Тёмный

KAMLEPO KALUWA BOMA ZOMWE MUKUFUNA KUPANGA NDIKUDZIWA 

Malawi Trends TV
Подписаться 34 тыс.
Просмотров 10 тыс.
50% 1

Опубликовано:

 

1 авг 2024

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 49   
@MosesTangwe
@MosesTangwe 21 день назад
Uku mkuchikweza amputa olakwika, voice imeneyo ikumveka mwa simple koma ili fire😊
@user-ux8bc6wy1i
@user-ux8bc6wy1i 21 день назад
Even neba ku Zambia they know that we don't have president in Malawi
@TwalikiWisiki
@TwalikiWisiki 21 день назад
Mr Kaluwa i appreciate you,,,you a true gentleman a hero,, if it takes you to go back to your past to resolve this chakwera issue so it be,,
@wittinessnkhokwe
@wittinessnkhokwe 21 день назад
Inu a mcp nenani kuti tonse amalawi tichokemo tifune kolowela muone kuti mudzilanulira ndani?
@user-pv9uk6sc3w
@user-pv9uk6sc3w 21 день назад
You have to take this Government to court for this damage.
@luuu22mwanjabala79
@luuu22mwanjabala79 21 день назад
Wise man from the North side
@FionaKhoma
@FionaKhoma 21 день назад
Bora ilili tikachotsa chakwera a police ambili akuyenera kuchotsedwa tchito
@HenryLaidon-pl9ly
@HenryLaidon-pl9ly 21 день назад
Guys Kamlepo ndi One of True democrat ku Malawi kuno tsopano kodi kuzunza mukumuzuza munthu wobweretsa democracy koma kokoliko ndalama zamisonkho yamphawi zakomadi
@amoschataika7440
@amoschataika7440 21 день назад
Well said, loud and clear
@RobertLuka-wy9cl
@RobertLuka-wy9cl 21 день назад
Wise man mr kamulepo ❤❤❤❤❤
@brendamakokola7498
@brendamakokola7498 21 день назад
Politics is dirty game
@JamayakoJamayako-rv2he
@JamayakoJamayako-rv2he 21 день назад
Am agreed with you Pipo shud open their eyes Wise man
@user-jl6sq3ph1b
@user-jl6sq3ph1b 21 день назад
Amenewo ndie mawu amphamvu mbuzi za police zogwilisidwa ntchito ndi chikangawazo makape amenewo akuti agulidwa ndi mcp gvrt Makamaka mai yolamu nayeso chipawa chosamukhala mutu chija mbuzi ya munthu aziwona makape amenewo mu 2025 wonsewo akathela ku mawulapalibeso kuwakhululukila inshaAllah
@user-zy2nh4lj4h
@user-zy2nh4lj4h 21 день назад
Zinazo muzipanga koma za artist fredokiss mukangoesera 😮 malawi tiyatsa mukangopha fredo achinyamata tifafaniza state house
@chipilirokalison1334
@chipilirokalison1334 21 день назад
Sizitheka mulungu alipo kumwamba osamara
@user-ln3zx6wo4w
@user-ln3zx6wo4w 21 день назад
Ndikatundu ameneyu aboma musamutengele masewelo zomwewakambazo ndizoona ndithu
@EmmanuelGasiten-fo5dr
@EmmanuelGasiten-fo5dr 21 день назад
Chomwe wachiona wankulu atakhala pansi, mwana olo atakwera mumtengo sangachione. Welcome Big
@JameChome
@JameChome 21 день назад
Ask Bakii Muluzi anamtangwanitsa kooopya 😂😂😂😂😂
@AleksaWilliams-qc6cn
@AleksaWilliams-qc6cn 20 дней назад
Yooo zilichonchoso 😢
@Blessings-td4cr
@Blessings-td4cr 21 день назад
Boma iliri azitsogoleri mitu sikuyenda bwino why still keeping cellphones of Born kalindo and kamlepo why why Malawi President and the Police why can you please change your decisions why.
@NescotNyamwela
@NescotNyamwela 21 день назад
Ine president wanga ndi Dad Bingu wa mutharika kwa ine sanafe i can see kuti anapanga chani. Kma mbuz zinaz zimangozuza amalawi osalakwa anyway sindili ku malawi kma home is best mbuziyi izaziwa kazachopa pamwambapo
@temwarachaelkhonje3733
@temwarachaelkhonje3733 21 день назад
Aputa olakwika tu....
@FionaKhoma
@FionaKhoma 21 день назад
Mcp ikuyenera kuchoka basi ikuzuza athu osarakwa chakwera wakupha ayende basi
@raytavares2256
@raytavares2256 21 день назад
Collect your phone via the attorneys and high court on releasing it without prejudice and bias. We are praying for you. Ndine kuno ku Great Britain. Yes the late dad Green Ng'oma used to w for Southern Bottles even when they lived in Mzimba before moving to Zingwangwa Blantyre and after ZINGWANGWA THEY MOVED TO ALIMAUNDE AREA 25 LILONGWE. We must all pray for each other and the countries experiencing the political tarmoils.
@zelliachamboto5744
@zelliachamboto5744 19 дней назад
Kulibedi wamuyaya
@MzikaPhiri
@MzikaPhiri 21 день назад
Amen Amen...
@IdahNyasulu
@IdahNyasulu 21 день назад
Deal with them bwana kalua
@GeraldChisokeza-er5cf
@GeraldChisokeza-er5cf 21 день назад
Oh no osat Fredo ayi.Komano kukhetsa Mwazi chifukwa Cha mpamdo Kaya Mulungu amaona amakantha
@mbewemisoyaanenenji1908
@mbewemisoyaanenenji1908 21 день назад
You fought ngwazi , who are these dogs to fear .
@user-jl6sq3ph1b
@user-jl6sq3ph1b 21 день назад
Apolice yakhani kuti umuyaya uja udakalipobe kapena ai?
@MaxWell-d7o
@MaxWell-d7o 21 день назад
Pambuyo panu bwana..iponden
@user-kp7le2pu7h
@user-kp7le2pu7h 21 день назад
Wise man❤❤❤
@peterchikwakwa8476
@peterchikwakwa8476 21 день назад
Pena pache MCP tu , mukuonjeza eti!!?? Is this what we wanted? Why why why??
@ShorayChimera
@ShorayChimera 21 день назад
I feel ur pain father 💔
@victorauwana7258
@victorauwana7258 21 день назад
Good 👍
@NaduMbewe-zz6iw
@NaduMbewe-zz6iw 21 день назад
Zosaesanda
@AgnessMzengo
@AgnessMzengo 21 день назад
Iponden fadah,,,,,
@babranzima8120
@babranzima8120 21 день назад
Athu akupha abusa wokopha kodi eeeeee athu akumpoto mwasiye mutha ndinu achakwera ndi azanu wood
@EllinaBitto
@EllinaBitto 21 день назад
😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭
@user-fq4kv8dj4t
@user-fq4kv8dj4t 21 день назад
Mwaonjeza English enafe sitimva nde izizo muzilankhulako chichewa chifukwa nzatonse amalawi kuti timve
@CharlesKachipanda-jz9jv
@CharlesKachipanda-jz9jv 21 день назад
Awuzeni makapewa adziwe kuti inu madala madala
@MagaLassi-tg7lj
@MagaLassi-tg7lj 21 день назад
🆓✊
@user-ss9bj5eh6b
@user-ss9bj5eh6b 21 день назад
chonde bwelerani muzakale bwana tithane nawo anthu oipawa
@Standwell78
@Standwell78 21 день назад
Chana?? Ayesele
@YasinMusa-ym8lp
@YasinMusa-ym8lp 21 день назад
Akupa mcp
@MilacleSankhani
@MilacleSankhani 21 день назад
Ask late kamazu about u
@HamzaMkwanda-bh8dc
@HamzaMkwanda-bh8dc 21 день назад
Wise man
Далее
вернуть Врискаса 📗 | WICSUR #shorts
00:54
Штаны легионера
00:44
Просмотров 415 тыс.
Best exercises to lose weight ! 😱
00:19
Просмотров 12 млн
A Michael Usi Inu Si A UTM - Lyton Mangochi
23:13
Просмотров 26 тыс.
Malodza Akuchikangawa A Poem by Sir Michael Benjala
5:00
EXCLUSIVE INTERVIEW WITH BON KALINDO
59:52
Просмотров 54 тыс.
@HeadmanChigodora Mukadzi wemunhu haabatwi Pt1
48:21
Просмотров 39 тыс.
FREDOKISS WANG'ALULA LERO KU MZUZU 28 July 2024
22:16