Тёмный

KUDALI ZOTANI LERO? CHILIMA R.I.P😭😭 

HOT 265
Подписаться 58 тыс.
Просмотров 47 тыс.
50% 1

Опубликовано:

 

14 июн 2024

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 99   
@user-ml1su3ny2e
@user-ml1su3ny2e 5 дней назад
Mumamunyoza mwana uja inu a mcp ,samakuyankhani,koma mpaka tafika apa zoona? 😭😭😭💔
@AndrewKonondo
@AndrewKonondo 6 дней назад
A hero don't exist in avaccume😢😢😢chilima was ahero rest in peace
@user-yh3dw6qu7z
@user-yh3dw6qu7z 5 дней назад
Achakwera sipatha miyezi 9 mulungu asaphwanye ufumu wanu.nkhoswe mzimu oyera, fire to those crocodiles.
@user-ij3ol6jo5w
@user-ij3ol6jo5w 6 дней назад
Rip frm Namibia...it's so bad..I am also thinking about my late president..it's still fresh...all the comfort frm above
@princedetbozsmallboy1749
@princedetbozsmallboy1749 6 дней назад
Ngakhale ine sindikhulupilila 😢 Chakwera zomwe wapanga Mulungu achite nanu nose 😢
@PaulChaleka-lb4vx
@PaulChaleka-lb4vx 5 дней назад
Chilima adali osunga nthawi, odzichepetsa, olimbika and freedom fighter dziko tilowele kt ambuye? Eeeee mulungu yemwe wapanga izi eeeee pelekani chilango kt adziwe kt mulibe chinyengo alangeno
@user-oc8nj3or6y
@user-oc8nj3or6y 6 дней назад
I quote these words *Don't fear* don't get tired,, do not get discouraged. If I here this,,, I see The legend called SKC😢😢
@storytambala6088
@storytambala6088 6 дней назад
Chifukwa chiyani, mukutsogoza munthu oyipa pamaso pa anthu wolungama Chakwera m'busa oyipa.
@hissimajohn965
@hissimajohn965 6 дней назад
Bulayani mukachezenso ndi achakwera tiwamve ndithu ndi iwe mtola nkgani wa luso
@peterchikwakwa8476
@peterchikwakwa8476 6 дней назад
Imfa ya chilima yowawa, he is a matyr
@PaulChaleka-lb4vx
@PaulChaleka-lb4vx 5 дней назад
Chilima anali munthu ofunika koma mulungu atithandize kuchotsa chakwera eeeee munthu oipa wamuzunza chilima koopsa
@dondamissonchdziwe3958
@dondamissonchdziwe3958 5 дней назад
Tachipheni chi Yudas Chakwera cho, chitsiruu chikupangapo chani? wamupha si ndi iyeyo Chifukwa cha nsanje fisi ameneyo nkhope yake ngati mzukwa,muchithamangitse ku Malawiko
@isaiahbanda4590
@isaiahbanda4590 6 дней назад
Noted with thanks Brian we are really lost the wise one from ZAMBIA thanks 🙏
@MIMIEZenga
@MIMIEZenga 6 дней назад
WApha chakwera
@PaulChaleka-lb4vx
@PaulChaleka-lb4vx 5 дней назад
Zoona chakwera ndi oipa adaonetsa pophwanya lamulo LA gwilizano
@BernadettaBanda
@BernadettaBanda 5 дней назад
Because God does not reveal to some pipo don't know how precious someone is like Judas we regret at the end. MHSRIP.
@victorauwana7258
@victorauwana7258 6 дней назад
Achakwela powona nkhope anvekele yah 😮,,, " yah ndakunyesa galu iwe" ..
@mailos.laisoni7001
@mailos.laisoni7001 6 дней назад
Kkkkkkk inu
@aureliojose763
@aureliojose763 6 дней назад
Kkkkk
@MarkFloraLimbaniManyowa
@MarkFloraLimbaniManyowa 6 дней назад
🤣🤣🤣🤣 Amvekele umati utani mwana wausilu iwe
@janetmalambo9559
@janetmalambo9559 6 дней назад
Koma inu mmmmmmm poti iwowo ndi amuyaya
@YNOTGEORGE8
@YNOTGEORGE8 6 дней назад
Azafabe naye
@TimothyKadyamaliro
@TimothyKadyamaliro 6 дней назад
May his Saul rest in massive peace and anthu NDI abodza koma Mulungu ndiye wachoonadi
@raphaelbanda875
@raphaelbanda875 6 дней назад
Apapa zikuoneka kuti Chilima anabeledwa ma vote 2019...
@jacksonmaston7055
@jacksonmaston7055 6 дней назад
Sir mwanama inuyo or mutafa lero Adani anu aja sangaime poyera kukunenerani zoipa ata but the truth is that he was a hero may his soul rest in peace
@paulmakupe
@paulmakupe 6 дней назад
Koma chakwera akumaonera zimenezi?
@champianchampian2148
@champianchampian2148 5 дней назад
Enawo akuoneka ali nzokamba koma akuopa,,ati mulungu nde akudziwa
@JaneMoyo-ws2di
@JaneMoyo-ws2di 6 дней назад
Nanga ife tili ku mudzi simungatijambulileko nkhope kuti nafe timuone komalizaapapa. Ili ndi pempho ku mpando
@user-yk5xv4dt7v
@user-yk5xv4dt7v 5 дней назад
Achakwera asaiwale kt mack sall wathawa ku senegol ndipo ali ku france
@atupelemwangomba206
@atupelemwangomba206 5 дней назад
Awowonso anapita kukapereka ulemu , zikukhala ngati akukasewreratu
@mozykavalo7352
@mozykavalo7352 5 дней назад
pali mau oti palibe ochita choipa azakhale moyo wake osalangidwa onse apanga izi i decrear kut Juses azuke and pay punshiment to those who take hand accordingly I pray to Jeaus to bring another person who will fullfi ma plan a Yesu pa ana ake death to the life opresser
@McphersonMsulira-zx2lj
@McphersonMsulira-zx2lj 6 дней назад
Ngozi ya ndenge anthu kuona kope koyamba kuziona ku Malawi kuno
@user-fl9xy8bk7e
@user-fl9xy8bk7e 6 дней назад
Imfa yopweteka kwambili chakwera ndgulu lake nonse muzalipira nd2
@HanniaAwali
@HanniaAwali 5 дней назад
Akuti anadya nkhumba yootchedwa ndi vp eish timva zinthu.
@user-xx4jb9se3z
@user-xx4jb9se3z 5 дней назад
Ndakhumudwa ine dzulo ndimayankhula ndi anthu kumudzi akundyankha ali musamanene ZA chilima akumangani ine eshhh akuti ndipoakuti ku Malawi kwavuta chakwera must go
@user-oc9vl9xz8e
@user-oc9vl9xz8e 6 дней назад
Watching live from SA
@EmmanuelMwaskakata-ln8po
@EmmanuelMwaskakata-ln8po 6 дней назад
RIP kudzanja lawo lamanja kwima malia mfumu yamtendele
@user-ux3ed3ni1p
@user-ux3ed3ni1p 5 дней назад
What a loss for Malawi😢
@CassimMbalaka
@CassimMbalaka 6 дней назад
Mulungu salakwitsa kalikose adziwa yekha chochita nximu wanu uuse mumtendere bwana chilima
@PaulChaleka-lb4vx
@PaulChaleka-lb4vx 5 дней назад
Ndikutha kuona kt vote ichitike mawa mcp percent go down dabble or triple
@user-ly3fc5xq2f
@user-ly3fc5xq2f 6 дней назад
Chilima mulungu amusogolere ku umoyo wina omwe waulowa
@GospelSoldiers-sr7np
@GospelSoldiers-sr7np 6 дней назад
Amen
@ChrispinVekani2-qe8tj
@ChrispinVekani2-qe8tj 5 дней назад
Ndi zinthu zopweteka kwambiri, koma chofunika ndi kuvomeleza komanso kuzisiya zonse mmanja mwa mulungu. Chifukwa tisaiwale kt mulungu amakondwera ndi imfa ya munthu olungama. Koma tsoka Kwa iye emwe akakamila machimo nadzafa ali chichimwileni. Chifukwa mulungu sakondwera ndi imfa ya munthu ochimwa. Tsoka Kwa iye adzetsa imfa Kwa munthu osalakwa , komanso nalora kufa asadalape tchimolo. Mizimu ya anthu onse omwe adafa pangoziyi yiuse mu mtendere osatha. Ndipo mulungu apukute misonzi ya abale komanso amalawi tonse omwe tikulira pa imfa imeneyi. Mulungu ndiwachikondi nthawi zonse
@FrankKambwani
@FrankKambwani 6 дней назад
Chakwera apapa Bola akanamupha Kunkuyu or Zikhale
@victorauwana7258
@victorauwana7258 6 дней назад
So sad😢
@JaneElisha-db1dz
@JaneElisha-db1dz 6 дней назад
Out of words😭😭😭
@bongimageret8792
@bongimageret8792 6 дней назад
May his soul rest in peace. Farewell leader
@FunnyMtonga-fb9rd
@FunnyMtonga-fb9rd 6 дней назад
Mzimu wao uunse mtendele achilima
@Furnituremaker-vt8ku
@Furnituremaker-vt8ku 6 дней назад
Ausi muntendere Dr saulosi chilima
@y-cmsamalastarz3097
@y-cmsamalastarz3097 6 дней назад
Walira Patrick mwaungulu😢😢😢
@Hopenandola-zg6kz
@Hopenandola-zg6kz 6 дней назад
Zovesa chison kwambili chilima akause mtendele
@user-xc1gk6bw6m
@user-xc1gk6bw6m 5 дней назад
Rest in peace mr chilima but only God knows for your Death 😭😭😭😭😭
@Disiel-ez1ce
@Disiel-ez1ce 5 дней назад
😭😭😭😭outof words😭😭😭😭
@user-xx4jb9se3z
@user-xx4jb9se3z 5 дней назад
Chakwera wapha anthuwa chilima munthu adali odzichepetsa mpaka kusesa mu church.kutolera ndalama mu church mzimuwake uusemu mtendere
@JustinLipipa
@JustinLipipa 6 дней назад
Chakwera wapha chilima, Mulungu amuone bac
@user-tx3oq4ns8p
@user-tx3oq4ns8p 5 дней назад
Very sad indeed
@WhiteRichard-cw2fo
@WhiteRichard-cw2fo 6 дней назад
Pamene tose tikulira amene wachita chipogwe ichi mulungu musamusiye choncho ayi
@juliusnjerengo2610
@juliusnjerengo2610 5 дней назад
Paja anthu ankati ku DPP anthu aphana nthawi ija Nankhumwa akupanga zake zosokoneza. tell me now, ndikuti kumene aphana? Wakusendani Chakwera.
@JosephAlaba-hj5kx
@JosephAlaba-hj5kx 6 дней назад
Ngat bodza koma ayi ndi2 .
@SteveChirwa-ne9nt
@SteveChirwa-ne9nt 6 дней назад
Chakwera tula pansi udindo pamodzi nduna zakozigawenga mulungu akuoneni nose !!!!
@hassanimaliki2145
@hassanimaliki2145 6 дней назад
😢😢
@priscachiyenda
@priscachiyenda 5 дней назад
😢😢what a life
@jacksonmaster2288
@jacksonmaster2288 5 дней назад
Tikudikila kuti atiuze kuti amanama sanafe 😢😢
@user-on9yh6sg4g
@user-on9yh6sg4g 6 дней назад
Ndikutha kuwona azimayi azipani zina koma amayi a tambala wakuda ali kuti?
@user-yk5xv4dt7v
@user-yk5xv4dt7v 5 дней назад
Kulila kumeneko ndi mavote bro
@InnocentChiwaya-pk1fo
@InnocentChiwaya-pk1fo 6 дней назад
R I P
@VincentMadalitso-wk1ny
@VincentMadalitso-wk1ny 5 дней назад
😭😭😭😭😭😭
@IssahMussah-oq3js
@IssahMussah-oq3js 5 дней назад
Chakwela ndimutu oyipa kwambili
@hendieNkhomah
@hendieNkhomah 5 дней назад
rest in peace my president
@maggiendala664
@maggiendala664 5 дней назад
😭😭😭😭😭😭😭😭😭
@christopherbiskem4087
@christopherbiskem4087 6 дней назад
May he's soul rest in peace watching from South Africa Derban
@user-ez9lg7wn6m
@user-ez9lg7wn6m 5 дней назад
Onse a MCP akuziwa zokwe akupanga agalu
@laston-rj2qs
@laston-rj2qs 6 дней назад
Mwayionela patali kusabwera kwanu naye ku mzuzu
@PaulChaleka-lb4vx
@PaulChaleka-lb4vx 5 дней назад
Chakwera akunera kumuotcha ndi munthu oipa
@RobertLuka-wy9cl
@RobertLuka-wy9cl 6 дней назад
Galu chakwera mulungu amulanga ali moyo mbuzi ya munthu
@user-hs1pl5qn7i
@user-hs1pl5qn7i 5 дней назад
Ana Amma 2000 mwadziwano kuti mcp ndichani eti?
@SteveChirwa-ne9nt
@SteveChirwa-ne9nt 6 дней назад
Chakwera wapha chilima . Chakwera usamange asilikali achilungamo kuposa Valentino wako apo pamafunika malemu Manken chigawa mzimu wake uwuse mumtendere.osati chigewenga Ichi Chi Valentino Phiri
@newtonk5822
@newtonk5822 6 дней назад
I think we should be objective here. Have we considered the role that the pilots contributed? According to the UDF commander, he said the lady had 700 flying hours. That is not a lot and she may have been fatigued with the back and forth. Don't discount pilot error especially when the weather is not good. Let's wait for the inquiry
@ChristinaLigomeka
@ChristinaLigomeka 6 дней назад
INEYO namvera nkhani za bakili muluzi anati wagwila ma hours 2000 zinazo zabodza za 700
@ChristinaLigomeka
@ChristinaLigomeka 6 дней назад
Bakili muluzi tv
@MosesNgwira-dm4ui
@MosesNgwira-dm4ui 6 дней назад
Pepani kwa aMalawi wonse MHSRIP
@Thembokatuli
@Thembokatuli 6 дней назад
Chakwera galu galu mbuzi munthu osayamika chizete
@laurentbutao4084
@laurentbutao4084 5 дней назад
Following
@kingjaddumalawi
@kingjaddumalawi 6 дней назад
Chakwera ndamene wapha chilima
@MichaelWilliamsNyirenda
@MichaelWilliamsNyirenda 6 дней назад
That's facts
@Justman34_dislike
@Justman34_dislike 6 дней назад
Mulungu azaweruza tsiku limodzi
@IssahMussah-oq3js
@IssahMussah-oq3js 5 дней назад
Chakwela wajayila pamalawi
@lungisanishezi1023
@lungisanishezi1023 6 дней назад
Chakwera naweso udzafa ufune usafune
@HalisonSolomon
@HalisonSolomon 6 дней назад
Ndipo satana chakwera akadakhala wina momwe anthu akulirira akanatula pansi udindo ndi nduna zake zonse lusifar kunamizira ubusa, saulos may your soul rest in peace, we shall remember you, koma Mulungu odziwa kuyankha ayankheni a malawi, pa kulira kwao LORD you are consumin fire please Lord consume every evil in Malawi's government
@Enocie
@Enocie 6 дней назад
Zimu wanu uwuse mumtendere
@sandramkaligida1163
@sandramkaligida1163 6 дней назад
Palibe pozembela imfa
@DansaYamikani
@DansaYamikani 6 дней назад
Hiloma tizimulirabe PA nkhani yamatumizidwe a ndalama kuno ku South Africa Airtel money ndiyachangu kwa Ife anthu tili ku South Africa adatikodzera tsogolo lowala lija 😢😢😢
@PaulChaleka-lb4vx
@PaulChaleka-lb4vx 5 дней назад
Chilima adali osunga nthawi, odzichepetsa, olimbika and freedom fighter dziko tilowele kt ambuye? Eeeee mulungu yemwe wapanga izi eeeee pelekani chilango kt adziwe kt mulibe chinyengo alangeni
@jonathanmunthali8500
@jonathanmunthali8500 6 дней назад
Nayeso yizampezaso yangati yimeneyi ifa yowawa ngati yomweyi
@Justman34_dislike
@Justman34_dislike 6 дней назад
Mulungu azaweruza tsiku limodzi
Далее
Они всё испортили..!? Lixiang Mega
27:14
D3 Ferrari 296 GTS. ОНО ТЕБЕ НАДО?
17:12
Просмотров 134 тыс.
KAFUKUFUKU PA IMFA YA ACHILIMA
30:18
Просмотров 56 тыс.
Maloto A Bon Kalindo (Part 2) - Bon Kalindo
14:17
Просмотров 43 тыс.
ZINTHU AKUZIYENDETSA MOTANI_IMVANI ZONSE PA KWAGWANJI?
33:23
Unknown side of Dr Saulos Chilima
13:37
Просмотров 25 тыс.
Они всё испортили..!? Lixiang Mega
27:14