife ndalama tidya koma sitidzawavotela talira kokwana sife opusaso pano
@MPHATSOKALUWA-lm2uy
@MPHATSOKALUWA-lm2uy Месяц назад
Akuchedwa Nd pule yomweyo😂😂😂😂😂
@imaculadaAndre-ns1py
@imaculadaAndre-ns1py Месяц назад
Fiti ndifiti basi awa sangaulule chilingamo kwao ndikunama basi koma ife chilingamo tinachipeza kale
@zimmekapachika6784
@zimmekapachika6784 Месяц назад
Akuti mbwexe😅😅😅😅😅😂😂😂
@catherineKalinga-m4c
@catherineKalinga-m4c Месяц назад
🤩
@AishaChipande
@AishaChipande Месяц назад
Chakwela azuzula bwanji pomwe iyeyo anaphaso muzake
@EsnartMbalale
@EsnartMbalale Месяц назад
Ipitilile ndiyabwino coz ikulakhula mosatenga bali
@imaculadaAndre-ns1py
@imaculadaAndre-ns1py Месяц назад
Tamusiyani maganya abakhala komweko adzatiuza zenizeni abawatola zifukwa adzapange sewelo mutu wake chakwera anapha zake chifukwa chaudindo
@OfwaMwambila
@OfwaMwambila Месяц назад
Alot of people re in marriages that ended a long time ago but due to kids u re forced to still living together that's what I think was the case of SKC&usi.
@StiveKantiki
@StiveKantiki Месяц назад
Akuyambisa kuchedwa ndi achakwela ndipo ife tinalakwisa kumuika munthu onamizila ubusa Ngati uyu pa mpando
@chitanibenito1109
@chitanibenito1109 Месяц назад
Mbwelera zokha zokha za mcp kkkkkkk koma pankuku!!!!!!
@BestonStima
@BestonStima Месяц назад
Mcp ivutika chifukwa isanalowe m'boma amalawi ankaopa nkhanza za mbiri yawo Lero in their 4yrs rule patuluka nkhanza. Do you think they can reign???????????
@robertnambazo9936
@robertnambazo9936 Месяц назад
President osaziwachomwe akuchita he is so relaxing President President uyu ndi bubu shatapu zake
@SteveKanongwa
@SteveKanongwa Месяц назад
Koma ma guys inuo hahaha munatopa nalo dzikoli simufunaso zachikape
@KennedyPhiri-h9h
@KennedyPhiri-h9h Месяц назад
Manganya ndi wa mcp not utm
@johnmhango9405
@johnmhango9405 Месяц назад
Briefcase parties end just like that.
@chitanibenito1109
@chitanibenito1109 Месяц назад
Uyakhura za chidodoyo ndiye ili mbudzi yoyambisa chakwera samasata zinthu that’s y anyamata ake angomisewera basi.
@SteveChapola
@SteveChapola Месяц назад
A mcp chipani chokupha
@gracemkandawire8769
@gracemkandawire8769 Месяц назад
Sitizalola report. Wonder you are very Intelligent than pankukuyo
@GodfryMalishe
@GodfryMalishe Месяц назад
Salute u guys 😂
@MPHATSOKALUWA-lm2uy
@MPHATSOKALUWA-lm2uy Месяц назад
How many meetings manganya has been attending?? Can he allow to apart from the alliance coz it's obvious manganya it's won't allow
@peterchikwakwa8476
@peterchikwakwa8476 Месяц назад
Eeeeeee yankhulani guys ❤
@lukedumbula2724
@lukedumbula2724 Месяц назад
Very true wonder and jona, a PULE akuchedwaa
@user-pv9uk6sc3w
@user-pv9uk6sc3w Месяц назад
Pa nkhani yochedwetsa chitukuko, tingomuchotsa next year basi, sali fit Chakwera to be a President.
@gracemkandawire8769
@gracemkandawire8769 Месяц назад
A Usi si president wanthu,,munthu mkazi wake tamuziwa polumbilitsa mkumazitama kuti ine sindinayendepo ndi mkazi wanga,,muthuyu angayendese chipani
@RafiqueChibwana
@RafiqueChibwana Месяц назад
You guys u don't share kamba here really keep it up guys kkkkkkkkk
@JaphetSakala-pq4fl
@JaphetSakala-pq4fl Месяц назад
Kuchokela pa ifa ya VP chilima kufikila pasiku la mavoti UTM ILI PA TOP ONE. or Dpp ndi mcp ita phatikizana. UTM IKUTENGA BOMA TIZAIPEPESA NDI VOTE.
@SheenahMwalabu-iz3pr
@SheenahMwalabu-iz3pr Месяц назад
Lero munabweratu a jonah kkk wonder akuti back to sender eee Chakwera dzimvere mumtolo
@JuuuKomba
@JuuuKomba Месяц назад
Eni ake a UTM ndifeyo ovotafe Tatupu ndife awowo dyela Paolo asaleko tilibe nawo film
@PartsonKamkuzi
@PartsonKamkuzi Месяц назад
Osawopa ayi a malawi ambiri tikuyang'anira inu kut muziyakhura mosawopa apa
@CosimassShyman
@CosimassShyman Месяц назад
Wakulu andevu zamwayi amayankhura Chichewa cha boo
@YamikanChirwa
@YamikanChirwa Месяц назад
Ng'alula iwe
@INNOCENTMOFOLO-io8tg
@INNOCENTMOFOLO-io8tg Месяц назад
😂😂😂😂😂 anyamata inu mwandisangalatsatu chikufunika ndichimenechi osanyangerera kulankhula chilungamo kubandaluka basi sizoopaso ayi
@user-mj2te7vl6p
@user-mj2te7vl6p Месяц назад
Kaya DPP kaya ilibe ndalama iwinabe 2025
@user-rd9pd9hr2l
@user-rd9pd9hr2l Месяц назад
Inuyo munabwera ngati coming 🔥
@MisheckAselo
@MisheckAselo Месяц назад
A pule ayamba kupemphera ku CCAP kamutu kataya
@joneskalitsilo6556
@joneskalitsilo6556 Месяц назад
Exactly Wonder bambo wanzelu amakonza mavuto amu nyumba mwake not kutuluka nkumakadandaula panja or kubwalo kuti mnyumba mwanga sitikudya ana anga sakuvala bwino, sitikudya bwino! Nde ana Inu muzivala bwino, muzidya bwino, ukuganiza kuti anawo azitenga kuti?
@peternashyo9850
@peternashyo9850 Месяц назад
Nkhaniyo ndiyoona, a President akugona kwambiri pachiongolero, dziko silingatukuke ai
@henryphiri6100
@henryphiri6100 Месяц назад
Anaphedwa ku Mwanza aja ndiochepa.pano ayesetsetsa kupha ambiri.athakati sadzasintha.Malawi Congress of Perishers
@DarlingtonMaya
@DarlingtonMaya Месяц назад
Gyz mmmatha
@user-nf3ik3ff6y
@user-nf3ik3ff6y Месяц назад
MCP ndi Yakupha
@PartsonKamkuzi
@PartsonKamkuzi Месяц назад
Iwe pankuku osamayakhura mowopa apa
@BENSONRANGWANI
@BENSONRANGWANI Месяц назад
Chakwela wamupha chilima zasala zosatila Zach
@MuhamadYassin-ye4hn
@MuhamadYassin-ye4hn Месяц назад
Mumakwana mabigi
@Amos-tr6ro
@Amos-tr6ro Месяц назад
Koma makosana inu MMM mwanditha keen on on our behalf
@jackmambo2638
@jackmambo2638 Месяц назад
Kod amaphang’ombe ali kut😂😂
@user-cf9yz3ei5o
@user-cf9yz3ei5o Месяц назад
Did. Mcp ask Afford
@StiveKantiki
@StiveKantiki Месяц назад
Aganizq bwanji mwakuya kuposa anthu zosatheka ubongo unatha chifukwa ankadya zopasidwa Za chaulele
@user-tg7ni7wh2c
@user-tg7ni7wh2c Месяц назад
Eeh 😂
@johnmhango9405
@johnmhango9405 Месяц назад
A kaliati ndi a njawala nzokonza izi, akufuna apange handpick Kabambe, can't you read between the lines? Typical of atsogoleri a dyela.
@user-fd1tu6ku1r
@user-fd1tu6ku1r Месяц назад
Emusipi ofunika isale yokha. Anthu woipa awa
@frankdomingo1109
@frankdomingo1109 Месяц назад
Decisiveness palibepo
@yusufjab786
@yusufjab786 Месяц назад
Ndipo inuyo kumeneko mumaitha 😂😂😂 akuchedwesa ndi chakwera
@user-cf9yz3ei5o
@user-cf9yz3ei5o Месяц назад
You. are. wrong. it. Is. People. at. the. grassroots. who matters not individuals
@PartsonMdeza
@PartsonMdeza Месяц назад
🤣🤣🤣 iponden fadah kkk
@MosesShaibu-ee8hn
@MosesShaibu-ee8hn Месяц назад
Ofufuza ngozi akuti, khoswe akakhala pakhate sapheka
@SteveChapola
@SteveChapola Месяц назад
Asiyeni atuiuka chifukwa chake achakwera apha chirima ndipo ndizoona
@lastonmasoatenganji-bs5gf
@lastonmasoatenganji-bs5gf Месяц назад
Osamayiwala ku mudzi kaamba kokomedwa ndi maidyaidya chifukwa tsiku Lina amadzakusandutsa mtsamiro wa mfumu ikadzamwalira.
@michealchaomba9761
@michealchaomba9761 Месяц назад
😂😂😂 President wake utiyo mukudikira kuti azuzuleyo
@MarthaBanda-ye4pt
@MarthaBanda-ye4pt Месяц назад
Koma Wonder Ati kukura mtima 😂😂😂😂🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥uyatseni basi ng'alulani basi
@user-ru4px8os2v
@user-ru4px8os2v Месяц назад
Anthu ake ndi chimwendo banda,howeh mkaka,zikhaleng'oma ndiomwe akuyenela kuchoka
@ThandiMbewe
@ThandiMbewe Месяц назад
Musamamuzile zochita president, yekha samawona???
@Extratremendouszeus
@Extratremendouszeus Месяц назад
President wake uti Ma comments 100 wa MCP yekha .chita manyazi😅😅
@SteveChapola
@SteveChapola Месяц назад
Chakwera ndiwofoka koma kumagaanthu chimenecho ndiye chitukuko.chake
@NdazionaKumcheza
@NdazionaKumcheza Месяц назад
Ine dakalira malemu za chipani tizitaye uko aaa
@YusufuUsumani
@YusufuUsumani Месяц назад
agaluwa alilimosi ndi chachera
@JudithMaida-ug4oi
@JudithMaida-ug4oi Месяц назад
Mumatiimilira big hands for you
@PartsonKamkuzi
@PartsonKamkuzi Месяц назад
Osamayakhura ngat akupatsani za lent kung'alura basi ukuva iwe ndevuzamwayi !!
@user-ql8nf2vb8s
@user-ql8nf2vb8s Месяц назад
Inu a times muyang'ane mgwirizanou kuchokela mmbuyo inunomwe mumaunikira mgwirizanou mmene umayendela chilima asanamwalile asiyeni ausi ali ndigululawo odya zake alibe mulandu
@MuhamadYassin-ye4hn
@MuhamadYassin-ye4hn Месяц назад
Mumakwana mabigi
Далее
Get 10 Mega Boxes OR 60 Starr Drops!!
01:39
Просмотров 11 млн
Gelik yoki Velik?
00:20
Просмотров 644 тыс.
Sevinch Ismoilova - Xayollarim 18-Avgust 19:00 Premera
00:19
BEAN PHIRI WAFOTOKOZA ZOMWE ADZACHITE |
20:13
Malodza Akuchikangawa A Poem by Sir Michael Benjala
5:00
Shamim Mayanja(Zubeda) akooye aba Family
50:18
Просмотров 3,1 тыс.
TIMES SPECIAL - ENG. VITUMBIKO MUMBA  |  6 AUGUST 2024
58:46
Get 10 Mega Boxes OR 60 Starr Drops!!
01:39
Просмотров 11 млн