Тёмный

ZINTHU AKUZIYENDETSA MOTANI_IMVANI ZONSE PA KWAGWANJI? 

HOT 265
Подписаться 61 тыс.
Просмотров 32 тыс.
50% 1

Опубликовано:

 

19 июн 2024

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 107   
@user-mh7cc8up4i
@user-mh7cc8up4i 6 дней назад
Zabwino zose Mr usi koma pempho ndilakuti mumamuwona chilima mene amakhalila ndi athu analibe sakho ndiye tikuziwa kuti simungatenge zose zomwe ankachita chilima koma pangani zoti amalawi tisakuzondendi komaso muziwe kuti mwakhala pamenepo namba 1chifukwa cha malemu chilima namba 2 chifukwa chachipani chamampha UTM namba 3 chifukwa chaife amalawi ndiye momwe timakuziwilani musasithe mawanga nkumalindila mandasi panopo amalawi anasukusula kumaso mapeto azose mukhale owopa mulungu komaso kupewa njila zachinyengo well come Mr usi
@user-uv5rf4zt5q
@user-uv5rf4zt5q 6 дней назад
Politics is a dirty game don't trust.
@user-jk8sh7fh2d
@user-jk8sh7fh2d 6 дней назад
Ndi amozi , usi ndi wa mcp ameneyo munthu winaso oipa pa ziko pano. Ku utm Michael usi anangobisalirako ku utm chifukwa amaziwa kuti ilibe pic yabwino ku ntundu wa amalawi, tingoti ndi ochenjela kwambili.
@user-lu5db5qk2o
@user-lu5db5qk2o 6 дней назад
He is the next dont woŕry
@Dickies-mk8cd
@Dickies-mk8cd 6 дней назад
Mkanakhala Usi mkanakana udindowo umenewo😮
@user-hm9nc7lz6e
@user-hm9nc7lz6e 6 дней назад
Zoonadi micheal utsi amadziwa kanthu za chilima mdi mkona anakhala pakhani ya imfa yawo
@inessmsiyambiri8517
@inessmsiyambiri8517 6 дней назад
Ndalama ndi satana mmm
@user-bq9rj2mi4h
@user-bq9rj2mi4h 6 дней назад
ndalama zizawaphesa a malawi
@MarthaJafali
@MarthaJafali 6 дней назад
Ndiwadyela ndiye kuti anali kazitape wazaukndi uku
@MTUKK
@MTUKK 6 дней назад
A usi tsekani makutu anu muva zambiri kuchokela ku anthu osiyanasiyana paja bible Ku miyambo limati chitsiru chifunafuna zeru koma osayipeza koma milomo ya zeru impulumutsa iye. Chonde endetsani udindowo motsogozedwa ndi mulungu was zatheka bwanji
@MTUKK
@MTUKK 6 дней назад
Ufune usafune using ndi vice president iwe Cadet ulongolola utopa chifukwa ukungonaniza chabe choona akudziwa ndi mulungu koma ngati uli ndi umboni oposa mulungu kalankhula koma ngati ulibe umboni okwanila Kuala chete ungachimwe pa maso pa mulungu
@JosephyMagombo
@JosephyMagombo 6 дней назад
Mulungu ndiwadongotsolo let it be
@MemoryMbalat
@MemoryMbalat 6 дней назад
Mulungu ndiwadongosolo bas Takulandilani bas
@MemoryMbalat
@MemoryMbalat 6 дней назад
Komanso tsogoleli amasakha ndi Mulungu ❤❤❤ine ndendawakondatu amanganya❤❤❤❤Welcome my dear ❤❤
@StevenMjMbama
@StevenMjMbama 6 дней назад
Mikhatheya atatu inu mumandivetsa kukoma u are there for Malawi big up time Bayana msiska ndi Brian that's great
@user-fb6kh2dk1y
@user-fb6kh2dk1y 6 дней назад
Congrats Mr VP aaaa Mulungu akudalitsen
@PeterThomas-lw3io
@PeterThomas-lw3io 6 дней назад
Wowo Mr B I like your Question
@MisheckAselo
@MisheckAselo 6 дней назад
Koma mongokumbutsana MCP ndale amapanga ma dzulo ndiye eee tiziona 🤔
@Yasin-Charles_169
@Yasin-Charles_169 6 дней назад
😅😂🤣😁😄😃😀
@BaxterKachelenga-mb7wx
@BaxterKachelenga-mb7wx 6 дней назад
Dr usi ,welcome you have a lot to do at a short period,study Bingu politics before candidacy which led him to be elected to be president, people will watch your practices very carefully.And learn how good was Saulos.wish you good Long live.
@wezzieneba9238
@wezzieneba9238 6 дней назад
Congratulations Dr Michael Usi
@OmarMkwela
@OmarMkwela 6 дней назад
Akuphipilitsa za imfa ya achilima kokhonza ma program okumupha chilim utsi yo analipo akuziwapo kanthu nagati amqfuna kusankua munthu ochokera ku UTM ndikumuyika ku MEC nanga sipamenepo mgwirizano ukanakhala ukupitilirabe
@nelsonstevenphiri7096
@nelsonstevenphiri7096 6 дней назад
pompano akhala president amanganyawo .
@Geraldmkwewu
@Geraldmkwewu 6 дней назад
Manganya lnari game kale ndichakwera ndiwa mcp ameneyo tikulira chilima wanthu lfe mpaka kalekare
@JamesIikagwa
@JamesIikagwa 6 дней назад
Congrats Dr Usi
@JimmyIsaac-xd4ef
@JimmyIsaac-xd4ef 6 дней назад
Ausi adzazioona zimene wakumananazo a Chilima, MCP ndikhalidwe lawo
@AndrewPande-gg6ek
@AndrewPande-gg6ek День назад
❤❤Congrats usi
@user-um1lq7ms5d
@user-um1lq7ms5d 6 дней назад
Muthu akachita chabwino tiyamikile .apa kunena zoona alemekeza chipani cha utm. Cifukwa ndi vis wa malemu
@chitanibenito1109
@chitanibenito1109 6 дней назад
Ndi zomwe amafuna kumpereka nzake munthu osalakwa ayi there is God in heaven!!!!
@ThivadoartistDyson
@ThivadoartistDyson 6 дней назад
Kkkķkkkmk ndimanganya kumene
@EmanuelChitsambatata
@EmanuelChitsambatata 6 дней назад
Apa ndiye dziko lino linkhalira masewero ndimthu😂😂😂
@ShearstonNyirenda
@ShearstonNyirenda 6 дней назад
Congra usi
@user-oc9vl9xz8e
@user-oc9vl9xz8e 6 дней назад
Mr usi ndi wanzeru Bola asapusisidwe ndi MCP muonese chisanzo cha bwino ku UTM osapanga zokomela MCP... congratulations
@OwamThoko
@OwamThoko 6 дней назад
Si anthu koma president ndi amene ali ndi vuto,bwanji wapha vice wake
@Groly-fq5tt
@Groly-fq5tt 6 дней назад
Koma chonde bwana usi musatembenuke kuti azanu a UTM kuwakhumudwisa mumene mwarowera mu office imeneyi mukakumbuke masomphenya achirima komaso kuti inuyo muzasogorere 2025 malingana ndimugwirizano wa chakwera nda achirima musakawope nduna za MCP chonde chonde kuchokera kuno ku mzuzu chipoka stv mundirembekoso tchito yo kuyendesani ❤❤❤❤
@EmilyTembo-zu4zy
@EmilyTembo-zu4zy 6 дней назад
Eish this life no balance only God knows
@MadehNYC
@MadehNYC 6 дней назад
Aaa palowa ndale apo Mr chakwela atenga Mr utsi ku UTM ndicholinga chofuna kuti akhale chete Ku UTM ndy angochenjela basi
@AlexKaunda-ny2eg
@AlexKaunda-ny2eg 6 дней назад
Awaso akwagwanji anadya chibanzi chokani Afiti inu
@JafaliChiwimbi
@JafaliChiwimbi 6 дней назад
Zapatunthu zimenezo musati pepelese ife
@user-zk7jw9up6m
@user-zk7jw9up6m 6 дней назад
Brian ndi wa Mcp
@jogechawa6192
@jogechawa6192 6 дней назад
Usi analowa MCP Kalekale amangobisalira ku UTM he is a sell out soon alengeza kuti walowa mu MCP
@alinafesalima5597
@alinafesalima5597 6 дней назад
Nkhaniyi ndi yoona and Usi ndi munthu woyipa kwambiri ndi amene wamugulitsa chilima
@PrinceKachimanga
@PrinceKachimanga 6 дней назад
BRIAN...PANO AKUMVEKA KUTI NDIWA MCP...no doubt
@blessingbanda6206
@blessingbanda6206 6 дней назад
Good example is Zelensky from comedian to president .
@user-vr5jn8sz5r
@user-vr5jn8sz5r 6 дней назад
Munapasidwakale mabadzi.Andevu zasoka .
@Alliechamolie
@Alliechamolie 6 дней назад
Tilibenazo ntchito zimenezo mukuseka Maso ndani
@danieltengeletu3952
@danieltengeletu3952 6 дней назад
Michael usi ndiwa MCP kuchoka kale . UTM anangolowako muwone film yakubwera kwa ngwazi
@BatumeyoChikopa
@BatumeyoChikopa 6 дней назад
Tikuferanji ntsopano
@DaveSitolo
@DaveSitolo 6 дней назад
Kodi Kwa asowa anthu okhala vice president uchitsiru kumalawi suzatha
@OwamThoko
@OwamThoko 6 дней назад
Don't allow chak😢wela kukuphuzisa maplan okupha
@GiftPetros
@GiftPetros 6 дней назад
Congratulations bizwiki but be clever like skc
@InnocentMlowoka-ew4lo
@InnocentMlowoka-ew4lo 6 дней назад
Bakili mluzi tv adatiuza kale izi😂😂
@Yasin-Charles_169
@Yasin-Charles_169 6 дней назад
Exactly
@Dickies-mk8cd
@Dickies-mk8cd 6 дней назад
Brian ndi azinzakowo ndinu agalu nonse, muli pamenepo kuseka uku mukukambilana zanu zapamtumbozo, inu moti simukuona kut iyi ndi game plan kut imva ya Chilima mbali foul play kuti napamtumbo wako Manganya wapha nawo Chilima😭😭😭🤚🤚
@kearabetswemashego3084
@kearabetswemashego3084 6 дней назад
Zaugalu
@LodrickJamitoni
@LodrickJamitoni 6 дней назад
He was able to pick up the microphones and use the voice of the priest
@Alliechamolie
@Alliechamolie 6 дней назад
Komaso timaziwila nsimungatenge wa mcp cholinga mupusitse wathu unja mwamuphela cholinga panalingwizano wa five years, awatso muwabudula tikuziwa
@chekiamaabdul5083
@chekiamaabdul5083 6 дней назад
Bambo asikono umatokotatu nthawi yomwe unalu out of politics now you're in tikuwonela
@StiveKantiki
@StiveKantiki 6 дней назад
Km muwachenjeze anzanuwo sachedwa kuwachula mabatile abayana tchungawo
@OwamThoko
@OwamThoko 6 дней назад
Komanso malangizo kwa usi,,alembe asilikali achitetezo ambili owateteza otherwise sitifunanso kulira popano,ndege ukamakwela pls make sure pls ,n akakupasa ndege yoti uyendele paulendo make sure employee 5000 asilikali n also they mct gurd 5 days bfr ulendo
@AdamzChirwa
@AdamzChirwa 6 дней назад
🙏
@AllanChabwela
@AllanChabwela 6 дней назад
Usi ndi wa mcp since kalekale .birds with the same feathers fly together
@user-do2cs8nf4b
@user-do2cs8nf4b 6 дней назад
Tiyeni nazoni tidziwona m'mene zithere
@DangoNgwira
@DangoNgwira 6 дней назад
Nkhope yanu muzichotsapo. Ifeyo like your followers tiziona full pictures.
@lucksongondwe8266
@lucksongondwe8266 6 дней назад
Asamale naye ndege ingagweso
@meditationmusic293
@meditationmusic293 6 дней назад
Musakhaletu mukulimbilana ma udindo ku times ko kkkkkk
@PrinceKachimanga
@PrinceKachimanga 6 дней назад
kutha kwa UTM 😂😂😂
@EdwardSamuel-xj8qq
@EdwardSamuel-xj8qq 6 дней назад
Yaya
@SolomonDmajor
@SolomonDmajor 6 дней назад
We're not stupid we just looking at you next year tivotabe
@Alliechamolie
@Alliechamolie 6 дней назад
Amalawi two days amakamba za chilima pano alipa usi , mulindimvuto tsimuchedwa kuyiwala
@RodggerBandah
@RodggerBandah 6 дней назад
Maganizo abwino cifukwa phavu za tose areas ziri muzipani zose 9
@Groly-fq5tt
@Groly-fq5tt 6 дней назад
❤❤❤❤❤❤❤❤❤usi
@Dickies-mk8cd
@Dickies-mk8cd 6 дней назад
Usi ndi betrayer😭😭🙏🙏
@PrinceKachimanga
@PrinceKachimanga 6 дней назад
Bambo a sikono😂😂😂😂
@JafaliChiwimbi
@JafaliChiwimbi 6 дней назад
Kkkkkkk
@malikiabdulaziz
@malikiabdulaziz 6 дней назад
Utm nawonso asankhe mtsogoleri wawo yemwe akapitilitse mgwirizano wa mcp n utm. Michael ussi is not vice president for Malawi ussi is for mcp.
@OwamThoko
@OwamThoko 6 дней назад
Advise yoipa imeneyo asamamuze chakwela kuti wakuti wabwela ndiboza aphesa anthu
@MosesLeckson
@MosesLeckson 6 дней назад
Koma iyeyu ndege saziiopa?
@PamexMasanjala
@PamexMasanjala 6 дней назад
koma bola osamak panga sewelo
@nmbongeni27955
@nmbongeni27955 6 дней назад
agalu😂😂😂
@Dickies-mk8cd
@Dickies-mk8cd 6 дней назад
UTM musasekelele apa akufuna kukupakani mafuta kukamwa chabe. Usi siwa UTM
@kajawa6778
@kajawa6778 6 дней назад
Mkazi wachilima anachita kukana , chakwela anasankha mary Chilima
@Dickies-mk8cd
@Dickies-mk8cd 6 дней назад
Brian mongobweleza panyapako ndiiwe galu wa MCP, muli Kkkk kuseka amalawi tili mmasiku olira?
@YohanePatrick-lc2lq
@YohanePatrick-lc2lq 6 дней назад
Inu mukamati president mukunena chakwela yo ife kuna tilibe president ayi tilindi galu chakwela ndi galu dzikoli lalowa ma masewela latha basi paka manganya inu koma mukuti ganidzila ku malawi kuno mulungu chonde tithandidzeni kuno kumalawi tili ndi ophudzila ambili ambili koma panopa dzikoli likuyendesedwa nimbuli chonde mulungu tikakhala kuti ife ananu mulungu
@user-ct2ys7su2e
@user-ct2ys7su2e 6 дней назад
Mulungu amatenga zonyozekazo kuti zichitse manyazi amzeru nu ndipo mulungu si james
@Dickies-mk8cd
@Dickies-mk8cd 6 дней назад
Atumikile ndani Manganyayo ? Amalawi ake atiwo? Usi ndi mbuzi munthu oti anali nawo ku mkumano wadzidzi omwe mcp inapanga usiku wapa 10 June Chilima akuphupha ndi imfa
@raymondedwardo1188
@raymondedwardo1188 6 дней назад
What did he do to try to help chilima as he was his vise when the search was obviously being handled poorly. Anakayesesa pa yekha to demand better response.not to be trusted, Njoka ya mitu iwiri.
@malikiabdulaziz
@malikiabdulaziz 6 дней назад
Anangokhala chete osalunkhula kalikonse. Kodi kusangidwa kwa Michael ussi asangidwa kuchokera ku mcp or utm? Nanga mgwirizano udakalipobe? A kuti Dr ussi anachosedwa ku utm nanga asangidwa kuchipani chiti?
@OwamThoko
@OwamThoko 6 дней назад
And i hope a usi athandiza kufufuza zoona pangozi ya chilima
@mcsellahntv6896
@mcsellahntv6896 6 дней назад
Forget it, usi move yonse ya chilima amaiziwa bwino. Anamupanga promise udindou kale asanakonze chilima uja. Sunamuone mene amachitira behave nthawi ya maliro sanayankhuleko and anachita attend ma conference awiri okha kenaka anathamangitsidwa ataoneledwa kuti ali mgulumo. Panopa usi ndi wa MCP.
@aaronbanda4494
@aaronbanda4494 6 дней назад
Kkkkk mayesa Inu amalawi mumacula za cibanzi! Amuika cibanzi bambo usi sangakambe ciliconse.
@NumbDee
@NumbDee 6 дней назад
Victor Msalawatha kuno
@user-yk5xv4dt7v
@user-yk5xv4dt7v 6 дней назад
Siwa utm ndi wa mcp
@aloysiusdidymus7869
@aloysiusdidymus7869 6 дней назад
Abambo a sikono
@user-zk7jw9up6m
@user-zk7jw9up6m 6 дней назад
Kale Brian amayankhula koma pano akudya ndalama za boma la MCP
@AchinaKellz
@AchinaKellz 6 дней назад
Pajatu ndiwa mcp kale mphuno salota ine sizaoneranso masewero ose andinyasa
@user-hl3vl9nt1b
@user-hl3vl9nt1b 6 дней назад
Michael usi wakagazi uyu mxm
@Dickies-mk8cd
@Dickies-mk8cd 6 дней назад
Inu ndi agaludi mukanene kut dzulo lino amasomphenya ndi Chakwela ndi Usi? Mukugwilapo ntchito mwandale pamenepo
@user-hm9nc7lz6e
@user-hm9nc7lz6e 6 дней назад
Akupha ndi wako ndimayesa micheal utsi wacoka ku u t m manga akhala vice bwanji
@PatrickKaunda-qx7qd
@PatrickKaunda-qx7qd 6 дней назад
Wachoka lit?
@user-hm9nc7lz6e
@user-hm9nc7lz6e 5 дней назад
@@PatrickKaunda-qx7qd anali wa mcp osati wa utm
@hopembendela
@hopembendela 6 дней назад
manganya pa malilo anangoti chete osalankhula kalikonse amaziwa chomwe amapanga ndi munthu oipa
@Dickies-mk8cd
@Dickies-mk8cd 6 дней назад
Usi wafanso basi
@AlexKaunda-ny2eg
@AlexKaunda-ny2eg 6 дней назад
Manganya machende ako iwe ndi amene wagulisa chilima 😢😢😢
@malikiabdulaziz
@malikiabdulaziz 6 дней назад
Michal ussi ndakudabwani simunalankhule Kalikonse pamaliro achilima. Don't forget chilima he was the one who put you in the government with utm party.
@OwamThoko
@OwamThoko 6 дней назад
Inu ausi malangizo muzikapepha kwa adad abingu
@WysonChilonga
@WysonChilonga 6 дней назад
😅😅
Далее
Iindaba zesiXhosa @13H00 | 27 June 2024
23:20
Просмотров 13 тыс.
LISA - ROCKSTAR (MV Teaser)
00:10
Просмотров 6 млн
Recycled Car Tyres Get a Second Life! ♻️
00:58
Просмотров 543 тыс.
ZAMA PASSPORT ZIKUTHA BWANJI?26 June 2024
22:17
Просмотров 15 тыс.
KUCHIPANI CHA UTM CHADABWITSA ANTHU🤔🤔
49:16
Просмотров 66 тыс.
LIVE 🔴  KTN NEWS KENYA
Просмотров 7 тыс.
Mbiri ya Mama Cecilia Kadzamira
29:43
Просмотров 199 тыс.
KWAPHULIKA AUDIO YACHILIMA MU NDEGE ISANAGWE. TAMVANI
10:45
LISA - ROCKSTAR (MV Teaser)
00:10
Просмотров 6 млн